Filemom 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kuchokera kwa Paulo, amene ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu ndi Timoteyo mʼbale wathu.
1 Ayu Paul, Keriso Jesu wabinamaim ana dibur ama abowabow, Tai Timothy airi akirum,
2 Kwa Apiya mlongo wathu, Arkipo msilikali mnzathu, ndiponso mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwanu.
2 naatu rubui baitumatumayan babin Aphia auman ana merar ayiy, na’atube Arsipas ata of tur gewasin isan etatafafar, naatu ekaleisia nati abaremaim etei hai merar ayiyi.
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale ndi inu.
3 Manaw kabeber naatu tufuw Tamat Godane naatu ata Regah Jesu Keriso’one kwa etei isa nama.
4 Ine ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakukumbukira iwe mʼmapemphero anga.
4 Philemon, matan fufur au yoyobanamaim o anunuhi, naatu au God ana merar ayiy.
5 Pakuti ndamva za chikondi chako, za chikhulupiriro chako mwa Ambuye Yesu ndiponso za chikondi chako pa oyera mtima onse.
5 Anayabin o God ana sabuw isah kubiyabow naatu a baitumatum Regah Jesu wanawananamaim ibukikin kuma’am isan ana tur i anonowar.
6 Ine ndikupemphera kuti mgwirizano wako ndi ife mʼchikhulupiriro ukhale opindulitsa pozamitsa nzeru zako zozindikira zinthu zilizonse zabwino zimene timagawana chifukwa cha Khristu.
6 Ayu ayoyoyoban o a bowabow nati kubowabow i nigewasin inabow, saise sawar gewasih Keriso wanawananamaim tenan hai yabih etei boro inaso’ob.
7 Mʼbale, chikondi chako chandipatsa chimwemwe chachikulu ndi chilimbikitso, chifukwa umatsitsimutsa mitima ya anthu a Ambuye.
7 O a yabowamaim ayu yasisir gagamin na’in itu naatu koufair itu, anayabin o asinafumaim God ana sabuw dogoroh ibora’ah maiye.
8 Tsopano ngakhale kuti mwa Khristu nditha kulimba mtima ndi kulamulira kuti uchite zimene uyenera kuchita,
8 Isan imih ayu Keriso wabinamaim tur fokarin ata’uwi naatu atiyuni sawar abisa sinafumih itasinaf.
9 komabe ndikupempha mwachikondi. Ine Paulo, munthu wokalamba, ndipo tsopano ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu,
9 Baise yabow ana efamaim o abifefeyani, ayu Paul, naatu ayu i regah, na’atube Keriso Jesu abibinanumaim dibur ama’am.
10 ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga Onesimo, amene ndamubala ndili mu unyolo.
10 Ayu o isa ao abifefeyan natu Onesimus isan, ayu dibur ama’am ana veya i na ayu natu matar, Paul ma Onesmuis ana fef ekikirum|alt="Paul with paper, pen and Onesimus" src="CN02091B.TIF" size="span" loc="Phm 10" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="10"
11 Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso.
11 Onesimus marasika airi kwama’am i ana bowabow isan i’it furuw, baise boun i orot bowayan orot gewasin matar, boro o nibaisi na’atube ayu nibaisu.
12 Ine ndikumutumizanso kwa iwe tsopano, koma potero ndikukhala ngati ndikutumiza mtima wanga weniweni.
12 O isa abiyafar maiye, ana itinin i ayu dogorou o isa enan.
13 Ndikanakonda ndikanakhala naye kuno kuti iyeyo azinditumikira mʼmalo mwako pamene ndili mu unyolo chifukwa cha Uthenga Wabwino.
13 Ayu akokok kwanekwan i boro atabotan, ayu tur gewasin isan dibur ama’am i boro o efan ayu tibaisu ata ma.
14 Koma sindikufuna kuchita kanthu osakufunsa, nʼcholinga chakuti chilichonse chabwino ungandichitire chikhale mwakufuna kwako osati mokakamiza.
14 Baise ayu men akokok o a baibasit ufunane atasinaf, en baise wan i boro o dogor tutufin etei inibasit, saise men inanot ayu o sinaf isan ao’okikinimih.
15 Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse.
15 Ana’an ta Onesimus o biyamaim tit nabin mar kafai ma, saise tamatabir tan biya tatitit boro airi wanatowan kwatama.
16 Osati ngati kapolo, koma woposa kapolo, ngati mʼbale wokondedwa. Iyeyu ndi wokondedwa kwambiri kwa ine koma kwa iweyo ndi wokondedwa koposa, ngati munthu komanso ngati mʼbale mwa Ambuye.
16 Naatu boun i men bowayan akisin, en baise bowayan gewasin anababatun matar, tai baitumatumayan, ayu dogorou ana yasisir, naatu o dogor ana yasisir gagamin anababatun. Bowayan orot gewasin o isa naatu ata Regah isan.
17 Tsono ngati umati ndine mnzako, umulandire iyeyu monga momwe ukanandilandirira ineyo.
17 Imih ayu o bow turau inarouw inanotanot na’at, basit ana merar inay inab. Ayu au merar itay itabubuwu na’atube.
18 Ngati anakulakwira kapena kukongola kanthu kalikonse, ndidzalipira ineyo.
18 O isa sawar kakafin ta nasisinaf na’at, o sawar ta asir nab men nabibaiyan na’at, basit i wabin inabosair ayu wabu’umaim inakirum, boro anibaiyan.
19 Ine, Paulo ndikulemba zimenezi ndi dzanja langa. Ine ndidzalipira. Nʼkosafunika kukukumbutsa kuti iweyo ngongole yako kwa ine ndi moyo wakowo.
19 Ayu Paul iti tur i ayu taiyuwu umau’umaim akirum abiyafar. Ayu boro wan anay anibaiyan. Iti i boro men atao itanowar, en baise o ayawas tutufin etei ayu isou ibowabow ana bit i biyou ema’am.
20 Mʼbale, ndikufuna kuti ndipindule nawe mwa Ambuye; tsono tsitsimutsa mtima wanga mwa Khristu.
20 Taiu, baitumatumayan akokok ata Regah Keriso wabinamaim mi’itube o biyane baibais ta atab, Keriso wanawananamaim dogorou itakumamat koufair atab.
21 Ine ndili ndi chitsimikizo cha kumvera kwako pamene ndikukulembera kalatayi. Ndikulemba ndikudziwa kuti udzachita ngakhale kuposa zimene ndakupemphazi.
21 O abosiyasiyar isan i ayu abitumatum, naatu fef iti akirum o isa abiyafar, aso’ob o boro abisa ao tafanamaim inasinaf.
22 Chinthu chinanso ndi ichi: undikonzere malo, chifukwa ndikukhulupirira kuti Mulungu adzamvera mapemphero anu ndi kundibwezera kwa inu.
22 Naatu akokok nanawan bar awan ta ayu isou inayabuna, anayabin ayu abitumatum God boro a yoyoban nanowar, naatu boro niyunu isa anan maiye.
23 Epafra, wamʼndende mnzanga chifukwa cha Khristu Yesu akupereka moni.
23 Epaphras a merar eyiy, i ayu airi Keriso Jesu wabinamaim dibur ama’am.
24 Atumiki anzanga awa, Marko, Aristariko, Dema ndi Luka, akuperekanso moni.
24 Au ofonah bairi ai bowabow ta’imon etei’imak a merar tiyiy na’atube, Mark, Aristakus, Demas naatu Luke.
25 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wako.
25 Ata Regah Jesu Keriso ana manaw ana kabeber wanawanamaim bairi kwanama.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Filemom 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.