1 João 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs MNT
1 Tikukulalikirani za Mawu a moyo amene analipo kuyambira pachiyambi, amene tinawamva, amene tinawaona ndi maso athu, amene tinawapenyetsetsa, ndipo tinawakhudza ndi manja athu.
1 Yawas ana tur anamaim ma’am na tit a’itin, matai yan a’itin biyan abutubun naatu eo fanan anowar.
2 Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife.
2 Iti yawas na birerereb i aki a’itin, imih aorereb kwa a tur ao’owen, iti yawas wanatowan i Tamat God hairi hima’am na aki isai irerereb.
3 Tikukulalikirani chimene tinachiona ndi kumva, kuti inuyo muyanjane nafe. Kuyanjana kwathu, tikuyanjana ndi Atate ndiponso ndi Mwana wawo, Yesu Khristu.
3 Abisa a’itin anonowar, i ao’orereb kwa auman kwananowar, saise aki Tamat Natun Jesu Keriso bairi abita’ayomaim kwanarun kwanikofani tanita’ay.
4 Tikukulemberani zimenezi kuti chimwemwe chathu chikhale chathunthu.
4 Iti tur akikirum saise aki ai yasisir nan yomanin na’asa’ub.
5 Uthenga umene tinamva kwa Iye ndipo tikuwulalikira kwa inu ndi uwu: Mulungu ndiye kuwunika ndipo mwa Iye mulibe mdima konse.
5 Tur God Natun biyanane anonowar i iti ao’orereb kwananowar. God i marakaw, i biyanamaim men kafai’imo gugumin ta ema’ama’amih.
6 Tikanena kuti timayanjana naye, koma nʼkumayendabe mu mdima, tikunama ndipo sitikuchita choonadi.
6 Awatamaim ta’orereb it i God bairi tabita’ay, baise ata yawasamaimi gugumin wanawanan tama’am,it i baifuwenayah naatu men turobe’emaim tama’am.
7 Koma tikamayenda mʼkuwunika, monga Iye ali mʼkuwunika, pamenepo timayanjana wina ndi mnzake, ndipo magazi a Yesu, Mwana wake, amatitsuka ndi kutichotsera tchimo lililonse.
7 Baise i marakawinamaim ema’am na’atube it marakawinamaim tanama’am, boro taituwat bairi tanita’ay gewas, naatu i Natun Jesu Keriso ana rara’amaim ata bowabow kakafih etei boro nakusouwen.
8 Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi.
8 It aurit bowabow kakafih en tanarouw tanayayaub, i taiyuwit tabifufuwit naatu wanawanat men turobe ema’am.
9 Koma tikavomereza machimo athu, Iye ndi wokhulupirika ndi wolungama ndipo adzatikhululukira machimo athu, nadzatiyeretsa ndi kutichotsera chosalungama chilichonse.
9 Baise God matanamaim ata bowabow kakafih tana’e’en i boro ana omatanen nakaif gewasin nasinaf, ata kakafih boro nanotawiyen naatu ata sinaf kakafihine boro nakusouwit.
10 Ife tikanena kuti sitinachimwe, tikumutenga Mulungu kukhala wonama, ndipo Mawu ake sali mwa ife.
10 Baise it aurit bowabow kakafih en tanarouw tanao’o na’at, nati i tasinaf God baifufuwenayan emamatar. Naatu i ana tur wanawanatamaim ana efan men ema’am.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 João 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.