Neemias 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs BKJ

Sair da comparação
1 Pambuyo pake Eliyasibu mkulu wa ansembe ndi ansembe anzake anayamba kugwira ntchito ndipo anamanganso Chipata cha Nkhosa. Iwo anachipatulira Mulungu ndipo anayika zitseko zake. Khoma limene analipatula linafika mpaka pa Nsanja ya Zana ndi Nsanja ya Hananeli.
1 E Eliasibe, o sumo sacerdote, levantou-se com os seus irmãos, os sacerdotes, e edificaram o portão das ovelhas, o qual santificaram, e levantaram as suas portas; até a Torre de Meá eles o santificaram, e até a Torre de Hananel.
2 Anthu a ku Yeriko anamanga chigawo china pambali pake ndipo Zakuri mwana wa Imuri anamanga chigawo chinanso choyandikana nawo.
2 E próximo a ele edificaram os homens de Jericó. E próximo deles edificou Zacur, o filho de Inri.
3 Chipata cha Nsomba chinamangidwanso ndi ana a fuko la Hasena. Iwo anayika mitanda yake ndi zitseko, zotsekera zake, ndi mipiringidzo yake.
3 Todavia, os filhos de Hassenaá edificaram o portão do peixe que também lançaram as suas vigas, e puseram as suas portas, as suas trancas, e as suas barras.
4 Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi, anakonza chigawo choyandikana nacho. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya, mwana wa Mesezabeli anakonza chigawo china. Pambali pake, Zadoki mwana wa Baana anakonzanso chigawo china.
4 E próximo a eles reparou Meremote, o filho de Urias, o filho de Coz. E próximo a eles reparou Mesulão, o filho de Berequias, o filho de Mesezabel. E próximo a eles reparou Zadoque, filho de Baaná.
5 Pambali pa iwowa anthu a ku Tekowa anakonza chigawo china. Koma wolemekezeka awo anakana kugwira ntchito imene akuluakulu awo anawapatsa.
5 E próximo a eles os tecoítas repararam; mas os seus nobres não puseram o seu pescoço na obra do seu senhor.
6 Chipata cha Yesana chinakonzedwa ndi Yoyada mwana wa Paseya ndi Mesulamu mwana wa Besodeya. Iwo anayika mitanda yake ndi kuyika zitseko, zotsekera zake ndi mipiringidzo yake.
6 E o portão velho repararam Joiada, filho de Paseia; e Mesulão, o filho de Besodias; eles puseram as suas vigas, e levantaram as suas portas, e as suas travas, e as suas barras.
7 Pambali pawo Melatiya Mgibeyoni ndi Yadoni Mmerenoti ndiponso anthu a ku Gibiyoni ndi a ku Mizipa anakonza chigawo chawo mpaka ku nyumba ya bwanamkubwa wa chigawo cha Patsidya pa Yufurate.
7 E próximo deles repararam Melatias, o gibeonita, e Jadom, o meronotita, os homens de Gibeão, e de Mispá, até o trono do governador deste lado do rio.
8 Pambali pawo Uzieli mwana wa Harihaya wa mʼgulu amisiri osula golide anakonzanso chigawo china. Pambali pake Hananiya mmodzi mwa anthu oyenga mafuta onunkhira, anakonzanso chigawo china. Iwo anakonzanso Yerusalemu mpaka ku Khoma Lotambasuka.
8 Próximo a ele repararam Uziel, o filho de Haraías, dos ourives. Próximo a ele também reparou Hananias, o filho de um dos apotecários, e eles fortificaram Jerusalém até a muralha larga.
9 Refaya mwana wa Huri wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu anakonza chigawo china motsatana nawo.
9 E próximo a eles reparou Refaías, o filho de Hur, o governante da metade de Jerusalém.
10 Kulumikiza ichi, Yedaya mwana wa Harumafi anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba yake, ndipo Hatusi mwana wa Hasabaneya anakonzanso motsatana naye.
10 E próximo a eles reparou Jedaías, o filho de Harumafe, a saber, na frente da sua casa. E próximo a ele reparou Hatus, o filho de Hasabneias.
11 Malikiya mwana wa Harimu ndi Hasubu mwana wa Pahati-Mowabu anakonzanso chigawo china ndiponso Nsanja ya Ngʼanjo.
11 Malquias, o filho de Harim, e Hassube, o filho de Paate-Moabe, repararam a outra parte, e a torre das fornalhas.
12 Salumu mwana wa Halohesi wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu, anakonzanso chigawo chotsatana nawo mothandizidwa ndi ana ake akazi.
12 E próximo a ele reparou Salum, o filho de Haloés, o governante da metade de Jerusalém, ele e as suas filhas.
13 Chipata cha ku chigwa chinakonzedwa ndi Hanuni ndi anthu okhala ku Zanowa. Iwo anachimanganso ndi kuyika zitseko zake ndi zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iwo anakonzanso khoma lotalika mamita 450 mpaka ku Chipata cha Zinyalala.
13 Hanum, e os habitantes de Zanoa repararam o portão do vale; eles o edificaram, e puseram as suas portas, as suas trancas, e as suas barras, e mil côvados da muralha até o portão do esterco.
14 Chipata cha Zinyalala chinakonzedwa ndi Malikiya mwana wa Rekabu, wolamulira chigawo cha Beti-Hakeremu. Iye anachimanganso ndi kuyika zitseko zake, zotsekera zake ndi mipiringidzo.
14 Mas, o portão do esterco reparou Malquias, o filho de Recabe, o governante de parte de Bete-Haquerém; ele o edificou, e pôs as suas portas, as suas travas, e as suas barras.
15 Chipata cha Kasupe chinakonzedwa ndi Saluni mwana wa Koli-Hoze, wolamulira chigawo cha Mizipa. Iye anachimanganso ndi kuyikanso denga ndiponso zitseko, zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iye anakonzanso khoma la Dziwe la Siloamu limene lili pafupi ndi munda wa mfumu mpaka ku makwerero otsikira potuluka mzinda wa Davide.
15 Mas o portão da fonte reparou Salum, o filho de Col-Hozé, o governante de parte de Mispá; ele o edificou, e o cobriu, e pôs as suas portas, as suas travas, e as suas barras, e a parede do tanque de Siloá junto ao jardim do rei, e até as escadarias que descem da cidade de Davi.
16 Pambali pa iyeyo, Nehemiya mwana wa Azibuki, wolamulira theka la chigawo cha Beti Zuri anakonza chigawo china mpaka kumalo oyangʼanana ndi manda a Davide, mpaka ku dziwe lokumba ndi ku nyumba ya anthu ankhondo.
16 Depois dele reparou Neemias, o filho de Azbuque, o governante da metade de Bete-Zur, até o local defronte aos sepulcros de Davi, e até o tanque que foi feito, e até a casa dos poderosos.
17 Pambali pake Alevi anakonza chigawo china, ndipo mtsogoleri wawo anali Rehumi mwana wa Bani. Pambali pa iye Hasabiya wolamulira theka la chigawo cha Keyila anagwira ntchito ku chigawo chake.
17 Depois dele repararam os levitas, Reum, o filho de Bani. Próximo a ele reparou na sua parte Hasabias, o governante da metade de Queila.
18 Pambuyo pa iyeyu abale awo anapitiriza kukonza, ndipo mtsogoleri wawo anali Bawai mwana wa Henadadi, wolamulira theka lina la chigawo cha Keyila.
18 Depois dele repararam os seus irmãos, Bavai, o filho de Henadade, o governante da metade de Queila.
19 Motsatana naye Ezeri mwana wa Yesuwa, wolamulira Mizipa anakonza chigawo chinanso choyangʼanana ndi chikweza chofikira ku nyumba yosungira zida za nkhondo pa ngodya.
19 E próximo a ele reparou Ezer, o filho de Jesuá, o governante de Mispá, outra parte defronte da subida até a casa das armas na esquina da muralha.
20 Motsatana naye, Baruki mwana wa Zakai anakonzanso chigawo china kuchokera pa ngodya mpaka pa chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe.
20 Depois dele, Baruque, o filho de Zabai, reparou diligentemente a outra parte, desde a esquina da muralha até a porta da casa de Eliasibe, o sumo sacerdote.
21 Motsatana naye, Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi anakonzanso chigawo china kuchokera ku chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mpaka kumapeto kwake.
21 Depois dele reparou Meremote, o filho de Urias, o filho de Coz, outra parte, desde a porta da casa de Eliasibe até a extremidade da casa de Eliasibe.
22 Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china.
22 E depois dele repararam os sacerdotes, os homens da planície.
23 Pambuyo pawo, Benjamini ndi Hasubu anakonza kutsogolo kwa nyumba zawo. Ndipo motsatana nawo, Azariya mwana wa Maaseya mwana wa Ananiya, anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba zawo.
23 Depois dele repararam Benjamim e Hasube defronte da sua casa. Depois dele reparou Azarias, o filho de Maaseias, o filho de Ananias, por sua casa.
24 Motsatana naye, Binuyi mwana wa Henadadi anakonzanso chigawo china, kuchokera pa nyumba ya Azariya kukafika potsirizira pa ngodya.
24 Depois dele reparou Binui, o filho de Henadade, outra parte, desde a casa de Azarias até a esquina da muralha, a saber, até o canto.
25 Palali mwana Uzai anakonza chigawo china choyangʼanana ndi ngodya ndi nsanja yotuluka pa nyumba yapamwamba ya mfumu ku bwalo la alonda. Motsatana naye, Pedaya mwana wa Parosi,
25 Palal, o filho de Uzai, defronte à esquina da muralha, e da torre que se eleva da casa alta do rei, que estava junto ao átrio da prisão. Depois dele, Pedaías, o filho de Parós.
26 ndi otumikira mʼNyumba ya Mulungu amene amakhala pa khoma la Ofeli anakonza chigawo china mpaka pa malo oyangʼanana ndi Chipata cha Madzi kuloza kummawa ndiponso nsanja yayitali ija.
26 Além disso, os netineus habitaram em Ofel, até o local defronte ao portão das águas na direção leste, e até a torre que ali se ergue.
27 Motsatana nawo, anthu a ku Tekowa anakonzanso chigawo china choyangʼanana ndi nsanja ija yayikulu ndi yayitali mpaka ku khoma la Ofeli.
27 Depois, os tecoítas repararam outra parte, defronte da grande torre que se ergue, até a muralha de Ofel.
28 Kuyambira ku Chipata cha Akavalo anakonza ndi ansembe ena ndipo aliyense amakonza khoma loyangʼanana ndi nyumba yake.
28 Acima do portão do cavalo repararam os sacerdotes, cada um defronte à sua casa.
29 Motsatana nawo, Zadoki mwana wa Imeri anakonza chigawo china choyangʼanana ndi nyumba yake. Motsatana naye, Semeya mwana wa Sekaniya, mlonda wa Chipata cha Kummawa, anakonzanso khoma.
29 Depois, reparou Zadoque, o filho de Imer, defronte à sua casa. Depois dele também reparou Semaías, o filho de Secanias, o guarda do portão leste.
30 Hananiya mwana wa Selemiya ndiponso Hanuni mwana wachisanu ndi chimodzi wa Zalafi anakonza chigawo china. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya anakonza chigawo choyangʼanana ndi chipinda chake.
30 Depois dele repararam outra parte Hananias, o filho de Selemias, e Hanum, o sexto filho de Zalafe. Depois dele reparou Mesulão, o filho de Berequias, defronte da sua câmara.
31 Motsatana naye, Malikiya mmodzi mwa amisiri a golide anakonza chigawo china mpaka ku nyumba ya atumiki a ku Nyumba ya Mulungu ndiponso ku nyumba ya anthu amalonda moyangʼanana ndi chipata cha Mifikade ndiponso mpaka pa chipinda chapamwamba chapangodya.
31 Depois dele reparou Malquias, o filho de um ourives, até o local dos netineus, e dos mercadores, defronte ao portão Mifcade, e até a subida do canto.
32 Ndipo pakati pa chipinda chapamwamba chapangodya ndi Chipata cha Nkhosa anakonza ndi amisiri a golide ndi anthu amalonda.
32 E entre a subida do canto até a porta das Ovelhas repararam os ourives e os mercadores.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Neemias 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.