Deuteronômio 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs NTLH

Sair da comparação
NTLH Nova Tradução na Linguagem de Hoje 2000
1 Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu. Osamadzichekacheka kapena kudzimeta pamphumi chifukwa cha abale anu amene amwalira,
1 Moisés disse ao povo: — Vocês são filhos do
2 pakuti ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu. Pakati pa anthu onse pa dziko lonse lapansi, Yehova wasankha inu kuti chikhale chuma chake chamtengo wapatali.
2 Pois vocês são o povo escolhido pelo Senhor , nosso Deus; entre todos os povos da terra ele os escolheu para serem somente dele.
3 Musamadye chinthu chilichonse chonyansa.
3 — Não comam nada que seja impuro .
4 Nyama zomwe mukhoza kudya ndi izi: ngʼombe, nkhosa, mbuzi,
4 Vocês podem comer a carne dos seguintes animais: vacas, carneiros, cabritos,
5 mbawala, gwape, mphoyo, mphalapala, ngoma, nyumbu ndi mbalale.
5 veados, gazelas , corços , cabritos selvagens, antílopes, carneiros selvagens e gamos.
6 Nyama iliyonse imene ili ndi chipondero chogawikana pakati ndi yobzikula mukhoza kudya.
6 Todos esses animais têm o casco dividido em dois, e ruminam, e podem ser comidos.
7 Komabe pakati pa nyama zimene zimabzikula kapena zogawikana zipondero, zimene simukuyenera kudya ndi ngamira, kalulu ndi mbira. Zimenezi ngakhale zimabzikula, zipondero zake sizogawikana, choncho ndi zodetsedwa, musadye.
7 Mas nenhum animal deve ser comido, a não ser que tenha o casco dividido e que rumine. Portanto, não comam camelos, lebres ou coelhos selvagens, pois ruminam, mas não têm o casco dividido. Para vocês esses animais são impuros.
8 Nkhumba simabzikula ndi yodetsedwanso ngakhale ili ndi zipondero zogawikana. Musamadye nyama yake kapena kukhudza imene yafa.
8 Não comam carne de porco. Para vocês os porcos são impuros porque têm o casco dividido, mas não ruminam. Não comam nenhum desses animais, nem toquem neles quando estiverem mortos.
9 Mwa zamoyo zonse zimene zimakhala mʼmadzi, mukhoza kudya chilichonse chimene chili ndi minga ya pa msana ndi mamba.
9 — Vocês podem comer qualquer peixe que tenha barbatanas e escamas,
10 Koma chilichonse chimene chilibe minga ya pa msana ndi mamba musadye pakuti nʼchodetsedwa.
10 mas não podem comer peixes que não tenham barbatanas nem escamas. Para vocês esses peixes são impuros.
11 Mukhoza kudya mbalame iliyonse yoyenera kudya.
11 — Vocês podem comer qualquer ave pura ,
12 Koma simukuyenera kudya izi: mphungu, nkhwazi, mwimba,
12 porém não comam as seguintes aves : águias, urubus, águias marinhas,
13 nankapakapa, akamtema, akhungubwi a mitundu yonse, ndi mtundu uliwonse wa miphamba,
13 açores, falcões,
14 mtundu uliwonse wa khwangwala,
14 corvos,
15 kadzidzi wamphondo, kadzidzi wodzuma, chipudo, mtundu uliwonse wa akabawi,
15 avestruzes, corujas, gaivotas, gaviões,
16 kadzidzi wamngʼono, chiswankhono ndi mantchichi,
16 mochos, íbis, gralhas,
17 tsekwe, vuwo, dembo,
17 pelicanos, abutres, corvos marinhos,
18 indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.
18 cegonhas, garças e poupas; e também morcegos.
19 Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa. Musamadye zimenezi.
19 — Todos os insetos que voam são impuros; vocês não podem comê-los.
20 Koma chowuluka chilichonse choyenera kudya mukhoza kudya.
20 Mas podem comer todos os insetos puros.
21 Musamadye chilichonse chimene mwachipeza chofaifa. Mukhoza kupatsa mlendo amene akukhala mu mzinda wina uliwonse wa mizinda yanu. Iyeyo akhoza kudya kapena mukhoza kugulitsa kwa wina aliyense amene sali wa mtundu wanu. Koma inu ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu.
21 — Não comam qualquer animal que tenha tido morte natural. Vocês podem dar o animal aos estrangeiros que moram nas cidades de vocês ou podem vendê-lo a outros estrangeiros. Mas vocês não o podem comer, pois são o povo escolhido pelo Senhor , nosso Deus. — Não cozinhem um cabrito ou um carneirinho no leite da sua própria mãe .
22 Muzionetsetsa kuti mukupatula chakhumi pa zokolola zanu chaka chilichonse.
22 — Todos os anos juntem uma décima parte de todas as colheitas
23 Muzidyera chakhumi cha tirigu wanu, vinyo wanu watsopano ndi mafuta, ndi ana oyamba kubadwa a ngʼombe zanu pamaso pa Yehova Mulungu wanu pa malo amene adzasankhe ngati kokhalako dzina lake, kuti muphunzire kuopa Yehova Mulungu wanu.
23 e levem até o lugar que o Senhor , nosso Deus, tiver escolhido para nele ser adorado. Ali, na presença do Senhor , nosso Deus, comam aquela décima parte dos cereais, do vinho e do azeite e também a primeira cria das vacas e das ovelhas. Façam isso para aprender a temer a Deus para sempre.
24 Koma ngati malo amenewa ali kutali kwambiri ndipo kuti inu mwadalitsidwa ndi Yehova Mulungu wanu, ndipo simungathe kunyamula chakhumi chanu (chifukwa chakuti malo amene Yehova adzasankha kukayikako dzina lake ali kutali kwambiri),
24 Mas, se o lugar de adoração ficar muito longe, e for impossível levar até lá a décima parte das colheitas com que Deus os abençoou,
25 ndiye musinthitse chakhumi chanucho ndi siliva, ndipo mutenge silivayo ndi kupita naye kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhe.
25 então façam isto: vendam aquela parte das colheitas, levem o dinheiro até o lugar de adoração que o Senhor tiver escolhido
26 Gwiritsani ntchito silivayo kugula chilichonse chimene muchifuna monga ngʼombe, nkhosa, vinyo kapena zakumwa zina zosasitsa, kapena china chilichonse chimene muchifuna. Ndipo inu ndi anthu a pa banja panu mudzazidyera komweko pamaso pa Yehova Mulungu wanu ndi kukondwera.
26 e ali comprem tudo o que quiserem comer: carne de vaca ou de carneiro, vinho, cerveja ou qualquer outra coisa que desejarem. E ali, na presença do Senhor , nosso Deus, vocês e as suas famílias comam essas coisas e se divirtam à vontade.
27 Alevi okhala mʼmizinda yanu musaleke kuwathandiza popeza alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo.
27 — Porém não esqueçam os levitas que moram nas cidades de vocês. Eles não receberão terras em Canaã, como as outras tribos .
28 Kumapeto kwa zaka zitatu zilizonse muzibweretsa zakhumi zonse pa zokolola za chaka chimenecho ndi kuzisunga mʼmidzi yanu,
28 De três em três anos juntem a décima parte das colheitas daquele ano e guardem nas cidades onde vocês moram.
29 kuti Alevi (amene alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo), alendo, ana ndi akazi amasiye, amene akukhala mʼmizinda yanu akhoza kubwera kudzadya ndi kukhuta. Ndipo kuti akutero Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa ntchito zanu zonse.
29 Essa comida é para os levitas, pois eles não têm terras próprias; é também para os estrangeiros, os órfãos e as viúvas que moram nas cidades de vocês. Assim todos eles terão toda a comida que precisarem. Façam isso para que o Senhor , nosso Deus, abençoe todo o trabalho de vocês.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Deuteronômio 14, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.