1 João 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Tikukulalikirani za Mawu a moyo amene analipo kuyambira pachiyambi, amene tinawamva, amene tinawaona ndi maso athu, amene tinawapenyetsetsa, ndipo tinawakhudza ndi manja athu.
1 Yawas ana tur anamaim ma’am na tit a’itin, matai yan a’itin biyan abutubun naatu eo fanan anowar.
2 Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife.
2 Iti yawas na birerereb i aki a’itin, imih aorereb kwa a tur ao’owen, iti yawas wanatowan i Tamat God hairi hima’am na aki isai irerereb.
3 Tikukulalikirani chimene tinachiona ndi kumva, kuti inuyo muyanjane nafe. Kuyanjana kwathu, tikuyanjana ndi Atate ndiponso ndi Mwana wawo, Yesu Khristu.
3 Abisa a’itin anonowar, i ao’orereb kwa auman kwananowar, saise aki Tamat Natun Jesu Keriso bairi abita’ayomaim kwanarun kwanikofani tanita’ay.
4 Tikukulemberani zimenezi kuti chimwemwe chathu chikhale chathunthu.
4 Iti tur akikirum saise aki ai yasisir nan yomanin na’asa’ub.
5 Uthenga umene tinamva kwa Iye ndipo tikuwulalikira kwa inu ndi uwu: Mulungu ndiye kuwunika ndipo mwa Iye mulibe mdima konse.
5 Tur God Natun biyanane anonowar i iti ao’orereb kwananowar. God i marakaw, i biyanamaim men kafai’imo gugumin ta ema’ama’amih.
6 Tikanena kuti timayanjana naye, koma nʼkumayendabe mu mdima, tikunama ndipo sitikuchita choonadi.
6 Awatamaim ta’orereb it i God bairi tabita’ay, baise ata yawasamaim i gugumin wanawanan tama’am, it i baifuwenayah naatu men turobe’emaim tama’am.
7 Koma tikamayenda mʼkuwunika, monga Iye ali mʼkuwunika, pamenepo timayanjana wina ndi mnzake, ndipo magazi a Yesu, Mwana wake, amatitsuka ndi kutichotsera tchimo lililonse.
7 Baise i marakawinamaim ema’am na’atube it marakawinamaim tanama’am, boro taituwat bairi tanita’ay gewas, naatu i Natun Jesu Keriso ana rara’amaim ata bowabow kakafih etei boro nakusouwen.
8 Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi.
8 It aurit bowabow kakafih en tanarouw tanayayaub, i taiyuwit tabifufuwit naatu wanawanat men turobe ema’am.
9 Koma tikavomereza machimo athu, Iye ndi wokhulupirika ndi wolungama ndipo adzatikhululukira machimo athu, nadzatiyeretsa ndi kutichotsera chosalungama chilichonse.
9 Baise God matanamaim ata bowabow kakafih tana’e’en i boro ana omatanen nakaif gewasin nasinaf, ata kakafih boro nanotawiyen naatu ata sinaf kakafihine boro nakusouwit. Tanabat kikin men au’uf tanabat|alt="may have confidence and not stink away" src="BA03015.tif" size="col" loc="1Jn 1.9" copy="Illustration is used by permission of Louise Bass." ref="1.9"
10 Ife tikanena kuti sitinachimwe, tikumutenga Mulungu kukhala wonama, ndipo Mawu ake sali mwa ife.
10 Baise it aurit bowabow kakafih en tanarouw tanao’o na’at, nati i tasinaf God baifufuwenayan emamatar. Naatu i ana tur wanawanatamaim ana efan men ema’am.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 João 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.