Deuteronômio 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs ARC

Sair da comparação
ARC Almeida Revista e Corrigida 2009
1 Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu. Osamadzichekacheka kapena kudzimeta pamphumi chifukwa cha abale anu amene amwalira,
1 Filhos sois do Senhor , vosso Deus; não vos dareis golpes, nem poreis calva entre vossos olhos por causa de algum morto.
2 pakuti ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu. Pakati pa anthu onse pa dziko lonse lapansi, Yehova wasankha inu kuti chikhale chuma chake chamtengo wapatali.
2 Porque és povo santo ao Senhor , teu Deus, e o Senhor te escolheu de todos os povos que há sobre a face da terra, para lhe seres o seu povo próprio.
3 Musamadye chinthu chilichonse chonyansa.
3 Nenhuma abominação comereis.
4 Nyama zomwe mukhoza kudya ndi izi: ngʼombe, nkhosa, mbuzi,
4 Estes são os animais que comereis: o boi, o gado miúdo das ovelhas, o gado miúdo das cabras,
5 mbawala, gwape, mphoyo, mphalapala, ngoma, nyumbu ndi mbalale.
5 o veado, a corça, o búfalo, a cabra montês, o texugo, o boi silvestre e o gamo.
6 Nyama iliyonse imene ili ndi chipondero chogawikana pakati ndi yobzikula mukhoza kudya.
6 Todo animal que tem unhas fendidas, que tem a unha dividida em duas, que remói, entre os animais, isso comereis.
7 Komabe pakati pa nyama zimene zimabzikula kapena zogawikana zipondero, zimene simukuyenera kudya ndi ngamira, kalulu ndi mbira. Zimenezi ngakhale zimabzikula, zipondero zake sizogawikana, choncho ndi zodetsedwa, musadye.
7 Porém estes não comereis, dos que somente remoem ou que têm a unha fendida: o camelo, a lebre e o coelho, porque remoem, mas não têm a unha fendida; imundos vos serão.
8 Nkhumba simabzikula ndi yodetsedwanso ngakhale ili ndi zipondero zogawikana. Musamadye nyama yake kapena kukhudza imene yafa.
8 Nem o porco, porque tem unhas fendidas, mas não remói; imundo vos será; não comereis da carne destes e não tocareis no seu cadáver.
9 Mwa zamoyo zonse zimene zimakhala mʼmadzi, mukhoza kudya chilichonse chimene chili ndi minga ya pa msana ndi mamba.
9 Isto comereis de tudo o que há nas águas: tudo o que tem barbatanas e escamas comereis.
10 Koma chilichonse chimene chilibe minga ya pa msana ndi mamba musadye pakuti nʼchodetsedwa.
10 Mas tudo o que não tiver barbatanas nem escamas não o comereis; imundo vos será.
11 Mukhoza kudya mbalame iliyonse yoyenera kudya.
11 Toda ave limpa comereis.
12 Koma simukuyenera kudya izi: mphungu, nkhwazi, mwimba,
12 Porém estas são as de que não comereis: a águia, o quebrantosso, o xofrango,
13 nankapakapa, akamtema, akhungubwi a mitundu yonse, ndi mtundu uliwonse wa miphamba,
13 o abutre, a pega e o milhano, segundo a sua espécie;
14 mtundu uliwonse wa khwangwala,
14 e todo o corvo, segundo a sua espécie;
15 kadzidzi wamphondo, kadzidzi wodzuma, chipudo, mtundu uliwonse wa akabawi,
15 o avestruz, o mocho, o cuco e o gavião, segundo a sua espécie;
16 kadzidzi wamngʼono, chiswankhono ndi mantchichi,
16 e o bufo, a coruja, a gralha,
17 tsekwe, vuwo, dembo,
17 o cisne, o pelicano, o corvo-marinho,
18 indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.
18 a cegonha, a garça, segundo a sua espécie, a poupa, e o morcego.
19 Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa. Musamadye zimenezi.
19 Também todo réptil que voa vos será imundo; não se comerá.
20 Koma chowuluka chilichonse choyenera kudya mukhoza kudya.
20 Toda ave limpa comereis.
21 Musamadye chilichonse chimene mwachipeza chofaifa. Mukhoza kupatsa mlendo amene akukhala mu mzinda wina uliwonse wa mizinda yanu. Iyeyo akhoza kudya kapena mukhoza kugulitsa kwa wina aliyense amene sali wa mtundu wanu. Koma inu ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu.
21 Não comereis nenhum animal morto; ao estrangeiro, que está dentro das tuas portas, o darás a comer ou o venderás ao estranho, porquanto és povo santo ao Senhor , teu Deus. Não cozerás o cabrito com o leite da sua mãe.
22 Muzionetsetsa kuti mukupatula chakhumi pa zokolola zanu chaka chilichonse.
22 Certamente darás os dízimos de toda a novidade da tua semente, que cada ano se recolher do campo.
23 Muzidyera chakhumi cha tirigu wanu, vinyo wanu watsopano ndi mafuta, ndi ana oyamba kubadwa a ngʼombe zanu pamaso pa Yehova Mulungu wanu pa malo amene adzasankhe ngati kokhalako dzina lake, kuti muphunzire kuopa Yehova Mulungu wanu.
23 E, perante o Senhor , teu Deus, no lugar que escolher para ali fazer habitar o seu nome, comerás os dízimos do teu cereal, do teu mosto, do teu azeite e os primogênitos das tuas vacas e das tuas ovelhas; para que aprendas a temer ao Senhor , teu Deus, todos os dias.
24 Koma ngati malo amenewa ali kutali kwambiri ndipo kuti inu mwadalitsidwa ndi Yehova Mulungu wanu, ndipo simungathe kunyamula chakhumi chanu (chifukwa chakuti malo amene Yehova adzasankha kukayikako dzina lake ali kutali kwambiri),
24 E, quando o caminho te for tão comprido, que os não possas levar, por estar longe de ti o lugar que escolher o Senhor , teu Deus, para ali pôr o seu nome, quando o Senhor , teu Deus, te tiver abençoado,
25 ndiye musinthitse chakhumi chanucho ndi siliva, ndipo mutenge silivayo ndi kupita naye kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhe.
25 então, vende-os, e ata o dinheiro na tua mão, e vai ao lugar que escolher o Senhor , teu Deus.
26 Gwiritsani ntchito silivayo kugula chilichonse chimene muchifuna monga ngʼombe, nkhosa, vinyo kapena zakumwa zina zosasitsa, kapena china chilichonse chimene muchifuna. Ndipo inu ndi anthu a pa banja panu mudzazidyera komweko pamaso pa Yehova Mulungu wanu ndi kukondwera.
26 E aquele dinheiro darás por tudo o que deseja a tua alma, por vacas, e por ovelhas, e por vinho, e por bebida forte, e por tudo o que te pedir a tua alma; come-o ali perante o Senhor , teu Deus, e alegra-te, tu e a tua casa;
27 Alevi okhala mʼmizinda yanu musaleke kuwathandiza popeza alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo.
27 porém não desampararás o levita que está dentro das tuas portas; pois não tem parte nem herança contigo.
28 Kumapeto kwa zaka zitatu zilizonse muzibweretsa zakhumi zonse pa zokolola za chaka chimenecho ndi kuzisunga mʼmidzi yanu,
28 Ao fim de três anos, tirarás todos os dízimos da tua novidade no mesmo ano e os recolherás nas tuas portas.
29 kuti Alevi (amene alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo), alendo, ana ndi akazi amasiye, amene akukhala mʼmizinda yanu akhoza kubwera kudzadya ndi kukhuta. Ndipo kuti akutero Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa ntchito zanu zonse.
29 Então, virá o levita ( pois nem parte nem herança tem contigo), e o estrangeiro, e o órfão, e a viúva, que estão dentro das tuas portas, e comerão, e fartar-se-ão, para que o Senhor , teu Deus, te abençoe em toda a obra das tuas mãos, que fizeres.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Deuteronômio 14, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.