Isaías 61

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine,

2 Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;

3 Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,

4 Adzamanganso mabwinja akale a mzinda

5 Anthu achilendo adzakutumikirani; adzazidyetsa ziweto zanu;

6 Ndipo inu mudzatchedwa ansembe a Yehova,

7 Chifukwa manyazi awo anali owirikiza;

8 “Pakuti Ine Yehova, ndimakonda chilungamo;

9 Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu

10 Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;

11 Monga momwe nthaka imameretsa mbewu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 61, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.