Oséias 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Israeli anali mpesa wotambalala;

2 Mtima wawo ndi wonyenga

3 Pamenepo anthuwo adzanena kuti, “Ife tilibe mfumu

4 Mafumu amalonjeza zambiri,

5 Anthu amene amakhala mu Samariya akuchita mantha

6 Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya

7 Samariya ndi mfumu yake adzatengedwa kupita kutali

8 Malo opembedzerako mafano a ku Aveni adzawonongedwa.

9 “Iwe Israeli, wachimwa kuyambira mʼmasiku a Gibeya,

10 Pamene ndifunire, ndidzalanga anthuwo;

11 Efereimu ndi mwana wangʼombe wamkazi wophunzitsidwa

12 Mufese nokha chilungamo

13 Koma inu munadzala zolakwa,

14 phokoso lankhondo lidzamveka pakati pa anthu anga

15 Momwemonso zidzakuchitikira, iwe Beteli

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Oséias 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.