Isaías 53

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Ndani wakhulupirira zimene tanenazi;

2 Iye anakula ngati mphukira pamaso pake,

3 Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu,

4 Ndithudi, iye anamva zowawa mʼmalo mwa ife;

5 Koma iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu,

6 Ife tonse, ngati nkhosa, tasochera,

7 Anthu anamuzunza ndi kumusautsa,

8 Atatha kumugwira mwankhanza ndikumuyimba mlandu, kenaka anapita naye kukamupha.

9 Anamukonzera manda ake pamodzi ndi anthu oyipa

10 Komatu ndi Yehova amene anafuna kuti amuzunze ndi kumusautsa.

11 Atatha mazunzo a moyo wake,

12 Motero Ine ndidzamupatsa ulemu pamodzi ndi akuluakulu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 53, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.