Salmos 108

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu;

2 Dzukani, zeze ndi pangwe!

3 Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;

4 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba;

5 Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,

6 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja

7 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:

8 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;

9 Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo

10 Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa?

11 Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana

12 Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani,

13 Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 108, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.