Romanos 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Aliyense ayenera kumvera akulu olamulira, chifukwa palibe ulamuliro umene sunachokere kwa Mulungu. Olamulira amene alipo anayikidwa ndi Mulungu.
1 Kwa etei a aiwob kwanakakafiyih, anayabin roubabaruwen ana fair etei i Godane na orot bai. Naatu iti aiwob ana fair etei i God taiyuwin imatar.
2 Kotero kuti, iwo amene awukira ulamuliro atsutsana ndi chimene Mulungu anakhazikitsa. Ndipo amene atero adzibweretsera okha chilango.
2 Isan imih o yait aiwob orot kukwakwahir, o i God abisa bimatar kukwakwahir. Naatu sabuw iyab nati na’atube tisisinaf i taiyuwih babah teo’o.
3 Pakuti olamulira saopseza amene amachita zabwino koma amene amachita zoyipa. Kodi mukufuna kukhala osaopa olamulira? Tsono chitani zoyenera ndipo adzakuyamikirani.
3 Anayabin sabuw iyab gewasin tisisinaf bonawiyenayah isah boro men hinabir, baise kakafih sinafuyah boro hinabir.
4 Pakuti iyeyo ndi mtumiki wa Mulungu wokuchitirani zabwino. Koma ngati muchita zoyipa muchite mantha, pakuti iye ali ndi mphamvu zolangira. Iye ndi mtumiki wa Mulungu wobweretsa mkwiyo ndi kulanga onse ochita zoyipa.
4 Anayabin orot ukwarih i God ana’akir wairafih, kwa ama gewas isan tebowabow. Baise kakafin kwanasisinaf na’at i kwanabir, anayabin orot ukwarin sabuw baimakiyih isan ana fair God bitin i ema’am boro baimakiy nitih.
5 Nʼchifukwa chake ndi koyenera kugonjera olamulira, osati chifukwa choopa kulangidwa kokha komanso chifukwa cha chikumbumtima.
5 Isan imih, a orot ukwarih i kwanakakafiyih, anayabin nati kwasisinaf ebi’obaiyi i sawar gewasin, men baimakiy akisin isan kwanabir kwanakakafamih.
6 Ichi nʼchifukwa chakenso inu mumapereka msonkho. Pakuti olamulira ndi atumiki a Mulungu amene amapereka nthawi yawo yonse kulamulira.
6 Ana’an nati isan kwa kabay kwaya’aya, anayabin God ana bai’akirayah i faimar iti sawar isah tebowabow.
7 Mubwezereni aliyense amene munamukongola. Ngati inu muli ndi ngongole yamsonkho, perekani msonkho kwa oyenera kuwalipira. Ngati ndi kuopa perekeni kwa oyenera kuwaopa ndipo ngati ndi ulemu kwa oyenera ulemu.
7 Orot babin hai bit abisa biya ema’am kwanitih abit kwanikisisir, kabay ana bit kabay kwanayai, tura ana sawar biyamaim ana bit kua’abar wan inay maiye, isa tekakaf ibo isah inakakaf, tirurusagiyi ibo inarusagiyih.
8 Musakhale ndi ngongole ndi wina aliyense kupatula ngongole ya kukondana wina ndi mnzake. Pakuti amene amakonda munthu mnzake wakwaniritsa lamulo.
8 A bit sabuw biyahimaim tema’am etei kwanibaiyan nasawar, men kwanihamiyen hinama’amih. Bit ta’imon biyamaim nama’am i yabow akisin, taituwa bairi kwaniyabowbonen kwanama, anayabin orot yait taituwan ebiyabow i ofafar eo na’atube sinaf yabin emamatar.
9 Malamulo awa: “Usachite chigololo,” “Usaphe,” “Usabe,” “Usasirire,” ndi malamulo ena onse amene alipo, akhazikika pa lamulo limodzi ili, “Konda mnansi wako monga iwe mwini.”
9 Ofafar i iti, “Turanah a’aawah men ufuh inan, sabuw men ina’asbunubuw, men inabain, men inabahiy, naatu ofafar afa iti na’atube etei i iti ofafar suma’ay, taituwa iniyabuwih o taiyuw kubiyabuw na’atube.
10 Chikondi sichichitira mnzake zoyipa. Chifukwa chake chikondi ndicho chokwaniritsa lamulo.
10 Yabow taintuwan men ebiyababan. Isan imih yabow i abisa ofafar eo na’atube i sinaf yabih temamatar.
11 Ndipo chitani ichi pozindikira nthawi ino. Nthawi yafika yoti inu mudzuke kutulo, chifukwa chipulumutso chathu chili pafupi tsopano kuposa pamene tinayamba kukhulupirira.
11 Naatu sinaf iti kwanasinaf, abisa iti boun ana veya temamatar i kwanaso’ob. In ana veya i sawar, anayabin it yawas bain isan ana veya i na kabom, men marasika tabitumatum na’atube.
12 Usiku watsala pafupifupi kutha. Kwatsala pangʼono kucha. Tiyeni tsono tichotse ntchito zamdima ndipo tivale chovala chakuwunika.
12 Gugumin i kafa’imo nasawar, mar i boro’omo natoririb. Isan imih gugumin ana bowabow i tanihamiyen, naatu tanamisir marakawamaim ma isan taniyow.
13 Tiyeni tikhale moyenera monga nthawi ya masana, osati mʼmagulu amadyerero, achiwerewere ndi kuledzera, mʼmadama ndi zonyansa komanso osati mʼmagawano ndi nsanje.
13 Bowabow gewasin mar ana efamaim tanasinaf, men aatom, gamin, harew tom baikoko’aw, baiwa’an kwanekwan, baiyow, naatu baibobowen.
14 Koma valani Ambuye Yesu Khristu ndipo musaganizire za momwe mungakwaniritsire zokhumba zachikhalidwe cha uchimo.
14 Baise Jesu Keriso kwanab a faifuwamih kwaniyoun, saise boro men biya ana kok susuwin isan ana ef kwananuwetamih.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 13, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.