Romanos 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Choncho, iwe amene umaweruza munthu wina, ulibe pokanira pakuti nthawi iliyonse pamene uweruza wina ukudzitsutsa wekha chifukwa iwe amene umaweruzawe umachitanso zinthu zomwezo.
1 Isan imih kwa isa men ef ta ema’am boro imaim kwanabat sabuw afa hai kakafih kwanasebmatar ubar kwanitih, anayabin nati kakafin ta’imon kwa auman kwasisinaf.
2 Tsopano ife tikudziwa kuti chiweruzo cha Mulungu, chotsutsa amene amachita zinthu zotere, nʼchokhazikika pa choonadi.
2 Baise God turobe tafanamaim bat sabuw iyab kakafih tisisinaf isan baibatiyen ebitih i taso’ob.
3 Kodi ukuganiza kuti udzathawa chiweruzo cha Mulungu iwe munthu wamba, pamene uweruza ena, iwe ndi kumachitanso zomwezo?
3 Imih o orot maiyow, sawar kakafin o kusisinaf na’atube sabuw tisisinaf isan o kubibatiyih o kunotanot God ana baibatiyen boro inahaiw?
4 Kodi kapena ukupeputsa kukoma mtima kwa Mulungu, kuleza mtima kwake ndi kupirira kwake? Kodi sukuzindikira kuti kukoma mtima kwakeko, nʼkofuna kuti iweyo ulape machimo ako?
4 Ai o God ana baiwanbabanen, ana yawanan, ana yatenub i ku’i’itin furuw. Naatu o iwanbabani dogor baikitabirin isan enanawiyi kwa’i’itin ai en?
5 Koma pakuti ndiwe wosamvera ndi wa mtima wosafuna kulapa, ukudzisungira chilango pa tsiku la mkwiyo wa Mulungu, pamene chiweruzo cholungama cha Mulungu chidzaonetsedwa.
5 Baise anayabin kwa i kwafokar naatu dogor kwahir, a baimakiy kwama kwatutu ra’at eyey ana Veya’amaim God ana yaso’ar bebeyan nab natit turobe’emaim tafaram boro nabibatiy kwana’itin.
6 Mulungu adzabwezera aliyense molingana ndi ntchito zake.
6 God boro ta’ita’imon abowabow ana fofonin a baiyan nit.
7 Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira.
7 Sabuw iyab yatehnub hima gewasin tisisinaf, naatu marakaw, baifa’en, ma wanatowan tinunuwih boro ma’ama wanatowanin nitih.
8 Koma Mulungu adzakhuthulira mkwiyo ndi ukali wake pa amene amachita zofuna zawo ndi kukana choonadi nʼkumatsatira zoyipa.
8 Baise sabuw iyab i taiyuwih hai yawas tinunuwih, naatu turobe hikwahir kakafih tibi’ufunun, God ana gagamat naatu ana yaso’ar boro tafah yan nisuwai nare.
9 Masautso ndi zowawa zidzagwera munthu aliyense amene amachita zonyansa, kuyambira Myuda kenaka anthu a mitundu ina.
9 Sabuw iyab bowabow kakafih tisisinaf i boro bai’akir naatu biyababan gagamin maiyow hinab. Jew sabuw biyahimaim boro nabusuruf nan Ufun Sabuw biyahimaim nisawar.
10 Koma ulemerero, ulemu ndi mtendere zidzakhala kwa aliyense amene amachita zabwino, kuyambira Myuda kenaka anthu a mitundu ina.
10 Baise sabuw iyab bowabow gewasih tisisinaf, God boro fair, baifa’en, borara’aten naatu tufuw nitih, Jew sabuw biyahimaim boro nabusuruf nan Ufun Sabuw biyahimaim nisawar.
11 Pajatu Mulungu alibe tsankho.
11 Anayabin God i ana fofoninamaim sabuw bai’ubaren ebitih, men ta aukoun ebatabatamih.
12 Onse amene amachimwa osadziwa Malamulo, adzawonongeka ngakhale kuti sadziwa Malamulowo. Ndipo onse amene amachimwa akudziwa Malamulo adzaweruzidwa potsata Malamulowo.
12 Sabuw iyab ofafar ufunane hima kakafin hisisinaf auman boro baimakiy hinab. Naatu sabuw iyab ofafar babanamaim hima kakafin hisisinaf boro ofafar nibatiyih.
13 Pakuti si amene amangomva Malamulo amene amakhala wolungama pamaso pa Mulungu, koma ndi okhawo amene amachita zili mʼMalamulomo amene adzatchedwa olungama.
13 Anayabin sabuw i boro men ofafar tenonowaramaim nayamutufurih God matanamaim hinatitamih, en baise ofafar hinowar tibi’ufunun boro nayamutufurih.
14 Ndithu, pamene a mitundu ina, amene alibe Malamulo, koma mwachikhalidwe chawo amachita zimene zili mʼMalamulo, iwowo ndi Malamulo pa iwo okha, ngakhale kuti alibe Malamulowo.
14 Eteni Sabuw aurih ofafar i en, baise abisa i hai yawasamaim eo na’atube tisisinaf i hai ofafar turaban nati, basit i aurih ofafar anababatun i en.
15 Ntchito zawo zimaonetsa kuti Malamulowo alembedwa mʼmitima mwawo. Chikumbumtima chawonso chimawachitira umboni pakuti maganizo awo amawatsutsa kapena kuwavomereza.
15 Anayabin kakafin gewasin kousibin ana not i ofafar na’atube dogoromaim ema’am boro a tur na’owen, a kakafin isan boro ubar nit nakusairi, naatu a gewasin isan boro natafafari.
16 Izi zidzachitika pa tsiku limene Mulungu adzaweruza zinsinsi za anthu kudzera mwa Yesu Khristu, monga momwe Uthenga wanga Wabwino unenera.
16 Tur Gewasin iti ao’orereb na’atube boro namatar. Nati baibatebat ana veya God boro Jesu Keriso narubin sabuw hai not wa’iwa’irih etei boro nabow hinatit rerereb yah naya.
17 Koma iweyo, amene umadzitcha kuti ndiwe Myuda, umadalira Malamulo, ndipo umanyadira ubale wako ndi Mulungu,
17 Baise kwa Jew sabuw kwarouw kwao, naatu ofafar tafanamaim kwabat God isan kwanao ra’at.
18 ngati umadziwa chifuniro chake, ndi kudziwa zoyenera kuchita chifukwa unaphunzitsidwa ndi Malamulo;
18 God ana kokok sinaf isan i kwaso’ob, naatu kakafin gewasin hairi kusibin isan i ofafaramaim ebi’obaiyi.
19 ngati umadziwadi kuti ndiwe mtsogoleri wa osaona, nyale yowunikira amene ali mu mdima,
19 Taiyuw kwaso’ob, kwa i matah fim hai nabatanayah, gugumin ma’ayah hai marakaw
20 mlangizi wa anthu opusa, mphunzitsi wa makanda, chifukwa umadziwa kuti mʼMalamulo uli nayo nzeru yonse ndi choonadi,
20 koko’aw sabuw hai roube’atenayah, bereberefiy hai bai’obaiyenayan, naatu ofafar wanawanan ana kinitur tutufin etei naatu turobe etei auman i kwaso’ob.
21 tsono, iwe amene umaphunzitsa ena, sudziphunzitsa wekha kodi? Kodi iwe amene umalalikira kuti anthu asabe, umabanso?
21 Sabuw kwabi’obaibiyih, baise kwa taiyuwiban kwabi’obaiyi ai en? A binanumaim kwao, “Men kwanabain” Baise o kubabain ai en?
22 Kodi iwe amene umanena kuti anthu asachite chigololo, umachitanso chigololo? Kodi iwe amene umanyasidwa ndi mafano, umalandanso za mʼnyumba zopembedzera mafanowo?
22 Sabuw turahinah aawah ufun na isan i kuo’otanih, baise o turanah aawah ufuh kwenan ai en? Umataratar baifa’ifa’ih irouw kuo, baise hai kwafiren bar wanawanan o kubabain ai en?
23 Kodi iwe amene umadzitama ndi Malamulo, umamuchititsa manyazi Mulungu posamvera Malamulowo?
23 God ana ofafar isan i kuo’ora’ara’at, baise ofafar i’astu’ub God biya’ohow kubitiniban kui’itin ai en?
24 Monga kwalembedwa, “Dzina la Mulungu likuchitidwa chipongwe pakati pa a mitundu ina chifukwa cha inu.”
24 Buk Atamaninamaim iti na’atube hikirum, “Eteni Sabuw God wabin tibigigim anayabin kwa Jew sabuw asinafumaim.”
25 Mdulidwe umakhala ndi phindu ngati usunga Malamulo, koma ngati sumvera Malamulo, iweyo umakhala ngati kuti sunachite mdulidwe.
25 O ofafar inabobosiyasiyar na’at, a’ar hi’a’afuw i boro nan ana’an gagamin namatar, baise ofafar ina’a’astu’ub, o a’ar kanabin hi’a’afuw ana’itin i afuwina’e.
26 Ngati amene sanachite mdulidwe achita zomwe zili mʼMalamulo, kodi sadzatengedwa ngati ochita mdulidwe?
26 Sabuw iyab hai ar kanabih men hi’afuw, baise ofafar eo biyunih na’atube tebobosiyasiyar, nati sabuw i sabuw iyab hai ar kanabih hi’a’afuw hinasairih.
27 Munthu amene sanachite mdulidwe mʼthupi koma amamvera Malamulo adzakutsutsa iwe wosamvera Malamulowe, ngakhale kuti uli nawo Malamulo olembedwawo.
27 Orot yait biyanane ana ar kanabin men hi’afuw, baise ofafar i ebobosiyasiyar, o boro nasiksairi, anayabin o i ofafar iso’ob naatu a’ar kanabin hi’afuw, baise ofafar men kubobosiyasiyar.
28 Myuda weniweni si amene angooneka ngati Myuda pamaso pa anthu, ndipo mdulidwe weniweni si umene umangochitika mʼthupi pamaso pa anthu.
28 O yait Jew orot kumamatar i men biya ufunane hi’a’afuw imaim o ina Jew orot kumamataramih.
29 Ayi, Myuda weniweni ndi amene ali Myuda mu mtima mwake, ndipo mdulidwe weniweni ndi wa mtima, wochitika ndi Mzimu, osati ndi malamulo olembedwa. Woyamikira munthu wotere ndi Mulungu, osati anthu ayi.
29 En baise, Jew orot anababatun i dogor wanawanan. Naatu afu’afuw anababatun i dogor wanawananamaim Anun Kakafiyin esisinaf, men biya. Naatu bora’ara’aten etei i Godane nan inab men orot biyahine.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.