Romanos 7
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kodi simukudziwa abale kuti Malamulo ali ndi ulamuliro pa munthu pokhapokha ngati ali ndi moyo? Ine ndikuyankhula kwa anthu amene akudziwa Malamulo.
1 Taitu, abisa isan anao i kwa kwaso’ob, anayabin kwa etei’imak ofafar i kwaso’ob. Ofafar i orot babin yawasin ema’am ana veya i ebobonawiy.
2 Mwachitsanzo, Malamulo amati mkazi wokwatiwa ndi womangidwa ndi lamulo kwa mwamuna wakeyo nthawi yonse pamene mwamuna wakeyo ali moyo. Koma ngati mwamuna wake amwalira, mkaziyo ndi womasulidwa ku lamulo la ukwati.
2 Itinin ta i boro iti na’atube kwana’itin, tautabin babin aawan yawasin ema’ama ana veya ofafaramaim eo’o, nati babin i boro orot biyanamaim nafatum nama. Baise orot namomorob ufunamaim babin i tabin ana ofafarane hirufam.
3 Koma ngati iye akwatiwa ndi mwamuna wina pamene mwamuna wake ali moyo, amatchedwa wachigololo. Koma ngati mwamuna wakeyo amwalira, mkaziyo amasuka ku lamulo ndipo si wachigololo, ngakhale kuti wakwatiwa ndi mwamuna wina.
3 Isan imih babin aawan yawasin ema’am ana veya i orot ta nabi’awan, nati babin i moser kwebayan. Baise orot emomorob ana veya, nati babin i ofafarane tit. Naatu orot ta nabi’awan na’at i men moser kwebayan.
4 Chimodzimodzi inunso, abale anga, munafa ku Malamulo kudzera mʼthupi la Khristu, kuti mukwatiwe ndi wina, ndi Iye amene anauka kwa akufa kuti tibalire Mulungu chipatso.
4 Imih taitu tuwai’inah, ef ta’imon nati na’atube Keriso ana morobomaim baitumatumayah ofafar ana fairane rufamih hitit. Imih i ana misir maiye’emaim baita’ay boubun ana ef imatar, naatu boun morobone God biyawas maiye i nowan kwamatar, saise it bowayah gewasih na’atube God isan tanabow.
5 Pakuti pamene tinkalamulidwa ndi khalidwe lathu lauchimo, zilakolako zauchimo zimene Malamulo anaziwutsa zinkagwira ntchito mʼmatupi mwathu kotero kuti zinabala imfa.
5 Anayabin it taiyuwit biyat ana kok isan tanotanot ana veya, ofafar run biyat ana kok kakafin kura’ara’ah naatu biyat tutufin etei bonawiy in morobomaim yai.
6 Koma tsopano tamasulidwa ku Malamulowo pakuti tinafa ku zimene zinkatimanga, ndipo Mzimu Woyera akutithandiza kutumikira Mulungu mʼnjira yatsopano ndipo osati mʼnjira yakale yolembedwa.
6 Baise boun, it nati ofafar fatumit tamorob ta’inu’in, God nati fatufatumane rufamit tatit. Anun Kakafiyin ana ef boubunamaim tabowabow, men ef atamanin ana ofafar hikirum inu’in tai’ufunun tabowabowamih.
7 Nanga ife tinene chiyani? Kodi Malamulo ndi oyipa? Ayi. Nʼkosatheka! Kunena zoona, popanda Malamulo, ine sindikanazindikira tchimo. Pakuti sindikanadziwa kuti kusirira ndi tchimo ngati Malamulo sakananena kuti, “Usasirire.”
7 Imih ofafar i bowabow kakafin sinafuyan tanarouw tanao? En anababatun! Baise ofafar en na’at ayu au kakafih boro mi’itube ataso’ob. Anayabin ofafar men tama’am na’at ayu boro mi’itube bahiy isan hiofafar ataso’ob.
8 Koma chifukwa cha Malamulo uchimo unapeza mwayi owutsa mʼkati mwanga khalidwe lililonse la kusirira. Pakuti pakanapanda Malamulo, uchimo ukanakhala wopanda mphamvu.
8 Baise bowabow kakafin nati ofafaramaim ana ef tita’ur run ayu wanawana’umaim kura’ara’ah sawar kakafih asisinaf. Ofafar men tama’am na’at, bowabow kakafin i boro ana fair men tama.
9 Nthawi ina ndinali ndi moyo popanda Malamulo. Koma nditayamba kudziwa Malamulo, pomwepo uchimo unayamba kuphuka,
9 Marasika ayu ofafar men asoso’ob ana veya ayu i yawasu ama, baise obaiyunen tur tit anonowar ana veya bowabow kakafin yawas naatu ayu amorob.
10 ndipo ine ndinafa. Ine ndinazindikira kuti Malamulo omwe ankayenera kubweretsa moyo anabweretsa imfa.
10 Obaiyunen tur nati yawas bai na hirouw hio atitita’ur i morob bai na.
11 Pakuti uchimo unapeza mwayi chifukwa cha Malamulo ndipo kudzera mʼMalamulowo, unandinyenga ndi kundiyika mu imfa.
11 Anayabin bowabow kakafin, iti obaiyunen turamaim ana ef bai ayu ifuwu naatu easbunu.
12 Choncho lamulo ndi loyera, lolungama ndi labwino.
12 Isan imih ofafar i kakafiyin, naatu obaiyunen tur i kakafiyin, mutufurin naatu gewasin.
13 Kodi chomwe ndi chabwino tsopano chinasanduka imfa kwa ine? Si choncho ayi! Koma kuti uchimo uzindikirike kuti ndi uchimo unabala imfa mwa ine kudzera mu chomwe chinali chabwino, kotero kuti kudzera mu lamulo uchimo ukhale oyipa kopitirira.
13 Imih iti sawar gewasin imaim sinaf ayu au morob bai na? En anababatun! Baise bowabow kakafin i ayu easbunu, isan imih bowabow kakafin taiyuwin ana yawas botait irerereb, sawar gewasin wanawanan wa’ir na ayu imurubu. Naatu nati obaiyunenamaim bowabow kakafin na kakafin, kakafin anababatun matar.
14 Ife tikudziwa kuti Malamulo ndi auzimu; koma ine ndine munthu wofowoka chabe, wogulitsidwa ngati kapolo ku uchimo.
14 It taso’ob ofafar i ayubit isan; baise ayu i orot maiyow, bowabow kakafin ana akir wairafinamih tubunu.
15 Ine sindizindikira zimene ndimachita. Pakuti zimene ndimafuna kuchita sindizichita koma zimene ndimadana nazo ndi zimene ndimazichita.
15 Abisa asisinaf hai yabih men asoso’ob, anayabin abisa sinafumih akokok i men asisinaf, baise abisa abifutuw i asisinaf.
16 Ndipo ngati ndimachita zimene sindimafuna kuzichita, ndiye kuti ndikuvomereza kuti lamulo ndi labwino.
16 Naatu baise, abisa asisinaf i abisa men akokok i asisinaf nati i ayu abibasit ofafar i gewasin.
17 Monga mmene zililimu, si inenso mwini amene ndimazichita zimenezi, koma tchimo limene lili mʼkati mwanga.
17 Imih nati i men ayu asisinafumih, baise bowabow kakafin iti wanawana’umaim ema’am i esisinaf.
18 Ine ndikudziwa kuti mwa ine mulibe kanthu kabwino, ndiye kuti mʼthupi langa lauchimo. Pakuti ndimafuna kuchita zabwino, koma ndimalephera kuzichita.
18 Ayu so’ob wanawana’umaim i men gewasin ta ema’am, nati i ayu biyau naniyan kakafin. Anayabin ayu au kok gagamin i mi’itube gewasin ata sinaf, baise sinaf isan men karam boro anasinaf.
19 Ine sindichita zabwino zimene ndimafuna koma ndimachita zonyansa zimene sindikuzifuna.
19 Anayabin abisa gewasin sinafumih anotanot i men asisinafumih. Baise kakafih men akokok sinaf nati i ama asisinaf.
20 Tsopano ngati ine ndimachita zimene sindikuzifuna, si inenso amene ndimazichita, koma ndi tchimo limene lili mʼkati mwanga.
20 Naatu ayu sawar abisa men akokok i asisinaf, nati i men ayu asisinaf, baise bowabow kakafin wanawana’umaim ema’am i esisinaf.
21 Tsono ndapeza kuti lamuloli likugwira ntchito. Ngakhale ndimafuna kuchita zabwino, zoyipa zili nane pomwepo.
21 Isan imih iti ofafar ana ef mi’itube ebowabow i atita’ur. Ayu bowabow gewasin sinafumih anotanot ana veya, bowabow kakafin i mar etei etitit.
22 Mtima wanga umakondwera ndi lamulo la Mulungu.
22 Ayu wanawanau i ebiyasisir gagamin maiyow God ana ofafar isan.
23 Koma mʼkati mwanga ndimaona lamulo lina likugwira ntchito kulimbana ndi zomwe mtima wanga umavomereza. Lamulo limenelo landisandutsa wamʼndende walamulo la uchimo lomwe likugwira ntchito mʼkati mwa ziwalo zanga.
23 Baise ayu biyau wanawanan efan tata’ane ofafar ta ayu au not ana ofafar hairi hibiyow atatam. Nati baiyowamaim iwa’an ayu buwu bowabow kakafin ana ofafar wanawan dibur yariyu.
24 Kalanga ine! Adzandipulumutsa ndani ku thupi la imfali?
24 Ayu i yababan orot! Yait boro iti biyau murubinane niyawas nabotait.
25 Atamandike Mulungu, amene amandipulumutsa kudzera mwa Yesu Khristu Ambuye athu!
25 God ana merar ayiy Jesu Keriso’one ayu boro niyawasu. Imih ayu au not i boro God ana ofafar isan ni’akir nabow, baise ayu biyau i bowabow kakafin ana ofafar isan ni’akir nabow.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 7, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.