Romanos 15
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ife amene tili ndi chikhulupiriro champhamvu tiziwalezera mtima anthu ofowoka, ndipo tisamadzikondweretse tokha.
1 It iyab ata baitumatum fairih karam ata ofonah hai baitumatum ririmin tanibaisih hai bit turin tanab. Men akisit isat tananot taniyasisiramih.
2 Aliyense wa ife akondweretse mnzake pomuchitira zabwino zomulimbikitsa.
2 Naatu tanabow ata ofonah hiniyasisir, naatu tanibaisih hai baitumatum nawowab nayen.
3 Pakuti ngakhale Khristu sanadzikondweretsa yekha koma, monga kwalembedwa kuti, “Chipongwe cha anthu okunyozani chinagwera Ine.”
3 Keriso i men taiyuwin ana yasisir isan bowamih. Baise nati efanin, Buk Atamaninamaim iti na’atube eo na’atube sinaf. “Sabuw iyab tur kakafih hi’u hibi’a’akir ana bit etei ayu tafau yan re.”
4 Pakuti zilizonse zimene zinalembedwa kale zinalembedwa kuti zitiphunzitse ife. Malembawo amatilimbikitsa kupirira kuti tikhale ndi chiyembekezo.
4 Anayabin tur abisa marasika hikikirum i bai’obaiyit isan, saise nawawainabit ana veya, nati Buk Atamanin ana turamaim koufair tanab nuhit nafot tanama.
5 Mulungu amene amapereka kupirira ndi chilimbikitso akupatseni maganizo amodzi pakati panu monga inu mukutsatira Khristu Yesu,
5 God koufair naatu yatenub ana matuwan, isan ayoyoyoban i boro a kou’ay nita’imon, Jesu Keriso kwani’ufunun.
6 kotero kuti ndi mtima umodzi ndi movomerezana mulemekeze Mulungu ndi Atate a Ambuye athu Yesu Khristu.
6 Naatu dogor ta’imon namatar auta’imon fana kwanabora’ah God, ata Regah Jesu Keriso Tamah ana merar kwanay kwanabora’ara’ah.
7 Tsopano landiranani wina ndi mnzake, monganso Khristu anakulandirani inu, ndi cholinga choti Mulungu alemekezeke.
7 Taituwa hai merar kwanay kwanabuwih, Keriso a merar yi bubuwi na’atube. Saise bora’a’araten God kwanitin niyasisir.
8 Chifukwa kunena zoona, Khristu wasanduka mtumiki wa Ayuda, kuonetsa kuti Mulungu ndi wokhulupirika pa malonjezo amene anachita kwa makolo awo
8 A tur ao’owen, Keriso i na Jew sabuw hai bai’akirayan orot matar, God ana tur gewasin isan bow, ana omatanen uwatanah wabih gagamin itih hikirum inu’in sinaf na yabin matar.
9 kuti a mitundu ina atamande Mulungu chifukwa cha chifundo chake. Monga kwalembedwa kuti,
9 Saise Eteni Sabuw God hitabora’ara’ah i ana kabeber isan. Buk Atamaninamaim hikikirum na’atube
10 Akutinso,
10 Ibanak eo maiye;
11 Ndipo akutinso,
11 Naatu iban maiye eo,
12 Ndiponso Yesaya akuti,
12 Naatu iban Isaiah eo maiye,
13 Mulungu amene amatipatsa chiyembekezo adzaze mitima yanu ndi chimwemwe ndi mtendere pamene mukumudalira Iye, kuti chiyembekezo chanu chisefukire mwamphamvu ya Mzimu Woyera.
13 Ayoyoyoban abaitumatumamaim God nuhifot bit i yasisir naatu tufuw nit, saise Anun Kakafiyin ana fairamaim yasisir ebit dogor wanawanan awan nakaratan nakarsuwai nare.
14 Abale anga, ine mwini ndikutsimikiza kuti inuyo ndinu abwino, odzaza ndi chidziwitso ndi okhoza kulangizana wina ndi mnzake.
14 Taitu ayu aso’ob, kwa a gewasin i ra’at, naatu so’ob tutufin etei kwabai karam, imih karam taituwa boro kwani’obaiyih.
15 Ine ndakulemberani inu molimba mtima pa fundo zina, kukhala ngati kukukumbutsaninso za zimenezo, chifukwa cha chisomo chimene Mulungu anandipatsa ine
15 Baise iti fef wanawanan i sawar gagamih afa bebeyan a tur ao’owen saise nuhi anakusib. Anayabin God ana gewasin ayu wanawana’umaim yari’iy
16 kukhala mtumiki wa Khristu Yesu wa a mitundu ina ndi udindo wa wansembe, kulalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu, kuti a mitundu ina akhale nsembe yolandiridwa kwa Mulungu, yopatsidwa ndi Mzimu Woyera.
16 Keriso ana akir orot amatar Ufun Sabuw isah anabowamih. Naatu firis na’atube anabow God ana Tur Gewasin anao’orerereb. Saise Ufun Sabuw hinan siwar na’atube hinamatar God hai merar nay nabuwih, naatu Anun Kakafiyin nakusouwih kakafiyih hinamatar.
17 Choncho, ine ndikunyadira mwa Khristu Yesu potumikira Mulungu wanga.
17 Isan imih au bowabow God isan, Jesu Keriso wanawananamaim abowabow i abiyasisir gagamin maiyow.
18 Ine sindidzayesera kuyankhula za kanthu kalikonse koma zimene Khristu wazichita kudzera mwa ine zotsogolera a mitundu ina kuti amvere Mulungu mwa zimene ndinanena ndi kuzichita
18 Anayabin iti isan ayu boro men kafa’imo sawar afa isah anao’omih. Baise abisa Keriso iyunu ao naatu abow Ufun Sabuw abonawiyih hina God tebobosiyasiyar akisinamo boro anao.
19 mwamphamvu ya zizindikiro ndi zodabwitsa kudzera mwamphamvu ya Mzimu Woyera. Choncho kuchokera ku Yerusalemu ndi kuzungulira ku Iluriko, ine ndalalikira kwathunthu Uthenga Wabwino wa Khristu.
19 Anun Kakafiyin ana fairamaim, ina’inan naatu baifofofor fokarih himatar. Jerusalem imaim au nanawan abusuruf God ana tur abinan aremor ana tafaram wabin Ikonium atit.
20 Chakhala chilakolako changa nthawi zonse kuti ndilalikire Uthenga Wabwino kumene Khristu sadziwika, kuti ine ndisamange pa maziko a wina wake.
20 Akokok kwanekwan efan menamaim Keriso ana tur men hinonowar imaim anabinan hinanowar. Anayabin ayu men bar wowabayan orot boro orot ta ana bar bubu rarouw nonowatin tafanamaim anawowab.
21 Koma monga kwalembedwa kuti,
21 Bukamaim hikikirum na’atube,
22 Ichi nʼchifukwa chake ine ndakhala ndikuletsedwa kawirikawiri kubwera kwa inu.
22 Ana’an nati isan ayu kwa isa namih mar etei ayu hirorowenbibiru.
23 Koma tsopano popeza kulibenso malo anga woti ndigwire ntchito mʼmadera awa, ndakhala ndikufuna kukuonani kwa zaka zambiri.
23 Baise boun efan iti wanawanan ayu au bowabow i sawar naatu kwamur manin maiyow akok kwanekwan atan ata’iti isan ama akakaibababan.
24 Ine ndikukonza kuti nditero pamene ndipita ku Spaniya. Ine ndikuyembekeza kudzakuchezerani pamene ndikudutsa ndi kuti inu mudzathandize popitiriza ulendo wanga, nditasangalala ndi kukhala nanu kwa kanthawi.
24 Imih bounabo anotanot boro anan ana’iti. Spain bainanawan isan ananan founamaim boro anarun ana’iti.
25 Koma tsopano, ine ndili pa ulendo wopita ku Yerusalemu potumikira oyera mtima akumeneko.
25 Boun i ayu au Jerusalem anan God ana sabuw hai bowabow ta ta isan.
26 Pakuti kunakomera a ku Makedoniya ndi a ku Akaya kupereka thandizo kwa osauka pakati pa oyera mtima mu Yerusalemu.
26 Ekalesia sabuw nati Masedonia naatu Akaiya wanawanan Jerusalem sabuw yababan wairafih hai tur hinonowar i yasisir auman baibaisih isan hai siwar kaifai hiyai.
27 Iwo chinawakomera kuchita ichi, ndipo ndithu anali ndi ngongole kwa iwo. Pakuti ngati a mitundu ina anagawana ndi Ayuda madalitso auzimu, iwo ali ndi ngongole kwa Ayuda kuti agawane nawo madalitso awo a ku thupi.
27 Iti sinaf isan i hiyasisir, naatu kabay hiyai hibiyafar ana itinin i wayow na’atube hisinaf. Anayabin Jew sabuw ayubih ana baigegewasin i wan Ufun Sabuw hifaramih bairi hibai.
28 Tsono ine nditamaliza ntchito iyi ndi kutsimikiza kuti alandira chipatsochi, ndidzadzera kwanuko kudzakuchezerani pa ulendo wanga popita ku Spaniya.
28 Imih ayu bowabow anisawar hai siwar kafai abai anan anitih. Imaibo au Spain ananan ef aumatan boro anarun ana’itibo anan.
29 Ine ndikudziwa kuti pamene ndidzabwera kwa inu, ndidzafika ndili wodzaza ndi madalitso a Khristu.
29 Ayu kwa isa ananan, i aso’ob Keriso ana baigegewasin tutufin etei boro auman anan.
30 Abale, ine ndikukupemphani, mwa Ambuye athu Yesu Khristu ndi mwachikondi cha Mzimu, kuti mukhale nane pa kulimbika kwanga pondipempherera kwa Mulungu.
30 Taitu, abifefeyani ata Regah Jesu Keriso wabinamaim naatu Anun Kakafiyin ana yabowamaim au biyababanamaim kwanikofan naatu isou kwanayoyoban God nibaisu.
31 Pempherani kuti ine ndilanditsidwe kwa osakhulupirira a ku Yudeya ndi kuti utumiki wanga mu Yerusalemu ukhale ovomerezeka ndi oyera mtima.
31 Kwanayoyoban saise Eteni Sabuw Judea wanawanan tema’am umahine God natafafaru naatu God ana sabuw Jerusalemamaim tema’am au bowabow isan hiniyasisir au merar hinay.
32 Kuti mwachifuniro cha Mulungu ndibwere kwa inu ndi chimwemwe kuti ndidzapumule pamodzi ndi inu.
32 Saise God nakokok na’at ayu boro ereyasisir ana matabir maiye not boubun auman anan kwa aninanawani.
33 Mulungu wamtendere akhale ndi inu nonse. Ameni.
33 Tufuw ana God kwa etei isa nama wanatowan. Amen.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 15, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.