Mateus 22

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs VC

Sair da comparação
VC Versão Católica
1 Yesu anayankhula nawonso mʼmafanizo, nati,
1 Jesus tornou a falar-lhes por meio de parábolas:
2 “Ufumu wakumwamba uli ngati mfumu imene inakonzera phwando mwana wake wamwamuna.
2 The kingdom of the heavens has become like a king who made a wedding feast for his son,
3 Anatumiza antchito ake kwa amene anayitanidwa kuphwando koma anakana kubwera.
3 and sent his bondmen to call the persons invited to the wedding feast, and they would not come.
4 “Kenaka anatumiza antchito ena nati, ‘Awuzeni oyitanidwa kuti phwando lakonzedwa: ndapha ngʼombe yayimuna ndi nyama zina zonenepa ndipo zonse zakonzedwa. Bwerani ku phwando laukwati.’
4 Again he sent other bondmen, saying, Say to the persons invited, Behold, I have prepared my dinner; my oxen and my fatted beasts are killed, and all things ready; come to the wedding feast.
5 “Koma iwo sanalabadire ndipo anachoka; wina anapita ku munda wake ndi wina ku malonda ake.
5 But they made light of it, and went, one to his own land, and another to his commerce.
6 Ndipo otsalawo anagwira antchito ake, nawazunza ndi kuwapha.
6 And the rest, laying hold of his bondmen, ill-treated and slew {them}.
7 Mfumu inakwiya. Inatumiza asilikali ake ndipo anawononga opha anzawowo ndi kutentha mzinda wawo.
7 And {when} the king {heard of it he} was wroth, and having sent his forces, destroyed those murderers and burned their city.
8 “Pamenepo anati kwa antchito ake, ‘Phwando laukwati lakonzedwa, koma amene ndinawayitana sanali oyenera.
8 Then he says to his bondmen, The wedding feast is ready, but those invited were not worthy;
9 Pitani ku mphambano za misewu ndipo kayitaneni aliyense amene mukamupeze kuti abwere ku phwando.’
9 go therefore into the thoroughfares of the highways, and as many as ye shall find invite to the wedding feast.
10 Pamenepo antchitowo anapita ku misewu nakasonkhanitsa anthu onse amene anakawapeza, abwino ndi oyipa omwe, ndipo nyumba ya madyerero inadzaza ndi oyitanidwa.
10 And those bondmen went out into the highways, and brought together all as many as they found, both evil and good; and the wedding feast was furnished with guests.
11 “Koma pamene mfumu inabwera kudzaona oyitanidwawo, inaona munthu amene sanavale zovala zaukwati.
11 And the king, having gone in to see the guests, beheld there a man not clothed with a wedding garment.
12 Inamufunsa kuti, ‘Bwenzi walowa bwanji muno wopanda zovala zaukwati?’ Munthuyo anakhala chete.
12 And he says to him, {My} friend, how camest thou in here not having on a wedding garment? But he was speechless.
13 “Pamenepo mfumuyo inawuza otumikira kuti, ‘Mʼmangeni manja ndi miyendo, ndipo muponyeni kunja, ku mdima kumene kudzakhale kulira ndi kukuta mano.’
13 Then said the king to the servants, Bind him feet and hands, and take him away, and cast him out into the outer darkness: there shall be the weeping and the gnashing of teeth.
14 “Popeza oyitanidwa ndi ambiri koma osankhidwa ndi ochepa.”
14 For many are called ones, but few chosen ones.
15 Kenaka Afarisi anatuluka nakakonza njira zomupezera zifukwa Yesu mʼmawu ake.
15 — ausente —
16 Anatumiza ophunzira awo kwa Iye pamodzi ndi Aherodia. Anati, “Aphunzitsi, tidziwa kuti ndinu wangwiro ndi kuti mumaphunzitsa mawu a Mulungu monga mwa choonadi. Simutekeseka ndi anthu, popeza simusamala kuti kodi ndi ndani?
16 And they send out to him their disciples with the Herodians, saying, Teacher, we know that thou art true and teachest the way of God in truth, and carest not for any one, for thou regardest not men's person;
17 Tiwuzeni tsono maganizo anu ndi otani, kodi nʼkololedwa kupereka msonkho kwa Kaisara kapena ayi?”
17 tell us therefore what thou thinkest: Is it lawful to give tribute to Caesar, or not?
18 Koma Yesu podziwa maganizo awo oyipa anati, “Inu achiphamaso, bwanji mufuna kundipezera chifukwa?
18 But Jesus, knowing their wickedness, said, Why tempt ye me, hypocrites?
19 Onetseni ndalama imene mumapereka msonkho.” Iwo anabweretsa dinari,
19 Shew me the money of the tribute. And they presented to him a denarius.
20 ndipo anawafunsa kuti, “Kodi chithunzi ichi ndi malemba awa ndi za ndani?”
20 And he says to them, Whose {is} this image and superscription?
21 Iwo anayankha kuti, “Ndi za Kaisara.”
21 They say to him, Caesar's. Then he says to them, Pay then what is Caesar's to Caesar, and what is God's to God.
22 Atamva izi, anadabwa, ndipo anamusiya Iye, nachoka.
22 And when they heard {him}, they wondered, and left him, and went away.
23 Tsiku lomwelo Asaduki amene amati kulibe za kuukanso, anabwera kwa Iye ndi funso.
23 — ausente —
24 Iwo anati, “Aphunzitsi, Mose anatiwuza kuti munthu akamwalira wosasiya ana, mʼbale wake akuyenera kukwatira mkazi wamasiyeyo kuti amuberekere ana mʼbale wakeyo.
24 saying, Teacher, Moses said, If any one die, not having children, his brother shall marry his wife and shall raise up seed to his brother.
25 Tsopano panali abale asanu ndi awiri pakati pathu. Woyambayo anakwatira ndipo anamwalira, ndipo popeza analibe ana, mʼbale wake analowa chokolo.
25 Now there were with us seven brethren; and the first having married died, and not having seed, left his wife to his brother.
26 Izi zinachitikiranso mʼbale wa chiwiri ndi wachitatu mpaka wachisanu ndi chiwiri.
26 In like manner also the second and the third, unto the seven.
27 Pa mapeto pake mkaziyo anamwaliranso.
27 And last of all the woman also died.
28 Tsopano, kodi akadzaukitsidwa adzakhala mkazi wa ndani mwa asanu ndi awiriwa popeza aliyense anamukwatirapo?”
28 In the resurrection therefore of which of the seven shall she be wife, for all had her?
29 Yesu anayankha kuti, “Inu mukulakwitsa chifukwa simukudziwa malemba kapena mphamvu ya Mulungu.
29 And Jesus answering said to them, Ye err, not knowing the scriptures nor the power of God.
30 Anthu akadzaukitsidwa, sadzakwatira kapena kukwatiwa; adzakhala ngati angelo kumwamba.
30 For in the resurrection they neither marry nor are given in marriage, but are as angels of God in heaven.
31 Koma za kuukitsidwa kwa akufa, kodi simunawerenge zimene Mulungu ananena kwa inu kuti,
31 Quanto à ressurreição dos mortos, não lestes o que Deus vos disse:
32 ‘Ine ndine Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isake ndi Mulungu wa Yakobo?’ Iyeyo si Mulungu wa akufa koma wa amoyo.”
32 Eu sou o Deus de Abraão, o Deus de Isaac e o Deus de Jacó {Ex 3,6}? Ora, ele não é Deus dos mortos, mas Deus dos vivos.
33 Magulu a anthu atamva zimenezi, anazizwa ndi chiphunzitso chake.
33 E, ouvindo esta doutrina, as turbas se enchiam de grande admiração.
34 Pakumva kuti Yesu anawakhalitsa chete Asaduki, Afarisi anasonkhana pamodzi.
34 Sabendo os fariseus que Jesus reduzira ao silêncio os saduceus, reuniram-se
35 Mmodzi wa iwo, katswiri wa malamulo anamuyesa Iye ndi funso ndipo anati,
35 e um deles, doutor da lei, fez-lhe esta pergunta para pô-lo à prova:
36 “Aphunzitsi, kodi lamulo lalikulu koposa mu malamulo ndi liti?”
36 Mestre, qual é o maior mandamento da lei?
37 Yesu anayankha kuti, “Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse ndi moyo wako wonse ndi nzeru zako zonse.
37 Respondeu Jesus: Amarás o Senhor teu Deus de todo teu coração, de toda tua alma e de todo teu espírito {Dt 6,5}.
38 Ili ndi lamulo loyamba ndi loposa onse.
38 Este é o maior e o primeiro mandamento.
39 Ndipo lachiwiri ndi lofanana nalo: ‘Konda mnansi wako monga iwe mwini.’
39 E o segundo, semelhante a este, é: Amarás teu próximo como a ti mesmo {Lv 19,18}.
40 Malamulo onse ndi aneneri zakhazikika pa malamulo awiriwa.”
40 Nesses dois mandamentos se resumem toda a lei e os profetas.
41 Afarisi atasonkhana pamodzi, Yesu anawafunsa kuti,
41 Como os fariseus se agrupassem, Jesus interrogou-os:
42 “Kodi mukuganiza bwanji za Khristu? Ndi Mwana wa ndani?”
42 Que pensais vós de Cristo? De quem é filho? Responderam: De Davi!
43 Iye anawawuza kuti, “Nanga zikutheka bwanji kuti Davide poyankhula mwa Mzimu Woyera amatchula Iye ‘Ambuye?’ Pakuti akuti,
43 Como então, prosseguiu Jesus, Davi, falando sob inspiração do Espírito, chama-o Senhor, dizendo:
44 “Ambuye anati kwa Ambuye wanga:
44 O Senhor disse a meu Senhor: Senta-te à minha direita, até que eu ponha teus inimigos por escabelo dos teus pés {Sl 109,1}?
45 Ngati tsono Davide amamutchula ‘Ambuye,’ zingatheke bwanji kukhala mwana wake?”
45 Se, pois, Davi o chama Senhor, como é ele seu filho?
46 Panalibe wina anatha kuyankha, ndipo kuchokera pamenepo, panalibe wina anayerekeza kumufunsa funso.
46 Ninguém pôde responder-lhe nada. E, depois daquele dia, ninguém mais ousou interrogá-lo.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Mateus 22, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.