Provérbios 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Nzeru inamanga nyumba yake;

2 Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake;

3 Nzeruyo inatuma adzakazi ake,

4 “Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!”

5 “Bwerani, dzadyeni chakudya changa

6 Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo;

7 Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo;

8 Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe;

9 Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru;

10 Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru;

11 Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka,

12 Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa;

13 Uchitsiru ndi mkazi waphokoso,

14 Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake,

15 kuti aziyitana anthu ongodutsa,

16 Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,”

17 “Madzi akuba ndiye amatsekemera;

18 Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Provérbios 9, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.