Isaías 60

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 “Dzuka, wala, pakuti kuwala kwako kwafika,

2 Taona, mdima waphimba dziko lapansi

3 Mitundu ya anthu idzatsata kuwunika kwako

4 “Tukula maso ako, yangʼanayangʼana ndipo ona zimene zikuchitika.

5 Ukadzaona zimenezi udzasangalala kwambiri,

6 Gulu la ngamira lidzaphimba dziko lako,

7 Ziweto zonse za ku Kedara adzazisonkhanitsa kwa inu,

8 “Kodi ndi zayani izo zikuwuluka ngati mitambo,

9 Ndithu, izi ndi sitima za pa madzi zochokera ku mayiko akutali;

10 “Alendo adzamanganso malinga ako,

11 Zipata zako zidzakhala zotsekula nthawi zonse,

12 Pakuti mtundu wa anthu ndi mafumu amene sakutumikira iwe;

13 “Adzabwera nayo kwa iwe mitengo ya payini,

14 Ana aja amene anakuzunzani adzabwera ndipo adzakugwadirani;

15 “Ngakhale anthu anakusiya nadana nawe,

16 Udzamwa mkaka wa mitundu ya anthu

17 Ndidzakupatsa golide mʼmalo mwa mkuwa,

18 Ziwawa sizidzamvekanso mʼdziko lako,

19 Sipadzakhala dzuwa kuti likuwunikire,

20 Dzuwa lako silidzalowanso,

21 Ndipo anthu ako onse adzakhala olungama

22 Kabanja kakangʼono kadzasanduka fuko,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 60, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.