Romanos 5
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Tsopano popeza tayesedwa olungama mwa chikhulupiriro, tili ndi mtendere ndi Mulungu kudzera mwa Ambuye athu Yesu Khristu.
1 Isan imih ata baitumatumamaim yamutufurit bonawiyit tana Jesu Keriso ana sinafumaim God bairi taitafentutur tama’am.
2 Iyeyo ndiye amene anatsekulira njira mwachikhulupiriro yolowera mʼchisomo mʼmene takhazikikamo. Ndipo tikukondwerera chiyembekezo cha ulemerero wa Mulungu.
2 Baitumatumamaim buwit tana manaw kabeber God nowan i’obaiyit taso’ob boun imaim tama’am. Naatu ana marakaw bonamanamarin bairi faram isan nuhit fot tama tabiyasisir.
3 Koma si pokhapo ayi, koma ife tikukondweranso mʼmasautso athu chifukwa tikudziwa kuti masautso amatiphunzitsa kupirira.
3 Men nati akisin, baise biyababan ta ta tabaib auman isan tabiyasisir, anayabin biyababanane baitafofor ebimatar,
4 Ndipo kupirira kumabweretsa makhalidwe, makhalidwe amabweretsa chiyembekezo.
4 naatu baitafoforane ata yawas ewowowab, naatu nati yawasamaim it nuhifot ebitit.
5 Ndipo chiyembekezo chimenechi sichitikhumudwitsa chifukwa Mulungu mwa Mzimu Woyera, amene Iye anatipatsa, wadzaza mʼmitima mwathu ndi chikondi chake.
5 Naatu iti nuhifot tabaib boro men yababan nititamih, anayabin God ana yabow dogorot wanawanan Anun Kakafiyinane isuwai ra’iy, nati i God ana usar it ebitit.
6 Pakuti pa nthawi yake, tikanali ochimwa, Khristu anatifera anthu osapembedzafe.
6 Anayabin it ata fair naatu ata baibais en tama’am God ana veya yai inu’in imaim Keriso na tit ata kakafih isan morob.
7 Sizichitika kawirikawiri kuti munthu wina afere munthu wolungama, ngakhale kuti chifukwa cha munthu wabwino wina atha kulimba mtima kumufera.
7 Men yait ta boro orot ana yawas mutufurin isan morobomih nakok, basit orot babin ta boro orot gewasin isan nakok.
8 Koma Mulungu anaonetsa chikondi chake kwa ife chifukwa pamene tinali ochimwabe, Khristu anatifera.
8 Baise God ana yabow it bi’obaiyit i ra’at kwanekwan, it bowabow kakafin wanawanan tama’ama ana veya Keriso isat morob.
9 Popeza chifukwa cha magazi ake ife tapezeka olungama pamaso pa Mulungu, Iyeyo adzatipulumutsa koposa kotani ku mkwiyo wa Mulungu.
9 Naatu boun it i Keriso ana rara’amaim yamutufurit, baise men nati akisin, God ana yaso’arane auman iyawasit.
10 Pakuti pamene tinali adani a Mulungu, tinayanjanitsidwa ndi Iye kudzera mu imfa ya Mwana wake. Nanga tidzapulumutsidwa bwanji kudzera mʼmoyo wake, titayanjanitsidwa naye?
10 Marasika it i God ana kamabiy sabuw, baise I Natun ana morobomaim it tana God ana tounuw tamatar, naatu men baitounuw akisin, baise God ana tufuw auman itit, i Natun ana yawasamaim it boro niyawasit.
11 Sikuti izi zili chomwechi chabe, koma timakondweranso mwa Mulungu kudzera mwa Ambuye athu Yesu Khristu. Kudzera mwa Iye, ife tsopano tayanjanitsidwa ndi Mulungu.
11 Naatu men nati akisin, baise God isan taniyasisir anayabin ata Regah Jesu Keriso iyafar na God bairi taitounuw.
12 Choncho monga momwe tchimo linalowa mʼdziko lapansi kudzera mwa munthu mmodzi, ndi imfa kudzera mu tchimo, mʼnjirayi imfa inafika kwa anthu onse pakuti onse anachimwa.
12 Tafaramamaim bowabow kakafin i orot ta’imon biyanamaim matar, naatu i ana kakafinamaim morob matar, naatu sabuw etei hibusuruf himorob, anayabin sabuw etei kakafin hisinaf.
13 Pakuti Malamulo asanaperekedwe, tchimo linali mʼdziko lapansi. Koma pamene palibe Malamulo, tchimo silitengedwa kukhala tchimo.
13 Bowabow kakafin tafaramamaim i wan matar, God ana ofafar i ufibo na. Imih bowabow kakafin ana tur Bukamaim en, anayabin ofafar en.
14 Komabe, imfa inalamulira kuyambira nthawi ya Adamu mpaka nthawi ya Mose. Inalamulira ngakhalenso pa iwo amene sanachimwe posamvera Malamulo monga anachitira Adamu. Adamuyo amene anali chifaniziro cha wina amene ankabwera.
14 Baise tanaso’ob, Adam ana veya’ika busuruf na Moses ana veya’amaim titit, orot babin etei morob nawiyih. Sabuw afa himomorob i men God ana obaiyunen Adam ea’astu’ub na’atube hi’a’astu’ub isan himorobomih, baise rara kakafinane etei himomorob.
15 Koma sitingafananitse mphatso yaulereyo ndi kuchimwa kwa anthu. Pakuti ngati anthu ambiri anafa chifukwa cha kuchimwa kwa munthu mmodziyo, kuli koposa bwanji nanga chisomo cha Mulungu ndi mphatso zomwe zinabwera ndi chisomo cha munthu mmodzi, Yesu Khristu, ndi kusefukira kwa ambiri!
15 Baise iti siwar ana baiyan en God ana manaw ana kabeberamaim bitit i ra’at kwanekwan. Men Adam ana bowabow kakafin na’atube’emih. Anayabin orot ta’imon ana kakafinamaim sabuw etei himorob, baise orot ta’imon Jesu Keriso ana manaw ana kabeberane God ana siwar gewasin bai na sabuw moumurih na’in tubunih yawas itih.
16 Ndiponso, mphatso ya Mulungu sifanana ndi zotsatira za kuchimwa kwa munthu mmodzi. Chiweruzo chinatsatira tchimo la munthu mmodzi ndi kubweretsa kutsutsidwa koma mphatso inatsatira zolakwa zambiri ndi kubweretsa kulungamitsidwa.
16 Iban ao maiye, God ana siwar naatu Adam ana kakafin hairi hai itinin i men ta’imon. Anayabin orot ta’imon ana kakafinamaim baibatiyen na sabuw baimakiy hibai. Baise God ana siwar gewasin baiyan en nan ana maramaim sabuw moumurih na’in ata kakafihimaim tama’ama botaitit naatu yamutufurih tana God biyan tatit.
17 Pakuti ngati, chifukwa cha kulakwa kwa munthu mmodziyo, imfa inalamulira kudzera mwa munthu mmodziyo, kuli koposa bwanji nanga kwa iwo amene adzalandira chisomo chochuluka ndi mphatso yachilungamo, adzalamulira mʼmoyo kudzera mwa munthu mmodzi, Yesu Khristu.
17 Orot ta’imon ana kakafinamaim sabuw etei morob nawiyih, baise turobe orot ta’imon Jesu Keriso ana sinafumaim. God ana manaw ana kabeberamaim ef baimutufurin ana siwar gewasin bisuwai boro hini’aiwob Keriso wanawananamaim.
18 Choncho monga tchimo limodzi linabweretsa kutsutsika pa anthu onse, chimodzimodzinso ntchito imodzi yolungama inabweretsa chilungamo kwa anthu onse ndi kuwapatsa moyo.
18 Isan imih orot ta’imon ana kakafinamaim sabuw etei bonawiyih baimakiy bainamih hinan. Baise iban maiye Keriso bowabow gewasin sisinafumaim sabuw yamutufurih yawas bain ma isan ana siwar itih.
19 Pakuti kusamvera kwa munthu mmodzi kunasandutsa anthu ambiri kukhala ochimwa, chimodzimodzinso anthu ambiri adzasanduka olungama kudzera mwa munthu mmodzinso.
19 Anayabin orot ta’imon ana fanasairamaim sabuw tutufin etei hi’af, imih orot ta’imon ana fanabowamaim sabuw etei hina hai ef mutufor.
20 Malamulo a Mulungu anaperekedwa ndi cholinga chakuti anthu onse azindikire kuchuluka kwa machimo awo. Koma pamene machimo anachuluka, chisomo chinachuluka koposa.
20 Ofafar natit, saise bowabow kakafin nataub nara’at, baise efan menamaim bowabow kakafin toub erara’at God ana manaw ana kabeber nati’imaim auman i tafan ya’abar erara’at.
21 Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu.
21 Isan imih bowabow kakafinamaim nawiyit tan morob wan tayen, baise God ana manaw ana kabeberamaim ata Regah Jesu Keriso biyanamaim ata ef yamutufur ma’ama wanatowan itit. Manaw kabeberamaim yamutufurit|alt="sin reigned in death" src="C007.tif" size="col" loc="Illustration used with permission of New Tribes Mission." copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="5.21"
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.