Romanos 12
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Nʼchifukwa chake ine ndikukupemphani abale, mwa chifundo cha Mulungu, kuti mupereke matupi anu monga nsembe yamoyo, yopatulika ndi yokondweretsa Mulungu. Nsembeyi ndiye kupembedza kwanu kwa uzimu.
1 Isan imih taituwau, God ana kabeber ai’itin i ra’at kwanekwan, imih abifefeyani, kwa biya yawasin i kwanaya’asair God ana siboromih kwanitin. Nati sibor i kakafiyin naatu God ana yasisir, anayabin nati i ayubit ana kwafiren ef anababatun.
2 Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro.
2 Men tafaram ana yawasamaim nabonawiyi, baise God kwanifefeyan a not tutufin etei nabotabir niboubun. Imaibo kwa i karam God ana kok abisa boro kwanafufun gewas, i ana gewasin, ana yasisir naatu ana kok uhewbitan boro kwanaso’ob.
3 Chifukwa cha chisomo chopatsidwa kwa ine, ndinena kwa aliyense wa inu kuti musadziyenereze nokha kuposa mmene mulili. Koma mudziganizire nokha modzichepetsa, molingana ndi muyeso wa chikhulupiriro chimene Mulungu wakupatsani.
3 Manaw kabeber God ayu bitu imaim kwa au’uwi. Men taiyuw a notamaim nabora’ahi me’at, baise a not narumutufur gewas kwa a baitumatum God bit anafofonin imaim kwanabatkikin.
4 Pakuti monga aliyense wa ife ali ndi thupi limodzi koma ziwalo zambiri, ziwalozi sizili ndi ntchito yofanana.
4 Biyat i sawar maumurih na’in baina ikokofan wowab biyat matar. Naatu biyat wanawanan ana wowab ta ta i bowabow ta ta tebowabow.
5 Momwemonso mwa Khristu ife amene tili ambiri tipanga thupi limodzi ndipo chiwalo chilichonse ndi cholumikizika ku chinzake.
5 It i moumurit na’in, baise Keriso’one it etei tana biyat ta’imon matar. Naatu ta’ita’imon ikokofanit tana biyat ta’imon tutufin matar.
6 Ife tili ndi mphatso zosiyana, molingana ndi chisomo chopatsidwa kwa ife. Ngati mphatso ya munthu ndi kunenera, musiyeni ayigwiritse ntchito molingana ndi chikhulupiriro chake.
6 Isan imih manaw kabeberamaim ata siwar ta ta tabow. O ta a siwar God ana tur orereb isan na’at, a baitumatum ana fofoninamaim inabat inaorerereb.
7 Ngati ndi kutumikira, musiyeni atumikire. Ngati ndi kuphunzitsa, musiyeni aphunzitse.
7 God ana bowabow isan nabit na’at inabow, bai’obaiyen isan na’at ini’obaibiyen.
8 Ngati ndi kulimbikitsa, musiyeni alimbikitse. Ngati ndi kupereka kuthandiza osowa, musiyeni apereke mowolowamanja. Ngati ndi utsogoleri, musiyeni alamulire mosamala. Ngati ndi kuonetsa chifundo, musiyeni achite mosangalala.
8 Koufair na’at, sabuw koufair nitih, bosemorayan na’at, ereyasisir nabosemor, bonawiyenayan na’at, na’abar totofar sabuw nabonawiyih, kabeberayan na’at, erekawasa isah nasinaf.
9 Chikondi chikhale chopanda chinyengo. Dana nacho choyipa; gwiritsitsa chabwino.
9 Yabow i turobe’emaim iniyabow, abistan kakafih inarukouw, naatu abisa gewasih inabukikin.
10 Mukondane kwathunthu monga abale. Lemekezanani wina ndi mnzake kuposa inu eni.
10 Kirisiyan ana yabowamaim taituwa isah iniyabow, naatu taituwa bairi nena kwanikakafbonen.
11 Musakhale aulesi mʼmachitidwe anu. Khalani achangu mu mzimu ndipo tumikirani Ambuye.
11 Sunanub kwanabow men kwananokow, Regah isan dogor tutufin etei yoyobanamaim kwanabow.
12 Kondwerani mʼchiyembekezo, pirirani mʼmasautso ndiponso khulupirikani mʼpemphero.
12 Ereyasisir nuhi nafot kwanama, bai’akir ana veya yatenanub naatu mar etei kwanisnubanub kwanayoyoban.
13 Gawanani ndi anthu a Mulungu amene ali ndi chosowa. Cherezani alendo.
13 Kirisiyan sabuw iyab tibi’akir kwanibaisih, naatu a etawan kwanabotawiy nanawan sabuw isah.
14 Adalitseni amene akuzunzani. Adalitseni ndipo musawatemberere.
14 Sabuw iyab hirab tibia’akiri, God kwanifefeyan nigegewasinih, men nararafihimih
15 Kondwani pamodzi ndi amene akukondwa ndipo lirani ndi amene akulira.
15 Sabuw iyab tibiyasisir bairi kwaniyasisir, naatu sabuw iyab tibiyababan bairi kwaniyababan.
16 Muyanjane wina ndi mnzake. Musakhale onyada, koma lolani kuyanjana ndi anthu wamba. Musaganize kuti mumadziwa zonse.
16 Kou’ayomaim a not etei ta’imon taituwa kwananuhih bairi kwanibit abar kwanama. Men kwa akis notanotayah kwanarouw kwanaora’ara’at taituwa kwanitaiyih. Baise taiyuw kwanayariyi bairi anafofonin kwanaremor, men o akis not wairafi inarouw inao.
17 Musabwezere choyipa ndi choyipa kwa aliyense. Samalitsani kuchita chabwino pamaso pa aliyense.
17 Sabuw o isa kakafin hinasisinaf, men wan inay kakafin isah inasinafumih. Baise yate nanub abisa gewasin sabuw etei matahimaim inasinaf.
18 Ngati nʼkotheka, khalani mwamtendere ndi aliyense monga momwe mungathere.
18 Asinafumaim sawar etei gewasih inasinaf, saise sabuw bairi tufuwamaim kwanama.
19 Okondedwa anga, musabwezere choyipa, koma lekerani Mulungu. Pakuti kwalembedwa, “Kubwezera chilango nʼkwanga. Ndidzawalanga ndine,” akutero Ambuye.
19 Men kafa’imo isa kakafin hinasisinaf isan sa bowamih inanot, baise nati efan inihamiy God ana yaso’ar boro i sa nabow. Anayabin Buk Atamaninamaim iti hikirum, “Ayu boro wan anay, Regah iti na’atube eorereb.”
20 Koma,
20 Naatu Bukamaim iban eo maiye,
21 Musagonjetsedwe ndi choyipa, koma gonjetsani choyipa pochita chabwino.
21 Kakafin men nawasbunimih, baise gewasin inasinaf imaim kakafin inawasabun.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Romanos 12, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.