1 Tessalonicenses 5
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs NVT
1 Tsono abale, za nthawi ndi nyengo yake nʼkosafunikira kuti tikulembereni,
1 Não é necessário, irmãos, que eu lhes escreva sobre quando e como tudo isso acontecerá,
2 chifukwa mukudziwa bwino lomwe kuti tsiku la Ambuye lidzafika ngati mbala usiku.
2 pois vocês sabem muito bem que o dia do Senhor virá inesperadamente, como ladrão à noite.
3 Pamene anthu akunena kuti, “Mtendere ndi chitetezo,” chiwonongeko chidzafika pa iwo mwadzidzidzi, monga zowawa za amayi pobereka, ndipo sadzathawa.
3 Quando as pessoas disserem: “Tudo está em paz e seguro”, então o desastre lhes sobrevirá tão repentinamente como iniciam as dores de parto de uma mulher grávida, e não haverá como escapar.
4 Koma inu abale, simuli mu mdima kuti tsiku limeneli lidzakudzidzimutseni ngati mbala.
4 Mas vocês, irmãos, não estão na escuridão a respeito dessas coisas e não devem se surpreender quando o dia do Senhor vier como ladrão.
5 Nonse ndinu ana a kuwunika ndi ana a usana. Sindife anthu a usiku kapena mdima.
5 Porque todos vocês são filhos da luz e do dia. Não pertencemos à escuridão e à noite.
6 Chomwecho tsono, tisafanane ndi ena amene akugona koma tikhale maso ndi odzisunga.
6 Portanto, fiquem atentos; não durmam como os outros. Permaneçam atentos e sejam sóbrios.
7 Pakuti amene akugona, amagona usiku, ndi amene amaledzera, amaledzera usiku.
7 À noite, as pessoas dormem e os bêbados se embriagam.
8 Koma popeza ndife a usana, tikhale odzisunga, titavala chikhulupiriro ndi chikondi ngati chovala pachifuwa, ndi chiyembekezo cha chipulumutso ngati chipewa.
8 Mas nós, que vivemos na luz, devemos ser sóbrios, protegidos pela armadura da fé e do amor, usando o capacete da esperança da salvação.
9 Pakuti Mulungu sanatisankhe kuti tikavutike ndi mkwiyo koma kuti tilandire chipulumutso kudzera mwa Ambuye athu Yesu Khristu.
9 Porque Deus decidiu nos salvar por meio de nosso Senhor Jesus Cristo, em vez de derramar sua ira sobre nós.
10 Iye anatifera ndi cholinga chakuti, kaya tili ndi moyo kapena tagona, tikhale naye pamodzi.
10 Cristo morreu por nós para que, quer estejamos despertos, quer dormindo, vivamos com ele para sempre.
11 Choncho limbikitsanani wina ndi mnzake ndi kuthandizana kukula mu mzimu, monga momwe mukuchitira.
11 Portanto, animem e edifiquem uns aos outros, como têm feito.
12 Tsopano tikukupemphani abale kuti muziwalemekeza amene akugwira ntchito pakati panu, amene amakuyangʼanirani mwa Ambuye ndi amene amakulimbikitsani.
12 Irmãos, honrem seus líderes na obra do Senhor. Eles trabalham arduamente entre vocês e lhes dão orientações.
13 Muziwachitira ulemu kwambiri mwachikondi chifukwa cha ntchito yawo. Mukhale pa mtendere wina ndi mnzake.
13 Tenham grande respeito e amor sincero por eles, por causa do trabalho que realizam. E vivam em paz uns com os outros.
14 Ndipo tikukupemphani abale, muwachenjeze amene akungokhala osagwira ntchito, alimbikitseni amanyazi, thandizani ofowoka ndipo muzilezera mtima aliyense.
14 Irmãos, pedimos que advirtam os indisciplinados. Encorajem os desanimados. Ajudem os fracos. Sejam pacientes com todos.
15 Onetsetsani kuti wina asabwezere choyipa kwa omuchitira choyipa koma nthawi zonse yesetsani kukhala okoma mtima kwa wina ndi mnzake; ndiponso ndi kwa anthu ena onse.
15 Cuidem que ninguém retribua o mal com o mal, mas procurem sempre fazer o bem uns aos outros e a todos.
16 Kondwerani nthawi zonse.
16 Estejam sempre alegres.
17 Pempherani kosalekeza.
17 Nunca deixem de orar.
18 Yamikani mu zonse, pakuti ichi ndi chifuniro cha Mulungu kwa inu mwa Khristu Yesu.
18 Sejam gratos em todas as circunstâncias, pois essa é a vontade de Deus para vocês em Cristo Jesus.
19 Musazimitse moto wa Mzimu Woyera.
19 Não apaguem o Espírito.
20 Musanyoze mawu a uneneri.
20 Não desprezem as profecias,
21 Yesani zinthu zonse. Gwiritsitsani chimene ndi chabwino.
21 mas ponham à prova tudo que é dito e fiquem com o que é bom.
22 Mupewe choyipa cha mtundu wina uliwonse.
22 Mantenham-se afastados de toda forma de mal.
23 Mulungu mwini, Mulungu wamtendere, akuyeretseni kotheratu. Mzimu wanu wonse, moyo ndi thupi zisungidwe zopanda cholakwa mpaka kubwera kwa Ambuye athu Yesu Khristu.
23 E, agora, que o Deus da paz os torne santos em todos os aspectos, e que o espírito, a alma e o corpo de vocês sejam mantidos irrepreensíveis até a volta de nosso Senhor Jesus Cristo.
24 Amene anakuyitanani ndi wokhulupirika ndipo Iye adzachita zimenezi.
24 Aquele que os chama fará isso acontecer, pois ele é fiel.
25 Abale, mutipempherere.
25 Irmãos, orem por nós.
26 Perekani moni wachikondi kwa onse.
26 Cumprimentem todos os irmãos com beijo santo.
27 Pamaso pa Ambuye ndikulamula kuti kalatayi iwerengedwe kwa abale onse.
27 Encarrego-os em nome do Senhor de lerem esta carta a todos os irmãos.
28 Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu chikhale nanu.
28 Que a graça de nosso Senhor Jesus Cristo esteja com vocês.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Tessalonicenses 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.