Romanos 4
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Nanga tsono tidzati chiyani za Abrahamu kholo lathu, iyeyu anapezana ndi zotani pa nkhani imeneyi?
1 Abraham it uwat regah biyanamaim sawar abisa himatar, imaim itah soso’ob isah boro mi’itube tanao?
2 Kunena zoona, Abrahamu akanalungamitsidwa ndi ntchito zake, akanakhala nako kanthu kodzitamandira, koma osati pamaso pa Mulungu.
2 Anayabin Abraham ana bowabowamaim yamutufuren nabaib na’at, i karam ana ef ema’am boro nao ra’ara’at, baise men God nanamaim.
3 Kodi Malemba akuti chiyani? “Abrahamu anakhulupirira Mulungu, ndipo ichi chinamuchititsa kukhala wolungama.”
3 En baise, Buk Atamaninamaim iti na’atube eo? “Abraham God itumitum naatu i ana baitumatumamaim God yamutufuren ana i’inanen itin.”
4 Tsopano munthu amene wagwira ntchito, malipiro ake satengedwa kukhala ngati mphatso koma zimene anayenera kulandira.
4 Orot ebowabow isan tibibaiyan, nati i men ana siwar tibitin baise ana bowabow isan baiyan tibitin.
5 Koma kwa munthu amene sanagwire ntchito ndipo akhulupirira Mulungu amene amalungamitsa ochimwa, chikhulupiriro chakecho chimatengedwa kukhala chilungamo.
5 Orot yait ana bowabow men i’itin, baise ibitumitum God i sabuw kakafih eyayamutufurih. Nati orot boro yamutufuren ana’i’inanen Godane nab, anayabin ebitumatum, men ana bowabowamaim.
6 Davide ponena zomwezi pamene anayankhula za kudala kwa munthu amene Mulungu amulungamitsa osati chifukwa cha ntchito zake akuti,
6 Buk Atamaninamaim David i tur ta’imon eo, orot yait yamutufuren ana’i’inanen God bitin boro baigegewasin nab, men ana bowabowamaim. Imih David iti na’atube eorereb eo,
7 “Odala ndi amene
7 “Orot yait
8 Ngodala munthu amene
8 Nati orot i boro baigegewasin nab,
9 Kodi madalitso amenewa ali kwa ochita mdulidwe okha kapena kwa amene sanachitepo mdulidwe? Ife takhala tikunena kuti chikhulupiriro cha Abrahamu chinamuchititsa kukhala wolungama.
9 Iti baigegewasin i sabuw iyab hai ar kanabih hi’a’afuw akisih isah, ai hai ar afuwa’e tema’ama auman isah? Baise boun tanowar, “Abraham i ana baitumatumamaim God dogoron botabir ana ef mutufurin rouw eo.”
10 Kodi chinatengedwa bwanji? Kodi nʼkuti iye atachita mdulidwe kapena asanachite? Osati atachita mdulidwe koma asanachite!
10 Iti sawar i mi’itube matar? Abraham ana ar afuwina’e ma’am ana veya matar o ana ar hi’a’afuw ufunamaim matar? Baise anao kwananowar, Abraham i wan God ana baibasit wanawanan run, imaibo ana ar i uf hi’afuw.
11 Ndipo iye anachita mdulidwe ngati chizindikiro ndi chitsimikizo cha kulungama kumene anali nako mwachikhulupiriro pomwe anali asanachite mdulidwe. Choncho, iye ndi kholo la onse amene akhulupirira koma sanachite mdulidwe, ndi cholinga chakuti alungamitsidwe.
11 Naatu nati ar afu’afuw i Abraham ana baitumatumamaim yamutufuren baib ana i’inanen. Iti sawar i Abraham ana ar kanabin auman ma’am ana veya matar. Isan imih sabuw iyab hai ar kanabih auman baise hina baitumatumayah himamatar tamah i Abraham, anayabin i hai baitumatumamaim God hai ef mutufurin rouw eorereb.
12 Ndipo iyenso ndiyenso kholo la ochita mdulidwe osati amene anangochita mdulidwe kokha koma amene amatsata chitsanzo cha chikhulupiriro chimene kholo lathu Abrahamu anali nacho asanachite mdulidwe.
12 Naatu Abraham auman i tamah, men ar afu’afuw akisin, baise Abraham ana baitumatumamaim ana’ar kanabin auman ma reremor tibi’ufunun auman.
13 Abrahamu ndi zidzukulu zake sanalandire lonjezano lakuti adzalandira dziko lapansi kudzera mu Malamulo, koma kudzera mu chilungamo chimene chimabwera ndi chikhulupiriro.
13 Abraham wawawan bairi God tafaram nowahimih baitih isan eo’omatanih ana veya i men ofafar bobosiyasiyar isan. Baise ana baitumatumamaim ana ef mumutufor isan.
14 Pakuti ngati amene amadalira Malamulo ndiye olowa mʼmalo, ndiye kuti chikhulupiriro nʼchopanda pake ndipo lonjezano ndi lopanda phindu
14 Anayabin sabuw iyab ofafar tebobosiyasiyar isan God ana omatanen nabitih na’at, baitumatum i boro nan ana’an en namatar naatu God ana omatanen i owararin.
15 chifukwa Malamulo anabweretsa chilango. Ndipo kumene kulibe Malamulo kulibenso kuwalakwitsa.
15 Ofafaramaim ya so’ar emamatar, baise efan menamaim ofafar men ema’am, asto’oben men ema’ama.
16 Motero, timalandira lonjezo mwachikhulupiriro. Laperekedwa mwachisomo kuti patsimikizidwe kuti lonjezolo liperekedwa kwa ana ndi zidzukulu zonse za Abrahamu, osati kwa iwo okha amene amatsatira Malamulo komanso kwa iwo amene ali ndi chikhulupiriro cha Abrahamu. Iye ndiye kholo la ife tonse.
16 Isan imih omatanen etei i baitumatumamaim emamatar, saise manaw kabeber Godane nan Abraham wawawan etei isah, men sabuw iyab ofafar tebobosiyasiyar akisih isah. Baise baitumatumayah auman Abraham bitumatum na’atube. Anayabin it etei ayubit isanane tamat i Abraham.
17 Monga kwalembedwa kuti, “Ine ndakusandutsa kukhala kholo la mitundu yambiri.” Iye ndiye kholo lathu pamaso pa Mulungu, amene anamukhulupirira, Mulungu amene amapereka moyo kwa akufa ndipo amapereka moyo kwa zinthu zopanda moyo.
17 Bukamaim iti na’atube eo, “Ayu o asinafi tafaram tutufin etei tamah imatar. Imih iti omatanen isan Abraham God ana tur itumitum,” anayabin God i murumurubih ebiyayawasih, naatu sawar yanonowat eo hitit tibirerereb.
18 Ngakhale zinali zosayembekezeka, Abrahamu anakhulupirira ndi chiyembekezo kuti adzakhala kholo la mitundu yambiri. Izi ndi monga zinanenedwa kwa iye kuti, “Ndi mmene adzakhalire ana ako ndi zidzukulu zako.”
18 Abraham sawar God eo’omatan men itah, baise baitumatumamaim nuhin fot ma kakaif yomaninamaim tafaram maumurih na’in tamah matar. Bukamaim isan eo na’atube matar, “O natunat boro daman na’atube.”
19 Iye sanafowoke mʼchikhulupiriro. Anadziwa choonadi cha thupi lake kuti linali lakufa popeza anali ndi zaka pafupifupi 100 ndiponso mimba ya Sara inali yowuma.
19 Abraham ana kwamur i ra’at, biyan i morob, naatu aawan Sarah yan wanawanan kek ana bar auman i morob, baise Abraham ana baitumatum i men ririm.
20 Komabe iye sanagwedezeke chifukwa chosakhulupirira pa zokhudzana ndi lonjezo la Mulungu. Iye analimbikitsidwa mʼchikhulupiriro chake ndi kupereka ulemerero kwa Mulungu.
20 Naatu men kafa’imo God ana omatanen isan erekasiy auman ma’amih, baise ana baitumatum eabar totofar bat God ana merar yi bora’ara’ah.
21 Anatsimikiza mu mtima mwake kuti Mulungu anali ndi mphamvu yochita chomwe analonjeza.
21 Abraham ana naniyan tutufin etei bai so’ob God i fairin, abisa isan eo’omatan i karam boro nasinaf.
22 Nʼchifukwa chake “chinamuchititsa kukhala wolungama.”
22 Ana’an iti isan, Abraham ana baitumatumamaim ana yawas mumutufor isan God bai.
23 Mawu akuti, “chinatengedwa kwa iye” sanalembedwe chifukwa cha iye yekha,
23 Iti tur, “Ana ef mutufurinamaim God baib” i men Abraham akisin isan hikirum.
24 komanso chifukwa ife amene Mulungu adzatiyesa olungama, ife amene tikhulupirira mwa Iye amene anamuukitsa kwa akufa, Yesu Ambuye athu.
24 Baise it auman isat hikirum, it iyabowat ata ef emumutufor naatu iyabowat tabitumatum God Jesu ata Regah morobone biyawas maiye isan.
25 Iye anaperekedwa kuti aphedwe chifukwa cha machimo athu ndipo anaukitsidwa ndi kukhala ndi moyo kuti tilungamitsidwe.
25 Jesu it ata kakafin isan God ibasit hi’asabun, baise morobone iyawas maiye, saise it tanawiyit tanan God nanamaim tayamutufurit.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.