Isaías 54

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 “Sangalala, iwe mayi wosabala,

2 Kulitsa malo omangapo tenti yako,

3 Pakuti udzasendeza malire ako kumanja ndi kumanzere;

4 “Usachite mantha; sadzakunyozanso.

5 Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako,

6 Yehova wakuyitananso,

7 “Kwa kanthawi kochepa, Ine ndinakusiya,

8 Ndinakufulatira kwa kanthawi kochepa

9 “Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa.

10 Ngakhale mapiri atagwedezeka

11 “Iwe mzinda wozunzika, wokunthidwa ndi namondwe ndiponso wopanda wokutonthoza,

12 Ndidzamanga nsanja zako zankhondo ndi miyala yokongola ya rubi.

13 Yehova adzaphunzitsa ana ako onse,

14 Udzakhazikika mʼchilungamo chenicheni:

15 Ngati wina adzakuthirani nkhondo, si ndine amene ndachititsa;

16 “Taona, ndi Ine amene ndinalenga munthu wosula zitsulo

17 palibe chida chopangidwa ndi mdani chimene chidzakupweteke,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 54, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.