Romanos 3
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Nanga kodi pali ubwino wotani pokhala Myuda, kapena muli ubwino wanjinso mu mdulidwe?
1 Jew orot inamamatar boro Ufun Sabuw inanatabirih? Naatu a’ar kanabin hina’a’afuw ana gewasin i boro men tomar inab?
2 Ubwino wake ndi wambiri mʼnjira zonse! Choyambirira iwo anapatsidwa Mawu a Mulungu kuti awasunge.
2 Ef tata’ane etei i gewasih, wantoro’ot God ana tur i Jew sabuw hitutumih hitih.
3 Nanga zili bwanji ngati ena analibe chikhulupiriro? Kodi kupanda chikhulupiriro kwawo kukanalepheretsa kukhulupirika kwa Mulungu?
3 Baise sabuw afa men hibitumitum isan, kwanotanot God ana omatanen isan boro men nabosunusunub?
4 Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Mulungu akhale woona, ndi munthu aliyense akhale wonama. Monga kwalembedwa kuti,
4 En anababatun! God ana tur i mar etei turobe, baise sabuw i baifuwenayah. Buk Atamaninamaim iti na’atube hikirum,
5 Koma ngati kuyipa mtima kwathu kuonetsa poyera kuti Mulungu ndi wolungama, ife tinganene chiyani? Kodi tinganene kuti Mulungu ndi wosalungama pamene aonetsa mkwiyo wake pa ife? (Ine ndikuyankhula monga mmene anthu ena amayankhulira).
5 Baise it ata sinaf kakafihimaim God ana sinaf gewasin bebeyan natit sabuw hina’i’itin ana veya, it boro mi’itube tanao? God baifuwenamaim yan so’ar baimakiy ebitit? it i anababatun taikoko’aw tao kwanekwan.
6 Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Ngati zikanakhala zotero, kodi Mulungu akanaweruza bwanji dziko lapansi?
6 Nati tur i men turobe tao’omih, anayabin sinaf nati na’atube nama’am, God boro mi’itube tafaram ana sabuw nibatiyih?
7 Wina atanena kuti, “Ngati kunama kwanga kukuonetsa koposa kuti Mulungu ndi woona, ndi kuwonjezera pa ulemerero wake, nanga nʼchifukwa chiyani ndikuweruzidwa kuti ndine wochimwa?”
7 Orot babin ta boro nagam nao, “Ayu i men bosunusunubayan, baise au bowabowamaim turobe God nowan tit irerereb sabuw hi’itin God hifai tebobora’ara’ah, aisim God ayu kakafu rouw eo ekukusairu?”
8 Nʼchifukwa chiyani osanena kuti, monga ena amanena mosasamala kuti, “Tiyeni tichite zoyipa kuti zabwino zionekere?” Anthu onena zoterewa kulangidwa kwawo ndi koyenera.
8 Naatu iban boro kwanao maiye, kakafin tanasinaf, saise sinaf gewasin boro ine natit. Sabuw afa ayu iti na’atube o hirouw higam tiu’uwu, God nati sabuw boro baimakiy nitih.
9 Kodi timalize bwanji? Kodi Ayuda ndife oposa anthu ena? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Ife tinanena kale kuti Ayuda ndi a mitundu ina omwe ndi ochimwa.
9 Iti sawar ana an i abisa? It Jew ata gewasin i ra’at Eteni Sabuw tanatabirih? En anababatun! Jew sabuw naatu Eteni Sabuw etei i bowabow kakafin ana fair babanamaim tama’am.
10 Monga kwalembedwa kuti,
10 Buk Atamaninamaim iti na’atube hikirum,
11 Palibe ndi mmodzi yemwe amene amazindikira,
11 Men yait ta ana not rerekabin,
12 Onse apatukira kumbali,
12 Etei hitatabir kouh God hitin,
13 “Kummero kwawo kuli ngati manda apululu;
13 Sikah dub i tahahab sabuw tetotonan,
14 “Mʼkamwa mwawo ndi modzaza ndi zotemberera ndi mawu owawa.”
14 “Awah i orarafen awan karatan naatu tenakuyakuy.”
15 “Mapazi awo afulumira kukakhetsa magazi.
15 “Iti sabuw umah i rara awan karatan.
16 Kusakaza ndi chisoni kumaonekera mʼnjira zawo,
16 Menamaim tenan ma kakaf naatu gurugurusen mar etei imaim emamatar,
17 ndipo njira ya mtendere sayidziwa.”
17 Naatu tufuwamaim ma ana ef i men hiso’ob.
18 “Saopa Mulungu ndi pangʼono pomwe.”
18 Naatu God matanamaim men kafa’imo tibibiruw.”
19 Tsopano tikudziwa kuti chilichonse Malamulo amanena, amanena kwa amene amalamulidwa ndi Malamulowo, ndi cholinga chakuti aliyense asowe chonena, ndipo dziko lonse lidzayimbidwa mlandu ndi Mulungu.
19 Imih it ata so’obamaim ofafar hikikirum i sabuw iyab ofafar babanamaim tema’am isah, saise awah etei nabofafaren, naatu tafaram wanawanan sabuw etei nabow nan God ana baibatiyenamaim hinatit.
20 Chifukwa chake palibe mmodzi amene adzayesedwa wolungama pamaso pake chifukwa chosunga Malamulo, kuti ife timazindikira tchimo kupyolera mu Malamulo.
20 Isan imih God boro men sabuw ofafar tebobosiyasiyar imaim hai ef mutufurin narouw nabowamih, ofafar i orot babin ana bowabow kakafin botait ebirerereb.
21 Koma tsopano chilungamo chochokera kwa Mulungu, osati chochokera ku Malamulo, chaonetsedwa. Ichi ndi chimene Malamulo ndi Aneneri amachitira umboni.
21 Baise boun God sabuw yamutufurih isan ana ef i boubun botawiy. Moses naatu dinab oro’orot nati isan i ofafaramaim hio’orereb tanowar, men ofafar tanabi’ufununimaim nabuwitamih.
22 Timakhala olungama pamaso pa Mulungu pamene takhulupirira Yesu Khristu. Mulungu amachitira zimenezi anthu onse amene akhulupirira Khristu. Palibe kusiyana pakati pa Myuda ndi a mitundu ina,
22 It yamutufuren boubun Godane enan i sabuw iyab Jesu Keriso tibitumitum imaim enan, naatu God matanamaim it etei ata’itinin i men tata’amih.
23 pakuti onse anachimwa naperewera pa ulemerero wa Mulungu
23 Anayabin sabuw etei bowabow kakafin hisinaf naatu God ana gewasin bain isan umah kabom.
24 ndipo onse alungamitsidwa mwaulere mwa chisomo chake chifukwa cha Khristu Yesu amene anawawombola.
24 Baise manaw kabeber God ana siwar na’atube Jesu Keriso wanawananamaim na it ata kakafihine tubunit botaitit tatit.
25 Mulungu anamupereka Iyeyu kuti pokhetsa magazi ake, akhale nsembe yokhululukira machimo. Mulungu anachita zimenezi kufuna kuonetsa chilungamo chake. Chifukwa cha kuleza mtima kwake, sanalange anthu chifukwa cha machimo amene anachita kale.
25 Bowabow kakafin notawiyen isan God Keriso biyan siboromih yai, ana rara suwa re saise baitumatumamaim tanan biyan tanatit. Sawar iti na’atube sinaf saise bebeyan ti’obaiyit i ana ef i mutufurin. Anayabin I ana yatenub kakafiyin imaim bowabow kakafih marasika tasisinaf isubun rabon.
26 Iye anachita izi kuti aonetse chilungamo chake lero lino. Anthu azindikire kuti Iye ndi wolungama ndipo amalungamitsa aliyense amene akhulupirira Yesu.
26 Naatu iti boun it ata veya’amaim i turobe ebi’obaiyit i ana ef mutufurin. Imih i karam sabuw iyab Jesu tibitumitum boro nafufunih gewas nayamutufurih.
27 Nanga tsono pamenepa munthu anganyadenso? Kunyadatu kwachotsedwa. Chifukwa cha Malamulo? Kodi Malamulo samafuna ntchito za munthu? Ayi, koma mwachikhulupiriro.
27 Isan imih it boro abisa isan tanaora’ara’at? Ofafar tabobosiyasiyar isan tarara’at? En anababatun! Baise baitumatum isan i tarara’at.
28 Ife tikunenabe kuti munthu amalungamitsidwa mwachikhulupiriro osati mwakusunga Malamulo.
28 Anayabin sabuw iyab tibitumatum i hai ef mutufurin rouw ebowabow men ofafaramih.
29 Kodi Mulungu ndi Mulungu wa Ayuda okha? Kodi si Mulungu wa a mitundu inanso? Inde wa a mitundu inanso,
29 Imih kwanotanot God i Jew sabuw akisih hai God? Ai kwanotanot Ufun Sabuw auman hai God? Baise anao kwananowar, iti God i Ufun Sabuw auman hai God.
30 popeza ndi Mulungu mmodzi yemweyo amene adzalungamitsa mwachikhulupiriro ochita mdulidwe ndi osachita mdulidwe kudzera mʼchikhulupiriro chomwecho.
30 Kwanaso’ob God i ta’imon men rou’ab, imih sabuw iyab hai ar kanabih hi’afuw o men hi’afuw etei i baitumatum ta’imonamaim hiyawas.
31 Kodi tsono ife, tikutaya Malamulo pamene tikunena kuti pafunika chikhulupiriro? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Komatu ife tikukwaniritsadi Malamulo.
31 Kwanotanot iti baitumatumamaim aki ofafar abobosa’ir? En anababatun, aki i ofafar aiwa’an tit ana efan bai ebirerereb.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.