Tito 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ndine Paulo, mtumiki wa Mulungu, ndi mtumwi wa Yesu Khristu. Ndinatumidwa kuti nditsogolere amene Mulungu anawasankha ku chikhulupiriro ndi ku chidziwitso cha choonadi chimene chimawafikitsa ku moyo wolemekeza Mulungu
1 Ayu Paul God ana akirwairafin naatu Jesu Keriso ana tur abarayan. Baitumatum, turobe ana so’ob bonawiyit God ana efamaim ma, naatu God ana roubinen sabuw baibaisih hai baitumatum baira’atin isan yasairu.
2 ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe.
2 Naatu it ata nuhifot i yawas wanatowan tafanamaim ebitutut. Anayabin turobe ana God tafaram matara’e ana veya ana omatanen yai.
3 Pa nthawi yake Mulungu, Mpulumutsi wathu anawulula poyera mawu ake ndipo analamula kuti ndipatsidwe udindo wolalikira uthengawu.
3 Taiyuwin ana veya yakitifuw inu’in baib ana maramaim ana tur iwa’an irerereb ayu abibinan wanawanan. Iti obaiyunen tur i God ata baiyawasenayan ayu itutumu itu.
4 Kwa Tito, mwana wanga weniweni mʼchikhulupiriro cha ife tonse:
4 Titus o ayu natu anababatun baitumatum ta’imon wanawananamaim. Isa ayoyoyoban Tamat God naatu Jesu Keriso ata baiyawasenayan manaw kabeber, tufuw nit.
5 Ndinakusiya ku Krete kuti ulongosole zonse zimene ndinazisiya zisanathe ndiponso usankhe akulu ampingo mʼmizinda yonse, monga momwe ndinakulamulira.
5 Ana’an iti isan o aihamiy Kurit kuma’am saise abistanawat men tabisawaren o inayabuna naatu marisika au’uwi na’atube bar merar ta’ita’imon hai ukwarih inarubiniyih.
6 Mkulu wampingo akhale munthu wopanda cholakwa, akhale wa mkazi mmodzi yekha, munthu amene ana ake ndi okhulupirira, osati amakhalidwe oyipa ndi osamvera.
6 Orot yait aurin ubar en na’at, aawan ta’imon, natunatun bosunusunubayah, men yah so’aso’arin, men baifanasairayah.
7 Popeza mkulu wa mpingo amayendetsa ntchito za banja la Mulungu, ayenera kukhala wopanda cholakwa, asakhale womva zayekha, kapena wopsa mtima msanga, kapena womwa zoledzeretsa, kapena wandewu, kapena wopeza phindu mwachinyengo.
7 Anayabin Orot ukwarin God itumitum bowabow itin ana sabuw kaifih isan, aurin men ubar nama, men taiyuwin na’it ra’ah, men yan so’aso’arin, men harew fokarin tomayan, men fais robayan, naatu men sawar ana kabat.
8 Koma akhale wosamala bwino alendo, wokonda zabwino, wodziretsa, wolungama, woyera mtima ndi wosunga mwambo.
8 Baise orot babin hai merar nay nabuwih, gewasin nasinaf, not wairafin, ana ef mutufurin, naya’asair kakafiyinamaim nama, taiyuwin narumutufur.
9 Iye ayenera kugwiritsa mawu okhulupirika monga tinaphunzitsira, kuti athe kulimbikitsa ena ndi chiphunzitso choona ndiponso kugonjetsa amene atsutsana nacho.
9 Bosunusunub isan ana tur hibi’obaiy na’atube i nabukikin saise nati’imaim tur ana kirikirifotamaim i karam boro fair nab sabuw koufair nitih naatu sabuw iyab tibi’aw’ase’as boro nakwararih.
10 Paja pali anthu ambiri osaweruzika, makamaka mʼgulu la anthu a mdulidwe, oyankhula nkhani zopanda pake ndi kusocheretsa anzawo.
10 Anayabin sabuw maumurih na’in i baifanasairayah, okwanekwaneyah naatu baifufuwenayah, itinin ta sabuw hai ar afu’afuw kwa wanawanamaim tema’am na’atube.
11 Ayenera kuletsedwa kuyankhula chifukwa akusokoneza mabanja athunthu pophunzitsa zinthu zomwe sayenera kuwaphunzitsa. Iwo amachita izi kuti apeze ndalama mwachinyengo.
11 Gewasin nati sabuw awah kwanasakirafut, anayabin bar awan awan hirun hitit baifuwenamaim sabuw tibi’obaiyih, saise nati’imaim i sawar wairafih hinamatar hinama gewas isan.
12 Mneneri wina, mmodzi wa iwo omwewo anati, “Akrete nthawi zonse ndi amabodza, akhalidwe loyipitsitsa ndiponso alesi adyera.”
12 Taiyuwih hai dinab orot iti na’atube hio, “Kurit sabuw i mar etei baifuwenayah, sigarafor, nokonokow yah wiruw.”
13 Mawu amenewa ndi woona. Nʼchifukwa chake, uwadzudzule mwamphamvu, kuti akhale ndi chikhulupiriro choona,
13 Sawar iti isah sif hirurubon i turobe, isan imih tur fokarin kwanakwararih kwana’uwih, saise hai baitumatum nare baron na’of,
14 kuti asasamalenso nthano za Chiyuda, ndi malamulo a anthu amene akukana choonadi.
14 men Jew sabuw hai binanakwar hinanowar naatu men sabuw iyab turobe hikwakwahir hai obaiyunen tur hinanowaramih.
15 Kwa oyera mtima, zinthu zonse ndi zoyera, koma kwa amene ndi odetsedwa ndi osakhulupirira, palibe kanthu koyera. Kunena zoona, mitima yawo ndi chikumbumtima chawo, zonse nʼzodetsedwa.
15 Sabuw iyab tikukubaituturih hai sawar etei boro gewasih, baise sabuw iyab biyah karitanin naatu men tibitumatum hai sawar etei boro men ta gewasin, hai not naatu hai naniyan etei hibokarit.
16 Iwo amati amadziwa Mulungu, pamene ndi zochita zawo amamukana. Ndi anthu onyansa ndi osamvera, ndi osayenera kuchita kalikonse kabwino.
16 Hai turamaim i God hiso’ob, baise hai sinafumaim i God teyayaub, hai yawas tenakuyakuy naatu baifanasairayah, hai fanasair ra’at, hai mumunin sawar men karam boro bowabow gewasin hinasinaf.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Tito 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.