Tito 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Uwakumbutse anthu kuti azigonjera oweruza ndi olamulira, aziwamvera ndi kukhala okonzeka kuchita chilichonse chabwino.
1 Hai not inakusib sabuw iyab hi’ukwarin tebobonawiyih babahimaim hinama, hinifanabow, bowabow etei isah hinanowarasit hinabow gewas.
2 Asamachitire chipongwe aliyense, asamakangane, akhale ofatsa ndipo oganizira ena, ndipo nthawi zonse akhale aulemu kwa anthu onse.
2 Men yait ta isan tur kakafin hinao, baise dogoroh wanawanan tufuw nama, gamin kwanekwan hinahaiw, taiyuwih hinayara’iyih taituwah bairi hinibegon gewas hinama naatu kakaf sabuw hini’obaiyih.
3 Nthawi ina tinali opusa, osamvera, onamizidwa ndi omangidwa ndi zilakolako ndi zokondweretsa zamitundumitundu. Tinkakhala moyo wadumbo ndi wakaduka, odedwa ndiponso odana wina ndi mnzake.
3 Anayabin it auman marasika nati na’atube ata not hikwaris, tabifanasair, hibifufuwit, sawar kakafih yumatah ta ta biyat ana yasisir isan fatumit, kakafin wanawanan tama’am, tabahiy kwanekwan, dogorot wanawanan baifa’efa’en awan karatan, naatu taiyuwit nena taifa’ifa’it.
4 Koma kukoma mtima ndi chikondi cha Mulungu Mpulumutsi wathu chitaonekera,
4 Baise God ata baiyawasenayan ana kabeber naatu ana yabow yara’iy na birerereb ana maramaim
5 Iye anatipulumutsa, osati chifukwa cha ntchito zathu zolungama zimene tinachita koma chifukwa cha chifundo chake. Anatipulumutsa potisambitsa, kutibadwitsa kwatsopano ndi kutikonzanso mwa Mzimu Woyera
5 ata kakafihine iyawasit. Men bowabow gewasin tasisinaf isan iyawasitamih, baise i ana kabeberamaim yawas itit harewamaim ikifuwit tatufuw maiye. Naatu Anun Kakafiyinamaim ata yawas iwa’an boubun matar.
6 amene anatipatsa mowolowamanja kudzera mwa Yesu Khristu Mpulumutsi wathu,
6 Iti baitinin gewasin maiyow tafatamaim isuwai re ata baiyawasenayan Jesu Keriso wanawananamaim.
7 kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha.
7 Saise bosiyasiyaramaim tayamutufurit tanan i nowan tatamatar ma’ama wanatowan isan nuhit tafot tatama.
8 Mawuwa ndi okhulupirika ndipo ine ndikufuna kuti iwe utsindike zinthu izi, kuti amene akhulupirira Mulungu adzipereke kuchita ntchito zabwino. Zinthu izi ndi zabwino kwambiri ndi zopindulitsa kwa aliyense.
8 Tur etei au’uwi i turobe anababatun, ayu akokok inakubuna gewas, saise sabuw God tibitumitum hinakakaf bowabow gewasin hinasinaf. Sawar iti etei i gewasih naatu orot babin etei boro hai ma gewasin nitih;
9 Koma upewe kufufuzafufuza zopusa, kuwerengawerenga mndandanda wa mibado ya makolo, mikangano ndi mitsutso pa za Malamulo, chifukwa zimenezi ndi zosapindulitsa ndi zopanda pake.
9 baise ofafar isah baikoko’aw obosabosa, ginyow naatu gamin baiyow i kwanahaiw, anayabin nati sawar i hai yabin en orot babin hai ma boro ni’afiy.
10 Munthu woyambitsa mipatuko umuchenjeze koyamba, ndiponso umuchenjeze kachiwiri. Kenaka umupewe.
10 Kou’obo’obowayan orot wantoro’ot kwanimatanuw, naatu bairou’abin iban kwanimatanuw maiye, nati ufunamaim kwanahaiw.
11 Iwe udziwe kuti munthu wotero ngosokoneza ndi wochimwa, ndipo akudzitsutsa yekha.
11 O iso’obaka nati orot i ikwaris naatu taiyuwin ana kakafinamaim ubar itin.
12 Ndikadzamutuma Artema kapena Tukiko kwanuko, udzayesetse kundipeza ku Nikapoli, chifukwa ndatsimikiza kukhala kumeneko pa nthawi yozizira.
12 Artemas o Tychicus o isa aniyafar nan biya natitit ana mar, saife’ewat a ef inanuwet inan Nicopolis imaim ana ma’am biyau inatit. Anayabin ayu au not abogaigiwas yakukur ana veya boro nati’imaim anama.
13 Uyesetse chilichonse ungathe kuthandiza Zena katswiri wa malamulo ndi Apolo, kuti apitirize ulendo wawo, ndipo uwonetsetse asasowe kanthu.
13 Zenas, ofafar so’obayan naatu Apollos hairi hai ef remor isan sawar etei ana fofonin inibaisih saise hinanan efamaim men sawar ta isan hiniyababan.
14 Anthu athu aphunzire kudzipereka pogwira ntchito zabwino, nʼcholinga chakuti athandize zinthu zimene zikufunika msangamsanga. Ndipo asakhale moyo osapindulitsa.
14 Naatu ata sabuw hiyasairih bowabow gewasin sinaf isan ana ef hinaso’ob naatu hinan baibaisayah gewasih hinamatar, saise hai yawas men nan ro’on en namataramih.
15 Onse amene ali ndi ine akupereka moni. Upereke moni kwa amene amatikonda ife mʼchikhulupiriro.
15 Au tur yomanin, sabuw iyab iti bairi ama’am a merar teyiy. Naatu sabuw iyab bairit ata baitumatum ta’imon tibiyabuwit hai merar ayiy. Manaw kabeber kwa etei isan nama.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Tito 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.