Salmos 41

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka;

2 Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake;

3 Yehova adzamuthandiza pamene akudwala

4 Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo;

5 Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti,

6 Pamene wina abwera kudzandiona,

7 Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane,

8 “Matenda owopsa amugwira;

9 Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira,

10 Koma Yehova mundichititre chifundo,

11 Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane,

12 Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga

13 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 41, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.