Gênesis 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs NVT

Sair da comparação
NVT Nova Versão Transformadora
1 Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi:
1 Este é o relato dos descendentes de Adão. Quando Deus criou os seres humanos, formou-os semelhantes a ele.
2 Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”
2 Criou-os homem e mulher; quando foram criados, Deus os abençoou e os chamou de “humanidade”.
3 Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti.
3 Aos 130 anos, Adão teve um filho chamado Sete, que era semelhante a ele, à sua imagem.
4 Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
4 Depois do nascimento de Sete, Adão viveu mais 800 anos e teve outros filhos e filhas.
5 Zaka zonse za Adamu zinali 930 ndipo anamwalira.
5 Adão viveu 930 anos e morreu.
6 Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi.
6 Aos 105 anos, Sete gerou Enos.
7 Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
7 Depois do nascimento de Enos, Sete viveu mais 807 anos e teve outros filhos e filhas.
8 Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.
8 Sete viveu 912 anos e morreu.
9 Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.
9 Aos 90 anos, Enos gerou Cainã.
10 Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
10 Depois do nascimento de Cainã, Enos viveu mais 815 anos e teve outros filhos e filhas.
11 Zaka zonse za Enosi pamodzi zinali 905 ndipo anamwalira.
11 Enos viveu 905 anos e morreu.
12 Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.
12 Aos 70 anos, Cainã gerou Maalaleel.
13 Atabadwa Mahalaleli, Kenani anakhala ndi moyo zaka zina 840 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
13 Depois do nascimento de Maalaleel, Cainã viveu mais 840 anos e teve outros filhos e filhas.
14 Zaka zonse za Kenani zinali 910, ndipo anamwalira.
14 Cainã viveu 910 anos e morreu.
15 Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi.
15 Aos 65 anos, Maalaleel gerou Jarede.
16 Atabadwa Yaredi, Mahalaleli anakhala ndi moyo zaka zina 830 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
16 Depois do nascimento de Jarede, Maalaleel viveu mais 830 anos e teve outros filhos e filhas.
17 Zaka zonse za Mahalaleli zinali 895 ndipo anamwalira.
17 Maalaleel viveu 895 anos e morreu.
18 Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki.
18 Aos 162 anos, Jarede gerou Enoque.
19 Atabadwa Enoki, Yaredi anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
19 Depois do nascimento de Enoque, Jarede viveu mais 800 anos e teve outros filhos e filhas.
20 Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.
20 Jarede viveu 962 anos e morreu.
21 Pamene Enoki anali ndi zaka 65, anabereka Metusela.
21 Aos 65 anos, Enoque gerou Matusalém.
22 Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
22 Depois do nascimento de Matusalém, Enoque viveu em comunhão com Deus por mais 300 anos e teve outros filhos e filhas.
23 Zaka zonse za Enoki zinali 365.
23 Enoque viveu 365 anos,
24 Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.
24 andando em comunhão com Deus até que, um dia, desapareceu, porque Deus o levou para junto de si.
25 Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki.
25 Aos 187 anos, Matusalém gerou Lameque.
26 Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
26 Depois do nascimento de Lameque, Matusalém viveu mais 782 anos e teve outros filhos e filhas.
27 Zaka zonse za Metusela zinali 969, ndipo anamwalira.
27 Matusalém viveu 969 anos e morreu.
28 Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.
28 Aos 182 anos, Lameque gerou um filho.
29 Ndipo anamutcha Nowa ndipo anati, “Iyeyu adzatipumulitsa ku ntchito zathu zolemetsazi, zolima nthaka imene Yehova anayitemberera.”
29 Chamou-o de Noé, pois disse: “Que ele nos traga alívio de nossas tarefas e do trabalho doloroso de cultivar esta terra que o S enhor amaldiçoou”.
30 Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
30 Depois do nascimento de Noé, Lameque viveu mais 595 anos e teve outros filhos e filhas.
31 Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.
31 Lameque viveu 777 anos e morreu.
32 Pamene Nowa anali ndi zaka 500, anabereka Semu, Hamu ndi Yafeti.
32 Depois que completou 500 anos, Noé gerou três filhos: Sem, Cam e Jafé.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Gênesis 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.