Salmos 81

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Imbani mwachimwemwe kwa Mulungu mphamvu yathu;

2 Yambani nyimbo, imbani tambolini

3 Imbani lipenga la nyanga ya nkhosa yayimuna pa mwezi watsopano,

4 ili ndi lamulo kwa Israeli,

5 Iye anapereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe

6 Iye akunena kuti, “Ine ndinachotsa zolemetsa pa mapewa awo;

7 Pa mavuto anu munayitana ndipo ndinakulanditsani,

8 “Imvani anthu anga, ndipo ndidzakuchenjezani

9 Musadzakhale ndi mulungu wachilendo pakati panu;

10 Ine ndine Yehova Mulungu wanu,

11 “Koma anthu anga sanandimvere;

12 Kotero ndinawasiya ndi mitima yawo yosamverayo

13 “Anthu anga akanangondimvera,

14 nʼkanafulumira motani kuti ndigonjetse adani awo

15 Iwo amene amadana ndi Yehova akanakhwinyata pamaso pake,

16 Koma inu mukanadyetsedwa tirigu wabwino kwambiri;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 81, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.