Mateus 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Musaweruze ena, kuti inunso mungadzaweruzidwe.
1 “Taituwa hai kakafin men ina’itin inibibatiyih, God boro nibatiyi.
2 Pakuti momwe inu muweruzira ena, inunso mudzaweruzidwa chimodzimodzi, muyeso umene muyesera ena inunso mudzayesedwa ndi womwewo.
2 Anayabin God boro ef ta’imon taituwa ibibatiyih na’atube, o boro nibatiy, naatu fufun ta’imon taituwa ifufufunihimaim, o boro nafufuni.
3 “Chifukwa chiyani iwe uyangʼana kachitsotso ka mʼdiso la mʼbale wako koma susamalira chimtengo chili mʼdiso mwako?
3 “Aisim taituwa matah mutusukwar i’itin kikin ku’o naatu o mata ahay gagamin yi ebatabat men kui’itin.
4 Kodi unganene bwanji kwa mʼbale wako kuti, ‘Ndikuchotse kachitsotso mʼdiso mwako,’ pamene nthawi zonse chimtengo uli nacho mʼdiso mwako?
4 O taituwa isan boro mi’itube awa fariniwa’an inao, ‘Aro nekuna mata mutusukwar abosair.’ Naatu baise o mar etei i matan ahay yi ebatabat.
5 Wachiphamaso iwe! Yamba wachotsa chimtengo chili mʼdiso mwako ndipo pamenepo udzatha kuona bwino ndi kuchotsa kachitsotso kali mʼdiso mwa mʼbale wako.
5 Wanawan rerekabih, mat o taiyuw mata a’ahay ina’uy, saise boro inanuw gewas taituwa matan ana ahay ina’uy.
6 “Musapatse agalu zinthu zopatulika; kapena musaponyere nkhumba ngale zanu. Pakuti ngati mutero, zidzaziponda ndipo pomwepo zidzakutembenukirani ndi kukudulani nthulinthuli.
6 “Abisa kakafiyin men haru aninamih kwanitih, boro hinatatabir hinayubi. Naatu a nugunug men for nahimaim kwanarub nare, boro tafan hinayen hinawasu’uru’um.
7 “Pemphani ndipo mudzapatsidwa; funafunani ndipo mudzapeza; gogodani ndipo adzakutsekulirani.
7 “Inafefeyan boro inab, inanuwet boro inatita’ur, naatu inarukikitar etawan boro isa nabotawiy.
8 Pakuti wopempha aliyense amalandira; ndi wofuna amapeza; ndipo iye amene agogoda, adzamutsekulira.
8 Anayabin orot yait efefeyan boro nab, orot yait enunuwet boro natita’ur naatu orot yait erurukikitar etawan boro isan nabotawiy.
9 “Ndani mwa inu, mwana wake akamupempha buledi amamupatsa mwala?
9 “O yait natu, wahimih fefeyan kabay ibai itin ean?
10 Kapena ngati mwana apempha nsomba, kodi amamupatsa njoka?
10 Na’atube siyamih rererey kok ibai itin ean?
11 Tsono ngati inu woyipitsitsa mumadziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, nanga Atate anu akumwamba sadzapereka mphatso zabwino kwa iwo amene amupempha?
11 En baise Kwa i bowabow kakafih sinafuyah, baise kwaso’ob natunat boro siwar gewasih kwanitih, imih Tamat maramaim i ma tainin erubirub orot yait efefeyan boro siwar gewasin nitin.
12 Nʼchifukwa chake zinthu zilizonse mukafuna kuti anthu akuchitireni, yambani ndinu kuwachitira, pakuti izi ndi zimene malamulo ndi aneneri amaphunzitsa.
12 Imih sawar etei taituwa isah inabow, o kukok isa tebowabow na’atube, anayabin Moses ana ofafar naatu dinab oro’orot hai bai’obaiyen an anababatun i iti’imaim ku’ay inu’in.
13 “Lowani pa chipata chopapatiza. Pakuti chipata cholowera kuchiwonongeko nʼchachikulu ndipo msewu wake ndi waukulunso. Ndipo anthu ambiri amalowera pamenepo.
13 “Etawan awan kukurinamaim kwanarun kwan, anayabin etawan awan gagamin, naatu ef awan hahabin inarun inanan yomaninamaim i gurugurusen ema’am naatu sabuw moumurih na’in imaim tenan.
14 Koma chipata ndi chopapatiza ndi msewu ndi waungʼono umene utsogolera anthu ku moyo wosatha ndipo ndi owerengeka okha amene ayipeza njirayo.
14 Baise etawan awan kukurin naatu ef awan tuwafutin inarun inanan yomaninamaim i yawas ema’am, naatu sabuw matan ta’amo imaim tenan.
15 “Chenjerani nawo aneneri onyenga. Amabwera kwa inu atavala zikopa zankhosa, koma mʼkati mwawo ali mimbulu yolusa.
15 “Mata to niwa’an dinab baifufuwenayah hinanan kwana’itih, anayabin hinanan ufuhine ana itinin boro sheep na’atube, baise dogoroh wanawanan ana itinin i haru tuwetuwenih.
16 Mudzawazindikira iwo ndi zipatso zawo. Kodi anthu amathyola mpesa pa mtengo wa minga, kapena nkhuyu pa nthula?
16 Hai bowabowamaim boro kwana’inanih, agor ro’on boro men kiw tafanamaim inima’ub, naatu wanob ro’on boro men kiw tafanamaim inima’ub?
17 Chimodzimodzinso mtengo wabwino umabala chipatso chabwino, koma mtengo woyipa umabala chipatso choyipa.
17 Ai gewasin boro niw gewas, baise ai wanawanan kour nabiw ro’on boro nukunukuwin.
18 Mtengo wabwino sungabale chipatso choyipa, ndi mtengo woyipa sungabale chipatso chabwino.
18 Ai gewasin boro men ro’on nukunukuwin nayai, na’atube ai kakafin boro men ro’on gewasin nayai.
19 Mtengo uliwonse umene subala chipatso chabwino umadulidwa ndi kuponyedwa pa moto.
19 Ai menatan men ebiw gewas boro natar nare nab nan wairaf wan nayara’ah na’arah.
20 Momwemonso, ndi zipatso zawo iwo mudzawazindikira.
20 Imih dinab baifufuwenayah boro hai bowabowamaim kwana’inanih.
21 “Si munthu aliyense amene amanena kwa Ine, ‘Ambuye, Ambuye,’ adzalowe mu ufumu wakumwamba, koma ndi yekhayo amene amachita chifuniro cha Atate anga amene ali kumwamba.
21 “Men sabuw etei ayu wabu hisu’ub teo, ‘Regah, Regah’ boro mar ana aiwobomaim hinarun, baise sabuw iyabowat ayu Tamai ana kok tisisinafuwat boro hinarun.
22 Ambiri adzati kwa Ine pa tsikulo, ‘Ambuye, Ambuye, kodi sitinkanenera mʼdzina lanu ndi mʼdzina lanunso tinkatulutsa ziwanda ndi kuchita zodabwitsa zambiri?’
22 Baibatebat ana veya nanan, sabuw moumurih na’in boro hinao, Regah, Regah, o wabimaim aki tur abai aorereb, o wabimaim aki demon kakafih anunih hibihir, naatu o wabimaim aki ina’inan moumurih na’in asinaf.
23 Pamenepo ndidzawawuza momveka bwino kuti, ‘Sindinakudziweni inu. Chokani kwa Ine, inu ochita zoyipa!’
23 Imaibo ayu boro anauwih anao, Ayu men aso’ob kwa iyab. Biyau’umaim kwatit sa’ab kwan, bowabow kakafih sinafuyah.
24 “Nʼchifukwa chake aliyense amene amva mawu anga ndi kuwachita akufanana ndi munthu wanzeru amene anamanga nyumba yake pa thanthwe.
24 “Isan imih orot yait au tur nowar ebobosiyasiyar, i orot not wairafin ana bar to tafan wowab batabat na’atube.
25 Mvula inagwa, mitsinje inadzaza, ndi mphepo zinawomba pa nyumbayo; koma sinagwe, chifukwa maziko ake anali pa thanthwe.
25 Taun gagamin yar, harew tit, naatu wowog tit bar babin, baise bar men ufar re’emih, anayabin bar ana bubu an i to wanawanan rouw re wowab.
26 Koma aliyense amene amva mawu angawa ndi kusawachita ali ngati munthu wopusa amene anamanga nyumba yake pa mchenga.
26 Baise orot yait au tur nowar naatu men ebobosiyasiyar, i orot aurin not en bar ana bubu dones yan rouw wowowab na’atube.
27 Mvula inagwa, mitsinje inadzaza, ndi mphepo zinawomba pa nyumbayo, ndipo inagwa ndipo kugwa kwake kunali kwakukulu.”
27 Taun yar, harew tit, naatu wowog babin, bar babinakouw, naatu nati bar re’ere i ra’iy tagurugurus sawar.”
28 Yesu atamaliza kunena zonsezi, magulu a anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake,
28 Jesu iti tur eo in sasawar ufunamaim, sabuw rou’ay gagamin na’in Jesu binan hinonowar isan hifofofor men kafaita.
29 chifukwa anaphunzitsa ngati amene anali ndi ulamuliro osati ngati aphunzitsi amalamulo.
29 Anayabin bi’obaiyih ana itinin i roubabaruwen ana fair isan ma’am na’atube, men Ofafar Bai’obaiyenayah na’atube’emih.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Mateus 7, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.