Cânticos 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Nyimbo ya Solomoni, nyimbo yoposa nyimbo zonse.

2 Undipsompsone ndi milomo yako

3 Mafuta ako odzola ndi onunkhira bwino;

4 Nditenge ndipo ndizikutsata, tiye tifulumire!

5 Ndine wakuda, komatu ndine wokongola,

6 Musandiyangʼane monyoza chifukwa ndine wakuda,

7 Ndiwuze iwe, amene ndimakukonda, kumene umadyetsa ziweto zako

8 Ngati sukudziwa iwe wokongola kwambiri kuposa akazi ena,

9 Iwe bwenzi langa,

10 Masaya ako ndi okongola ndi ndolo zamʼmakutuzo,

11 Tidzakupangira ndolo zagolide

12 Pamene mfumu inali pa malo ake odyera,

13 Wokondedwa wanga ali ngati kathumba ka mure kwa ine,

14 Wokondedwa wanga ali ngati mpukutu wa maluwa ofiira,

15 Iwe wokondedwa wanga, ndiwe wokongoladi!

16 Iwe bwenzi langa, ndiwe wokongoladi!

17 Mitanda ya nyumba yathu ndi ya mkungudza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Cânticos 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.