Salmos 97

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale;

2 Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira;

3 Moto umapita patsogolo pake

4 Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse;

5 Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova,

6 Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake,

7 Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi,

8 Ziyoni akumva ndipo akukondwera,

9 Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi;

10 Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa

11 Kuwala kumafika pa anthu olungama,

12 Kondwerani mwa Yehova Inu olungama

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 97, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.