Oséias 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Iwe Israeli, usakondwere;

2 Malo opunthira tirigu ndi malo opsinyira mphesa sadzadyetsa anthu;

3 Sadzakhalanso mʼdziko la Yehova.

4 Iwo sadzaperekanso chopereka cha chakumwa kwa Yehova,

5 Kodi mudzachita chiyani pa tsiku la maphwando anu oyikika;

6 Ngakhale iwo atathawa chiwonongeko,

7 Masiku achilango akubwera,

8 Mneneri pamodzi ndi Mulungu wanga

9 Iwo azama mu zachinyengo

10 “Pamene ndinamupeza Israeli

11 Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame.

12 Ngakhale atalera ana

13 Ndaona Efereimu ngati Turo,

14 Inu Yehova, muwapatse.

15 “Chifukwa cha zoyipa zawo zonse ku Giligala,

16 Efereimu wathedwa,

17 Mulungu wanga adzawakana

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Oséias 9, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.