Tiago 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Nʼchiyani chimene chimayambitsa ndewu ndi mapokoso pakati panu? Kodi sizichokera ku zilakolako zimene zimalimbana mʼkati mwanu?
1 Kwa wanawanamaim iti gamin baiyow ana ef i menane na kwagam kwabiyow? Iti sawar etei i kwa a naniyanane enan, biya ana yasisir isan, naatu nati sawar i mar etei wanawanamaim in gamin ekukura’ara’ah.
2 Mumalakalaka zinthu koma simuzipeza, choncho mumapha. Mumasirira zinthu koma simutha kuzipeza zimene mukufuna, choncho mumakangana ndi kumenyana. Mulibe zinthuzo chifukwa simupempha kwa Mulungu.
2 A kok gagamin i sawar kwatabow, baise men kwabowabow. Sabuw kwa’a’asbunubunuw naatu kwababahiy kwanekwan, baise abisa kwakokok men kwabowabow. Naatu abisa men kwabaib isan kwagam kwabiyow, anayabin God men kwabifefeyan.
3 Koma ngakhale mumapempha simulandira, chifukwa mumapempha ndi zolinga zoyipa. Mumapempha kuti muzigwiritse ntchito pa zokusangalatsani nokha.
3 God kwabifefeyan men ibit, anayabin sawar kwa akis a yasisir isan kwakok kwabifefeyan, nati fefeyan i men gewasin.
4 Inu anthu achigololo, kodi simukudziwa kuti kuchita ubwenzi ndi dziko lapansi ndi kudana ndi Mulungu? Choncho, aliyense wosankha kukhala bwenzi la dziko lapansi amasanduka mdani wa Mulungu.
4 Baiwa’an kwanekwaneyah tak! Tafaram bairi kwai’of God ana rakit kwamamatar kwaso’ob ai en? Orot yait tafaram ana of emamatar i taiyuwin iwa’an God ana rakit matar.
5 Kapena mukuganiza kuti Malemba amanena popanda chifukwa kuti Mulungu amafunitsitsa mwansanje mzimu umene Iye anayika kuti uzikhala mwa ife?
5 Men kwananot tur iti Bukamaim eo i yabin en. “God Anun Kakafiyin wanawanatamaim yari’iy ema’am, abisa kakafin tasisinaf isan ana yaso’ar i gagamin maiyow ebaib.
6 Koma amatipatsa chisomo chochuluka. Nʼchifukwa chake Malemba amati,
6 Baise manaw kabeber Godane i gagamin na’in ebitit. Buk Atamaninamaim eo na’atube,
7 Dziperekeni nokha kwa Mulungu. Mukaneni Mdierekezi ndipo adzakuthawani.
7 Isan imih taiyuw God kwanitin. Naatu Demon Mowan kwanarukouw, saise i boro nabihir kwa nihamiyi.
8 Sendezani kufupi ndi Mulungu ndipo Iye adzasendeza kwa inu. Sambani mʼmanja mwanu, inu anthu ochimwa. Yeretsani mitima yanu, inu anthu okayikira.
8 Kwanan God biyanamaim kwaniyubin, i boro nan kwa biyamaim niyubin, kwa i bowabow kakafin wairafi, imih uma kwanasouwen, naatu dogor kwanasouwen, kwa wanawan rerekabih.
9 Chitani chisoni chifukwa cha zimene mwachita, lirani misozi. Kuseka kwanu kusanduke kulira, ndipo chimwemwe chanu chisanduke chisoni.
9 A kakafih isan kwaniyababan, kwanarerey kwana’osmetan, marib keteketef kwanihamiy kwanarerey. Naatu kawasa kwanihamiy kwaniyababan.
10 Dzichepetseni pamaso pa Ambuye ndipo Iye adzakukwezani.
10 Naatu au’uwi maiye Regah nanamaim taiyuw kwanayara’iyi, Regah boro kwa nabora’ahi.
11 Abale musamanenane. Aliyense wonenera zoyipa mʼbale wake kapena kumuweruza, akusinjirira ndi kuweruza Malamulo. Pamene muweruza malamulo, ndiye kuti simukusunga malamulowo, koma mukuwaweruza.
11 Taitu, men asir taiyuw wanawanamaim kwanagam, kwanigigim, kwana’uwi kwanikwaniyimih. O yait Kirisiyan tura isan igam iu naatu kubibabatiy, o i ofafar isan kugamigim naatu kubibabatiy. Imih o kubibatiy ana veya o i men ofafar kubobosiyasiyar, baise ana baibatiyenayan imatar.
12 Pali mmodzi yekha Wopereka Malamulo ndi Woweruza. Ndiye amene akhoza kupulumutsa ndi kuwononga. Kodi ndiwe yani kuti uziweruza mnzako?
12 God akisinamo ofafar ebitit naatu i akisinamo nibatiyit, i akisinamo boro niyawasit naatu i akisinamo boro nagurusit. Baise o a gewasin i men tomar taituwa kubibatiy?
13 Tsono tamverani, inu amene mumati, “Lero kapena mawa tipita ku mzinda wakutiwakuti, tikatha chaka chimodzi tikuchita malonda ndi kupanga ndalama.”
13 Iti ao kwananowar, o yait iti na’at inao, “Boun o maras it boro tanan tafaram ta gagamin, imaim kwamur ta’imon tanama tanabow kabay tanab ata kabay tafan tanaya’abar.”
14 Chifukwa chiyani mukutero? Inu simukudziwa zimene ziti zichitike mawa. Kodi moyo wanu ndi wotani? Inu muli ngati nkhungu imene imangooneka kwa kanthawi kochepa ndipo kenaka ndikuzimirira.
14 Baise maras ayawas isan abisa namamatar o men iso’ob. Kwa i sowasow na’atube, mar auman sowasow i’itin, mar kafai in veya nayey sowasow na’am in.
15 Koma inuyo muyenera kunena kuti, “Ambuye akalola, tikadzakhala ndi moyo, tidzachita zakutizakuti.”
15 Baise ana gewasin kwa iti na’atube kwatao, God nakokok na’at basit tanama sawar iti o ni’i tanasinaf.
16 Koma mmene zililimu mumangodzitama ndi kudzikuza. Kudzitama konse kotereku ndi koyipa.
16 Baise kwa i bai’o’orotoyah naatu ora’ara’atayah, nati a ora’ara’at etei i kakafih.
17 Aliyense amene amadziwa zabwino zimene amayenera kuchita koma osazichita, ndiye kuti wachimwa.
17 Isan imih orot yait sawar gewasin so’ob baise men isisinaf, nati orot i bowabow kakafin isisinaf.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Tiago 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.