Romanos 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndine Paulo, mtumiki wa Khristu Yesu, woyitanidwa ndi Mulungu kukhala mtumwi. Ndinapatulidwa kuti ndilalikire Uthenga Wabwino wa Mulungu
1 Ayu Paul, Jesu Keriso ana akir wairafin, tur abarin isan rubinu, naatu Tur Gewasin binan isan God eafu atit.
2 umene analonjeza kale mʼMalemba Oyera kudzera mwa aneneri ake.
2 Iti Tur Gewasin i marasika God ana dinab hai veya’amaim eomatanih, dinab oro’orot Buk Kakafiyinamaim hikirum.
3 Uthengawu ndi wonena za Mwana wake amene mwa umunthu wake anali wochokera mwa Davide.
3 Iti tur ana an gagamin i Natun it ata Regah Jesu Keriso isan. Biyanane ana tufuw i David ana rara’ane tufuw.
4 Iyeyu ndi amene anatsimikizidwa kukhala Mwana wa Mulungu mwamphamvu za Mzimu Woyera pamene anauka kwa akufa. Kudzera mwa Ambuye athu Yesu Khristu,
4 Baise i Ayubin ana kakafiyinamaim morobone mimisir ana veya, bebeyan ebi’obaiyit turobe i, i God Natun fairin.
5 ife tinalandira chisomo chokhala atumwi oyitana anthu a mitundu yonse kuti amukhulupirire ndi kumumvera mwachikhulupiriro kuti dzina lake lilemekezedwe.
5 I wanawananamaim naatu i wabin isan ayu manaw kabeber itu ana tur abarayan amatar, saise tafaram wanawanan Ufun Sabuw anabuwih hinan tur hinitumatum naatu hinabosiyasiyar.
6 Inunso muli mʼgulu la Amitundu oyitanidwawo kukhala ake a Yesu Khristu.
6 Naatu kwa auman i nati sabuw wanawanahimaim Jesu Keriso nowan matar isan God eafi.
7 Ndikulembera kwa onse okhala ku Roma amene Mulungu amakukondani nakuyitanani kuti mukhale oyera mtima.
7 Naatu Rome wanawanan kwa iyab God iyabuwi naatu rubini i ana sabuwamih kwamatar kwama’am etei, isa ayoyoyoban manaw kabeber, tufuw Tamat Godane naatu ata Regah Jesu Keriso’one mar etei kwa isa nama.
8 Poyamba, ndikuthokoza Mulungu wanga kudzera mwa Yesu Khristu chifukwa cha nonsenu, pakuti pa dziko lonse lapansi anthu akukamba za chikhulupiriro chanu.
8 Wantoro’ot Jesu Keriso wabinamaim ayu au God ana merar ayiy kwa etei isa, anayabin kwa a baitumatum i tuw ra’at tafaram wanawanan sabuw etei tenonowar.
9 Mulungu amene ndimamutumikira ndi mtima wanga onse polalikira Uthenga Wabwino wa Mwana wake, ndi mboni yanga kuti ndimakupemphererani nthawi zonse.
9 God isan dogorou tutufin etei abow i Natun ana tur gewasin abibinan, i so’ob, ayu mar etei kwa anunuhi.
10 Mʼmapemphero anga, nthawi zonse, ndimapemphera kuti ngati nʼkotheka mwachifuniro cha Mulungu, njira inditsekukire kuti ndibwere kwanuko.
10 Matanfufur isa ayoyoyoban, naatu au yoyobanamaim God abifefeyan nakokok na’at boun ana veya ef nabotawiy isou naham anan kwa aninanawani.
11 Ine ndikulakalaka kukuonani kuti ndikugawireni mphatso zina zauzimu kuti zikulimbikitseni
11 Au kok gagamin i mi’itube kwa ayumat ata itin, saise ayubit ana usar kwa atit imaim a fair kwatab.
12 ndiponso kuti tonsefe tilimbikitsane mʼchikhulupiriro wina ndi mnzake.
12 Iti tur i men ayu akisu kwa fair bait isan ao’omih, baise kwa auman ayu koufair kwanitu bairi tanibaibaisbonen ata baitumatum nakwat isan ao’o.
13 Abale, ine sindifuna kuti mukhale osadziwa kuti nthawi zambiri ndakhala ndikufuna zobwera kwanuko, koma mpaka pano pali zolepheretsa, ndi cholinga choti ndidzapezeko zipatso pakati panupo monga momwe ndakhala ndikuchitira pakati pa a mitundu ina.
13 Taitu tuwa’inah ayu akokok tain anayai kwanaso’ob, mar moumurih na’in abogaigiwas atan kwa ata’iti, saise kwa wanawanamaim Ufun Sabuw afa atabow hitan baitumatum wanawanan hitarun, nati’imaim abow hina baitumatum wanawanan hirur na’atube. Baise sawar moumurih maiyow ayu au ef hirufutifut tama tanan iti boun tatit.
14 Ine ndi wokakamizidwa ndi udindo wotumikira Agriki pamodzi ndi omwe si Agriki, kwa anzeru ndi kwa opusa omwe.
14 Ayu i sabuw etei’imak isah bai’akiramih atit, Greek sabuw naatu sabuw iyab men Greek, na’atube sabuw so’ob wairafih naatu men so’ob wairafih etei’imak isah anabow anibaisih.
15 Pa chifukwa chimenechi, ine ndikufunitsitsa kulalikira Uthenga Wabwino kwa inunso amene muli ku Roma.
15 Ana’an nati isan ayu akokok kwanekwan tur gewasin kwa iyab nati Rome kwama’ama auman isa anabinan.
16 Ine sindichita manyazi ndi Uthenga Wabwino chifukwa ndiwo mphamvu za Mulungu zopulumutsa aliyense amene akhulupirira, poyamba Myuda, kenaka Mhelene.
16 Ayu Tur Gewasin ao’orereb isan men biyou eo’ohow, anayabin God ana fair i ef iti’imaim tit sabuw iyab tibitumatum ebiyawasih. Iti yawas i wantoro’ot Jew sabuw isah, baise Ufun Sabuw auman.
17 Pakuti mu Uthenga Wabwino anawulula kuti chilungamo chimachokera kwa Mulungu. Kuyambira pachiyambi mpaka potsiriza ndi chilungamo chobwera mwachikhulupiriro, monga kwalembedwera kuti, “Wolungama adzakhala ndi moyo mwachikhulupiriro.”
17 Anayabin yawas mutufurin Godane i tur gewasinamaim orot babin eyayamutufurih, baitumatumamaim ebubusuruf naatu boro baitumatumamaim nasawar. Buk Atamaninamaim hikikirum iti na’atube eo,
18 Mkwiyo wa Mulungu ukuonekera kuchokera kumwamba. Ukutsutsana ndi kusapembedza konse ndi kuyipa kwa anthu amene amapondereza choonadi mwa chikhalidwe chawo choyipa.
18 Sabuw bowabow kakafih sinafuyah naatu sabuw tafa’asarih, i hai kakafinamaim turobe ana gewasin esumisum, imih maramaim God ana ya so’ar tit ibirerereb nati sabuw isah.
19 Za Mulungu zimene zingathe kudziwika, ndi zomveka bwino kwa iwo pakuti Mulungu anazionetsera kwa iwo.
19 Sawar tutufin etei i rereb yah hi’itah tesoso’ob, anayabin God etei bebeyanamaim sinaf tibirerereb.
20 Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula.
20 Anamaim God tafaram sinaf mamatar ana veya, God ana yawas wa’iwa’irin, ana fair wanatowanin naatu i ana itinin etei i sawar sinaf himamataramaim bebeyah hi’itan hiso’ob, imih boro men yait ta God su’ubina’e nao nifufuwenamih.
21 Ngakhale iwo anadziwa Mulungu, sanamulemekeze ngati Mulungu kapena kumuthokoza, koma maganizo awo anasanduka wopanda pake ndipo mʼmitima yawo yopusa munadzaza mdima.
21 Nati sabuw i God hisu’ub, baise men kafa’imo God hirouw tebora’ara’ah, o merarayow tibitinimih. Nati efanin i hai not bonawiyih kwarikwarisen wanawanan hirun dogoroh eowarar naatu gugumafut.
22 Ngakhale ankadzitama kuti ndi anzeru, anasanduka opusa.
22 Basit i not wairafih hirouw teo, baise hai not botabir hina koko’aw na’atube himatar,
23 Iwo anasinthanitsa ulemerero wa Mulungu wosafa ndi mafano opangidwa ndi manja wooneka ngati munthu amene amafa, kapena ngati mbalame, ndi nyama kapena zokwawa.
23 God morob atin bonamanamarin kwafirina’e i hitatabir orot hai yumatabe o mamu, o harufor, uma’ar, kok, i hai yumatabe hitar hima tekwakwafirih.
24 Nʼchifukwa chake Mulungu anawasiya kuti azingochita zilakolako zochititsa manyazi zauchimo zomwe mitima yawo inkafuna. Zotsatira zake anachita za chiwerewere wina ndi mnzake kunyazitsa matupi awo.
24 Isan imih God nati sabuw ihamiyih hitit bowabow kakafih ta ta wanawanan hirun. Dogoroh ana kok na’atube tisisinaf, orot baibin hai faifuw hikwahir naatu baibin ibo orot hai ar hikwahir taiyuwih hi’in hisesebar biyah tebobokarikarit.
25 Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni.
25 Turobe God nowan i hibotabir efanin baifuwen hiyari’iy, naatu God Sawar Sinafuyan kwafirina’e, hitatabir sawar i sinaf himamatar hai fair babahimaim hirun hikwafirih isah tebowabow. Baise ana gewasin sabuw i God akisinamo hitakwafir hitabora’ara’ah wanatowan, wanatowan, Amen.
26 Chifukwa cha ichi, Mulungu anawasiya kuti azitsata zilakolako zochititsa manyazi. Ngakhale akazi omwe anasiya machitidwe achibadwidwe pa za ukwati, namachita machitidwe ena otsutsana ndi chibadwa chawo.
26 Ana an iti isan God ihamiyih insesebar naniyan kakafin anababatun hibai tisisinaf. Baibin oro’orot hai ar hikwahir, i taiyuwih hi’in tibisesebar kwanekwan.
27 Chimodzimodzinso amuna analeka machitidwe a ukwati ndi akazi nʼkumakhumbana amuna okhaokha. Amuna ankachita zochitisa manyazizi ndi amuna anzawo, ndipo analandira chilango choyenera molingana ndi zochita zawo zachitayikozo.
27 Ef nati ta’imon oro’orot auman baibin hai faifuw hikwahir i taiyuwih baisesebar isan tibifi’afi. Naatu oro’orot taiyuwih hi’in tibisesebar kwanekwan. Ana an nati isan i taiyuwih hai kakafinamaim baimakiy tebaib.
28 Ndipo popeza anaona kuti nʼchopanda nzeru kumvera Mulungu, Iye anawasiya kuti atsatire maganizo achitayiko kuti achite zosayenera kuchitazo.
28 Anayabin sabuw God ana so’ob anababatun bain isan hai not kowarar naatu hirutawiy, imih God ihamiyih hitit not kwarikwarisen hibai hima kakafih men hitasisinaf i hima tisisinaf.
29 Iwo ndi odzazidwa ndi mtundu uliwonse wa makhalidwe oyipa, zonyansa, umbombo ndi dumbo. Iwo ndi odzazidwa ndi kaduka, kupha, mikangano, chinyengo ndi udani. Iwowo ndi amiseche,
29 Dogoroh wanawanan bowabow kakafih ta ta etei awan karatan: not kakafih, kabat, tafa’asar, bobowen, sabuw rouw morob; baiyow, baifufuwen, nuw okwanekwan, yanuw,
30 osinjirira, odana ndi Mulungu, achipongwe, odzitama ndi odzitukumula. Iwo amapeza njira zochitira zoyipa. Samvera makolo awo,
30 koutabitabir, God baifa’ifa’in, kakaf en, nuw furuwen, ora’ara’at, naatu bowabow kakafih sinaf isan hai ef boubuh tibimamataren. Naatu hinah tamah fanah tibifanasair.
31 alibe nzeru, chikhulupiriro, sakhudzidwa mu mtima ndipo ndi ankhanza.
31 Nati sabuw i hai naniyan en, aurih bosunusunub en, yabow, baiwan babanen en.
32 Ngakhale kuti amadziwa chiweruzo cholungama cha Mulungu chakuti amene amachita zinthu zotere amayenera imfa, iwo sangopitiriza chabe zimenezi, koma amavomerezanso amene amazichita zimenezi.
32 Naatu God ana ofafaramaim sabuw iti na’atube hinasisinaf isan hinamomorob i hiso’ob, baise i hima kakafin tisisinaf. Naatu sabuw afa bowabow iti na’atube tisisinaf auman isah i baibasit hitih hima tisisinaf.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.