1 Timóteo 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Tsono choyamba ndikukupemphani kuti mupempherere anthu onse. Mapemphero anu akhale opemba, opempha, opempherera ena ndi oyamika.
1 Isan imih antoro’ot au ototofaren tur i iti, ata fefeyan, ata yoyoban, ata yoyobanwainen, naatu ata merarayow sabuw tutufin etei isah kwanayoyoban,
2 Mupempherere mafumu ndi onse aulamuliro, kuti tikhale moyo wamtendere ndi bata, woopa Mulungu ndi oyera mtima.
2 aiwob sabuw isah, naatu sabuw iyab hi’ukwarin tema’am auman isah kwanayoyoban, saise it etei tufuw nuwarobamaim tanama God tanakakafiy tanabora’ara’ah.
3 Izi ndi zabwino ndipo zimakondweretsa Mulungu Mpulumutsi wathu,
3 Ef iti i gewasin naatu God ata baiyawasenayan i ebiyasisir,
4 amene amafuna kuti anthu onse apulumutsidwe ndipo kuti adziwe choonadi.
4 i ekokok sabuw etei’imak yawas hinab naatu hinan tur anababatun hinaso’ob,
5 Pakuti pali Mulungu mmodzi yekha ndi Mʼkhalapakati mmodzi yekha pakati pa Mulungu ndi anthu, munthu uja Khristu Yesu.
5 anayabin God i ta’imonamo, naatu orot foun bat sabuw bow na God bairi baitounuw isan i ta’imon, nati orot i Jesu Keriso akisin.
6 Iyeyu anadzipereka kukhala dipo lowombolera anthu onse. Umenewu ndi umboni umene waperekedwa mu nthawi yake yoyenera.
6 God ana sabuw baiyawasih isan ana veya yakitifuw inu’in na titit ana maramaim, Jesu Keriso taiyuwin ana yawas yare sabuw etei tubunih botaitih hitit.
7 Nʼchifukwa chake anandisankha kukhala mlaliki ndiponso mtumwi wophunzitsa anthu a mitundu ina mawu achikhulupiriro choona. Sindikunama ayi, ndikunena zoona.
7 Ana’an nati isan ayu tur abarin naatu tur binan isan God rubinu atit Ufun Sabuw isah baitumatum ana tur naatu turobe abi’obaibiyih. Ayu men abifufuwen ayu i tur anababatun au’uwi.
8 Choncho ndikufuna kuti paliponse popemphera, amuna azikweza manja awo kwa Mulungu mopanda mkwiyo kapena kukangana.
8 Isan imih ayu akokok kwafiren ana efan tata’amaim oro’orot etei umah kakafiyin hinabora’ah hinayoyoban, men yaso’ar gamin auman.
9 Ndikufunanso kuti amayi azivala mwaulemu, modzilemekeza ndi moyenera. Adzikongoletse koma osati ndi tsitsi loluka mowonjeza muyeso kapena zokongoletsa zagolide kapena mikanda yamtengowapatali kapena ndi zovala zamtengowapatali.
9 Iban maiye ayu akokok baibin hai faifuw i hina’osen gewas, naatu aribuh men yumatan ta ta hina’am kwanikwaniy, sawar hai baiyah gagamih hinabow aribuhimaim hinaya hinakusisiar, naatu faifuw baiyah gagamih hina’osenamih,
10 Koma adzikongoletse ndi ntchito zabwino zoyenera mayi wopembedza Mulungu.
10 baise itinin gewasin i hai faifuwamih hina’us, God kwafirin hirouw teo’o na’atube God ana kok hinasinaf sabuw afa hinibaisih.
11 Amayi azikhala chete pophunzitsidwa ndi mtima ogonjera kwathunthu.
11 Baibin so’ob hinakokok i hai yawas hinayare hinanutanubamo hinama tur hinanowar,
12 Ine sindikulola kuti amayi aziphunzitsa kapena kulamulira amuna; koma akhale chete.
12 ayu men abibasit baibin boro bai’obaibiyenayah hinamatar naatu men orot isah hini’ukwarin, baise baibin i awah nafot hinanutanubamo hinama.
13 Pakuti Adamu ndiye anayamba kupangidwa kenaka Hava.
13 Anayabin God i wantoro’ot Adam sinaf matar, imaibo Eve sinaf matar.
14 Ndipo Adamu si amene ananyengedwa koma mkazi ndiye amene ananyengedwa nachimwa.
14 Naatu Adam i men wan hikubibiruwimih baise babin i wan hikubibiruw naatu bowabow kakafin sinaf.
15 Ndipo mkazi adzapulumutsidwa pobereka mwana ngati apitiriza kukhala mʼchikhulupiriro, mʼchikondi ndi mʼkuyera mtima pamodzi ndi kudzichepetsa konse.
15 Baise baibin hai toub ana maramaim God boro nibaisih yawas nitih, nati i baitumatum, yabow naatu kakafiyinamaim hinabukikin hinama gewasin hinasisinaf na’at.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Timóteo 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.