Salmos 59

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Landitseni kwa adani anga, Inu Mulungu;

2 Landitseni kwa anthu ochita zoyipa

3 Onani momwe iwo akundibisalira!

4 Ine sindinachite cholakwa, koma iwo ndi okonzeka kundithira nkhondo.

5 Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli,

6 Iwo amabweranso madzulo

7 Onani zomwe amalavula mʼkamwa mwawo;

8 Koma Inu Yehova, mumawaseka,

9 Inu mphamvu yanga, ine ndiyangʼana kwa inu;

10 Mulungu wanga wachikondi.

11 Koma musawaphe, Inu Ambuye chishango chathu,

12 Chifukwa cha machimo a pakamwa pawo

13 muwawononge mu ukali (wanu)

14 Iwo amabweranso madzulo,

15 Iwo amayendayenda kufuna chakudya

16 Koma ine ndidzayimba za mphamvu yanu,

17 Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 59, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.