Salmos 60

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza.

2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba,

3 Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto;

4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera

5 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja,

6 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:

7 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;

8 Mowabu ndi mbale yanga yosambira,

9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa?

10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife

11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu,

12 Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 60, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.