Mateus 6

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Samalani kuti musachite ntchito zanu zolungama pamaso pa anthu kuti akuoneni. Popeza ngati mutero simudzalandira mphotho yochokera kwa Atate anu akumwamba.
1 “Yate nanub, men iti baifa’i isan a bowabow gewasih sabuw nahimaim kwanabowamih, nati na’atube kwanasisinaf na’at, Tamat maramaim boro men a baiyan nitimih.
2 “Pamene mupereka zachifundo, musachite modzionetsera monga amachita achiphamaso mʼmasunagoge ndi pa misewu kuti atamidwe ndi anthu. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti iwowo alandiriratu mphotho yawo yonse.
2 “Imih veya ta akir wairafin sawar inabitin men inakurereb sabuw etei hinanowaramih, men sabuw wanawanah rerekabih Kou’ay Bar wanawanan, naatu ef gagamih yahimaim sabuw itih baifa’ih isan tisisinafube kwanasinafumih, anababatun a tur ao’owen, nati sabuw i boro men hai siwar ta God nitihimih.
3 Koma pamene mupereka zachifundo, dzanja lanu lamanzere lisadziwe chimene dzanja lanu lamanja likuchita,
3 Isan imih akir wairafin inabibais, wa’iwa’iramaim inibais, saise a’of iti sisib ema’am men naso’ob o abisa kusisinaf.
4 kotero kuti kupereka kwanu kukhale mwachinsinsi. Ndipo Atate anu amene amaona zochitika mwachinsinsi, adzakupatsani mphotho.
4 Iti sawar i wa’iwa’iramaim inasinaf, saise Tamat maramaim o abisa wa’iwa’iramaim isisinaf na’iti boro a baiyan nit.
5 “Pamene mupemphera, musakhale ngati achiphamaso, chifukwa iwo amakonda kupemphera choyimirira mʼmasunagoge ndi pa mphambano za mʼmisewu kuti anthu awaone. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti iwo alandiriratu mphotho yawo yonse.
5 “Naatu yoyobanamih men wanawanah rerekabih tisisinafube, kwanasinafumih, anayabin i tekokok Kou’ay Bar wanawanan hinabat hinayoyoban, o ef na’ih awah kaukusebamaim hinabat hinayoyoban, saise sabuw hina’itih, baise anababatun a tur ao’owen, nati sabuw hai baiyan i hibaika.
6 Koma pamene mupemphera, lowani mʼchipinda chanu chamʼkati, ndi kutseka chitseko ndipo mupemphere kwa Atate anu amene saoneka. Ndipo Atate anu, amene amaona zochitika mseri, adzakupatsani mphotho.
6 Baise o yoyobanamih a bar inarun, etawan inahir, Tamat wa’iwa’iramaim ema’am isan inayoyoban, naatu Tamat abisa wa’iwa’iramaim isinaf i’itin boro a baiyan nit.
7 Ndipo pamene mukupemphera, musamabwerezabwereza monga akunja, pakuti iwo amaganiza kuti adzamveka chifukwa chochulutsa mawu.
7 Naatu yoyobanamih men a tur nidun namomonamih, Eteni Sabuw iyab God men hisusu’ub i na’atube tisisinaf. Tenotanot yoyoban manin hinayoyoban God boro hai yoyoban nanowar.
8 Musakhale ngati iwo chifukwa Atate anu amadziwa zimene musowa musanapemphe.
8 Men i hai sinaf kwani’u’ur, anayabin abisa inotanot Tamat i so’obabo o kubifefeyan.
9 “Chifukwa chake pempherani motere:
9 Imih iti na’atube kwanayoyoban,
10 Ufumu wanu ubwere,
10 A aiwob tan,
11 Mutipatse chakudya chathu chalero.
11 Biyai ana fair isan mar etei ai bay initi.
12 Mutikhululukire mangawa athu,
12 Ai kakafih kunotawiyen,
13 Ndipo musatitengere kokatiyesa;
13 Men routobonamaim inanawiyi’imih,
14 Ngati inu mukhululukira anthu pamene akuchimwirani, Atate anu akumwamba adzakukhululukirani.
14 “Taituwa o isa bowabow kakafin hisisinaf inanotawiyen, Tamat maramaim o a kakafih auman boro nanotawiyen.
15 Koma ngati inu simukhululukira anthu zolakwa zawo, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.
15 Baise hai kakafih men inanotanotwiyen na’at, o a kakafin auman Tamat boro men nanotawiyen.
16 “Pamene mukusala kudya, musaonetse nkhope yachisoni monga achita achiphamaso, pakuti iwo amasintha nkhope zawo kuonetsa anthu kuti akusala kudya. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti iwo alandiriratu mphotho yawo yonse.
16 “Kwanayoyohar ana veya men sabuw wanawanah rerekabih kwani’u’urih, anayabin nati na’atube teyoyohar, saise taituwah hina’itih yoharayah hinarouw hinifa’ih isan. Anababatun a tur ao’owen nati sabuw hai baiyan i hibaika.
17 Koma pamene ukusala kudya, samba mʼmaso nudzole mafuta kumutu,
17 Baise kwanayoyohar ana veya yumat kwanasouwen arib raiy kwanay kwanisuwar,
18 kuti usaonekere kwa anthu kuti ukusala kudya koma kwa Atate ako ali mseri; ndipo Atate ako amene amaona za mseri adzakupatsa mphotho.
18 saise sabuw afa boro men hina so’ob kwa i kwayoyohar, baise Tamat wa’iwa’iramaim ema’ama, o abisa akisimo isinaf i’itin boro a baiyan nit.
19 “Musadziwunjikire chuma pa dziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri zimawononga ndi pamene mbala zimathyola ndi kuba.
19 “A sawar gewasih iti tafaramamaim inaya inatototo, ganidor boro na’aan fufur naatu simur boro na’arah, naatu bainowah auman boro a bar hinakwib hinarun a sawar hinabain.
20 Koma mudziwunjikire chuma kumwamba kumene njenjete ndi dzimbiri siziwononga ndipo mbala sizithyola ndi kuba.
20 Imih a sawar etei maramaim inaya inatoto, saise ganidor boro men hina’aan, naatu simur boro men na’arah, naatu bainowah boro men a bar hinakwib hinarun hina bainuwihimih.
21 Pakuti kumene kuli chuma chako, mtima wako udzakhala komweko.
21 A toto abuyoy menamaim kuya’aya, o dogor boro imaim mar etei nama.
22 “Diso ndi nyale ya thupi. Ngati maso ako ali bwino, thupi lako lonse lidzakhala mʼkuwala.
22 “Matat i biyat ana hinow, matat gewasin, biyat etei boro marakawin.
23 Koma ngati maso ako sali bwino, thupi lako lonse lidzakhala mu mdima. Koma ngati kuwala kuli mwa iwe ndi mdima, ndiye kuti mdimawo ndi waukulu bwanji!
23 Baise matat kakafin, biyat tutufin etei boro gugumin kakafin, naatu nati gugumin i wanu’umin kakafin.
24 “Palibe munthu angathe kukhala kapolo wa ambuye awiri. Pakuti pena adzamuda mmodzi ndi kukonda winayo kapena adzagwira ntchito mokhulupirika kwa mmodzi, nadzanyoza winayo. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa chuma pa nthawi imodzi.
24 “Orot ta’imon men karam boro orot gagamih rou’ab isah nabow, ana gewasin orot ta i boro nakwahir, naatu orot ta isan niyabow, orot ta ana tur i boro nanowar naatu orot ta boro nifutuw.
25 “Nʼchifukwa chake ndikuwuzani kuti musadere nkhawa za moyo wanu kuti mudzadya chiyani kapena mudzamwa chiyani; kapenanso za thupi lanu kuti mudzavala chiyani. Kodi moyo suposa chakudya? Kodi thupi siliposa zovala?
25 “Isan imih a tur ao’owen, ayawas isan men kwaniyababan, a tom isan, biya isan, naatu ar faifuw isan. Kwanotanot yawas i sawar gagamin ar faifuw naatu a tom hairi natabirih?
26 Onani mbalame zamlengalenga sizifesa kapena kukolola kapena kusunga mʼnkhokwe komabe Atate anu akumwamba amazidyetsa. Kodi inu simuziposa kwambiri?
26 Kwanuw mamu kwa’itah, men masaw tebob naatu men masaw tefafour, na’atube aurih bay ana korom en baise Tamat maramaim kaifih bay ebitih. Imih kwa i men mamu ekakaifih na’atube ekakaifimih.
27 Kodi ndani wa inu podandaula angathe kuwonjeza ora limodzi pa moyo wake?
27 Imih yababan men karam boro a yawas nakumanin kwanama’amih
28 “Ndipo bwanji inu mudera nkhawa za zovala? Onani makulidwe a maluwa akutchire. Sagwira ntchito kapena kuwomba nsalu.
28 “Naatu aisim ar faifuw isah kwabiyababan? Sigar beran kwanuw kwa’itih, men kafai hibow raro’oh ebababan, o biyah isan ar faifuw tesasakiramih.
29 Ndikukuwuzani kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake sanavale mofanana ndi limodzi la maluwa amenewa.
29 Baise a tur ao’owen, aiwob orot Solomon toto buyoy wairafin, ana faifuw eo’osen i men ta iti beran ana gewasinabe’emih.
30 Ngati umu ndi mmene Mulungu avekera udzu wa kutchire umene ulipo lero ndipo mawa uponyedwa ku moto, kodi sadzakuvekani koposa? Aa! Inu a chikhulupiriro chochepa!
30 God kaiyar fotan ebi’osen wainih kwana’itin, fotan iti boun natasasar, maras boro nakimow nare wairaf wan hinayara’aten hina’arah. Baise kwa i Tamat God uman yanamaim ekakaifi, aisim men kwabitumitum?
31 Chifukwa chake musadere nkhawa ndi kuti, ‘Tidzadya chiyani?’ kapena ‘Tidzamwa chiyani?’ kapena ‘Tidzavala chiyani?’
31 Imih men kwaniyababan kwanao, au ar au faifuw boro menamaim anabow ana’osen, naatu bay boro menamaim anabow ana, harew menamaim anahun anatom?
32 Pakuti anthu akunja amazifuna zinthu zonsezi ndipo Atate anu akumwamba adziwa kuti musowa zimenezi.
32 Eteni Sabuw i sawar iti isah tibiyababan, naatu Tamat maramaim kwa a yababan etei i so’ob.
33 Koma muyambe mwafuna ufumu wake ndi chilungamo chake ndipo zinthu zonsezi zidzapatsidwa kwa inu.
33 Baise wan i mar ana aiwob naatu ma gewasin kwananuwih kwanab, naatu sawar iti etei boro tafan naya’abar nit kwanabow.
34 Chifukwa chake musadere nkhawa ndi za mawa, popeza tsiku lililonse lili ndi zovuta zake zokwanira.
34 Isan imih maras isan men kwaniyababan, anayabin maras ibo akisin ana yababan. Na’atube veya ta’ita’imon hai yababan men inabo’ay inanot a yababan nara’atamih.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Mateus 6, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.