Romanos 6
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Nanga tinene chiyani? Kodi tipitirire kuchimwa kuti chisomo chichulukebe?
1 Abistan boro tanao? It na’atuka tanama bowabow kakafih tanasinaf, saise God ana manaw ana kabeber tafan nayababar nara’at?
2 Ayi. Mʼnjira iliyonse! Popeza tinafa ku tchimo, nanga tidzapitirira bwanji kukhalabe mʼmenemo?
2 Men karam! It i bowabow kakafinane tamorob, aisim biyat boro namatabir bowabow kakafinamaim nama maiye?
3 Kodi simukudziwa kuti tonse amene tinabatizidwa mwa Khristu Yesu tinabatizidwa mu imfa yake?
3 Na’atube Keriso Jesu wanawananamaim kwarun bapataito kwabaib ana veya, morob auman ana bapataito kwabaib men kwaso’ob?
4 Chifukwa chake ife tinayikidwa mʼmanda pamodzi ndi Iye mwa ubatizo. Tinalowa mu imfa ndi cholinga choti monga momwe Khristu anaukitsidwa kwa akufa ndi ulemerero wa Atate, ifenso tikakhale mʼmoyo watsopano.
4 Isan imih it ata bapataito’omaim Keriso bairi hubemaim tare, ana morob bairi tafaram, saise Keriso hubene Tamah ana fairamaim iyawas maiye mimisir na’atube, it auman tanamisir yawas boubunamaim tanama.
5 Pakuti ngati ife tinakhala amodzi ndi Iye mu imfa yake, tidzakhalanso ndithu amodzi ndi Iye mu kuuka kwake.
5 I ana morobomaim it bairit iti na’atube tanikofan tanamomorob na’at, i ana misiramaim turobe boro bairit tanamisir maiye.
6 Ife tikudziwa kuti umunthu wathu wakale unapachikidwa pamodzi ndi Iye kuti thupi la uchimo likhale lopanda mphamvu ndi kuti tisakakhalenso akapolo a tchimo
6 Anayabin it biyat atamanin onaf afe’en Keriso hairi hi’onafih himomorob i taso’ob, saise biyat men tama bowabow kakafin isan ti’akiramih,
7 chifukwa aliyense amene anafa anamasuka ku tchimo.
7 Anayabin orot babin yait emomorob ana veya bowabow kakafin ana fairane ikitawiy tit.
8 Koma ngati tinafa pamodzi ndi Khristu, tikhulupirira kuti tidzakhalanso ndi moyo pamodzi ndi Iye.
8 Naatu Keriso bairi tanamomorob na’at, tabitumatum i ema’amamaim it auman boro bairit tanama.
9 Pakuti tikudziwa kuti popeza Khristu anaukitsidwa kwa akufa, Iye sangafenso. Imfa ilibenso mphamvu pa Iye.
9 Anayabin it etei taso’ob Keriso i morobone misir maiye, naatu boro men karam namorob maiye, morob ana fair i wasatan.
10 Imfa imene Iye anafa, anafa ku tchimo kamodzi kokha, koma moyo umene akhala ndi wa kwa Mulungu.
10 Imih nati morob i momorob i sabuw etei hai bowabow kakafin isan mar ta’imon morob, mar moumurih na’in isan, baise yawas iti boun ema’am i God ana yawasamaim ema’ama.
11 Kotero inunso, mudzione nokha ngati akufa ku tchimo koma a moyo kwa Mulungu mwa Khristu Yesu.
11 Ef nati ta’imon, kwa taiyuw kwanasu’ubi, bowabow kakafinamaim kwa easbuni kwamorob, baise Jesu Keriso’one God ana yawasamaim boun kwama’am.
12 Nʼchifukwa chake, musalole tchimo lilamulire matupi anu amene anafa kuti mumvere zilakolako zonyansa.
12 Isan imih men kafa’imo kwanibasit bowabow kakafin kanab nabonawiy ana kok kakafih kwani’ufunun.
13 Musapereke ziwalo zathupi lanu ku tchimo, ngati zipangizo zamakhalidwe oyipa. Mʼmalo mwake, mudzipereke kwa Mulungu, ngati amene achoka ku imfa kupita ku moyo. Ndipo mupereke ziwalo zathupi lanu ngati zipangizo zachilungamo.
13 Men biya turin kwanibasit bowabow kakafin nab ana not kakafih nasinafumih, baise nati efanin taiyuw biya God kwanitin, sabuw yawasihibe kwanasinaf men murubihibe. Naatu biya tutufin etei God ana kokok gewasih sinaf isan kwanitin.
14 Tchimo silidzakhalanso ndi mphamvu pa inu, chifukwa Malamulo sakulamulira moyo wanu koma chisomo.
14 Bowabow kakafin men kafa’imo kwa isa ni’ukwarin, anayabin kwa i men ofafar babanamaim kwama’amamih, baise God ana manaw ana kabeber babanamaim kwama’am.
15 Nʼchiyani tsono? Kodi tidzichimwa chifukwa sitikulamulidwa ndi Malamulo koma chisomo? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi!
15 Imih abisa boro tanao? Bowabow kakafin tanasinaf? Anayabin it men ofafar babanamaim tama’am baise God ana manaw ana kabeberamaim tama’am? Men karam!
16 Kodi inu simudziwa kuti pamene mudzipereka kwa wina wake, kumumvera ngati akapolo, ndinu akapolo a amene mumumvera? Ngati ndinu akapolo a tchimo mudzafa. Koma ngati ndinu akapolo akumvera, mudzakhala olungama pamaso pake.
16 Kwaso’ob ai en, o yait taiyuw orot ta initin isan ini’akir inabobosiyasiyar, o i nati orot ana’akir wairafin babanamaim kuma’am. Imih o yait bowabow kakafin isan inabi’akir yomanin i morob, naatu God inabobosiyasiyar yomanin i yawas mutufurin.
17 Koma ayamikidwe Mulungu pakuti ngakhale munali akapolo a tchimo, munamvera ndi mtima wonse chiphunzitso chimene munalandira.
17 Baise God ana merar ayiy, anayabin marasika kwa i bowabow kakafin ana aiwobomaim kwama isan kwabi’akir. Baise boun dogor tutufin etei bai’obaiyen abit i kwabai kwabi’ufunun.
18 Inu munamasulidwa ku tchimo ndipo tsopano mwasanduka akapolo achilungamo.
18 Kwa i bowabow kakafinane hirufami kwatit, naatu kwana yawas gewasin isan kwabi’akir.
19 Ine ndikufanizira zinthu za tsiku ndi tsiku chifukwa chikhalidwe chanu nʼchofowoka. Monga momwe munkapereka ziwalo za matupi kukhala akapolo a zonyansa ndi makhalidwe oyipa, zimene zimanka zichulukirabe, choncho tsopano dziperekeni ziwalozo kuti zikhale akapolo achilungamo ndi a kuyera mtima.
19 Mar etei tao’omaim ao, anayabin kwa a not i boro’ika ririmin. Marasika kwa biya turin i bowabow kakafin sinaf isan kwaibasit kwaitin sisinaf. Imih boun i ef ta’imon nati na’atube kwanasinaf biya tutufin etei kwanab God ana bowabow isan kwanaya’asair, saise yawas gewasin isan ni’akir.
20 Pomwe munali akapolo atchimo, simunkalabadira za chilungamo.
20 Bowabow kakafin isan kwabi’akir ana maramaim, yawas gewasin sinaf i ana ufunane kwama.
21 Kodi munapeza phindu lanji pochita zinthu zimenezi, zomwe tsopano mukuchita nazo manyazi? Zinthu zimenezo zotsatira zake ndi imfa!
21 Nati ana veya sawar iti boun kwasisinaf isan biya eo’ohow hai gewasin i abisa kwabai? Nati sawar hai yomanin i morob.
22 Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha.
22 Baise boun kwa i bowabow kakafinane hirufami kwatit kwana God ana’akir wairafin kwamatar. Ana gewasin kwabaib i kwa ayawas tutufin etei nawiy kakafiyin matar, naatu nati sawar yomanin i ma’ama wanatowan.
23 Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
23 Anayabin bowabow kakafin ana baiyan i morob, baise God ana siwar i ma’ama wanatowan Keriso Jesu wanawananamaim ema’am.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 6, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.