Salmos 90

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Ambuye, mwakhala muli malo athu okhalamo

2 Mapiri asanabadwe,

3 Inu mumabwezera anthu ku fumbi,

4 Pakuti zaka 1,000 pamaso panu

5 Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa,

6 ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano,

7 Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu;

8 Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu,

9 Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu;

10 Kuchuluka kwa masiku athu ndi 70,

11 Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu?

12 Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola,

13 Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?

14 Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha,

15 Tisangalatseni masiku ambiri monga masiku amene mwatisautsa,

16 Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu,

17 Kukoma mtima kwa Ambuye Mulungu wathu kukhale pa ife;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 90, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.