Isaías 32

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Taonani, kudzakhala mfumu ina imene idzalamulira mwachilungamo,

2 Munthu aliyense adzakhala ngati pothawirapo mphepo

3 Ndipo maso a anthu openya sadzakhalanso otseka,

4 Anthu a mtima wopupuluma adzadziwa ndi kuchita zinthu mofatsa,

5 Chitsiru sichidzatchedwanso munthu waulemu wake

6 Pakuti munthu opusa amayankhula zauchitsiru,

7 Munthu woyipa njira zake ndi zoyipanso,

8 Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino,

9 Khalani maso, inu akazi

10 Pakapita chaka ndi masiku pangʼono

11 Nthunthumirani inu okhala mosatekesekanu;

12 Dzigugudeni pachifuwa mwachisoni chifukwa minda yachonde,

13 Mʼdziko la anthu anga

14 Nyumba yaufumu idzasiyidwa,

15 Yehova adzatipatsa mzimu wake,

16 Tsono mʼchipululu mudzakhala chiweruzo cholungama

17 Mtendere udzakhala chipatso chachilungamo;

18 Anthu anga adzakhala mʼmidzi yamtendere,

19 Ngakhale nkhalango idzawonongedwa ndi matalala

20 inutu mudzakhala odalitsika ndithu.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 32, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.