Salmos 72

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Patsani mwana wa mfumu nzeru zanu zoweruzira mwa chilungamo,

2 Iye adzaweruza anthu anu mwachilungamo,

3 Mapiri adzabweretsa chuma kwa anthu anu,

4 Iye adzateteza ozunzika pakati pa anthu

5 Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse,

6 Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa

7 Mʼmasiku a munthu wolungama adzakhazikika;

8 Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina

9 Mafuko a mʼchipululu adzawerama pamaso pake

10 Mafumu a ku Tarisisi ndi a ku zilumba zakutali

11 Mafumu onse adzamuweramira

12 Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira,

13 Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowa

14 Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawa

15 Iye akhale ndi moyo wautali;

16 Mulole kuti tirigu achuluke mʼdziko lonse;

17 Dzina lake likhazikike kwamuyaya,

18 Matamando akhale kwa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israeli

19 Matamando akhale ku dzina lake laulemerero kwamuyaya

20 Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 72, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.