Mateus 25
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 “Nthawi imeneyo ufumu wakumwamba udzafanizidwa ndi anamwali khumi amene anatenga nyale zawo napita kukakumana ndi mkwati.
1 “Nati ana veya’amaim mar ana aiwob itinin i boro baibitar nah ten biyah numin tabin boubun itinamih hai ramef hibow hinan na’atube.
2 Asanu anali opusa ndipo asanu ena anali ochenjera.
2 Baibitar five i not wairafih, naatu baibitar five i men not wairafih.
3 Opusawo anatenga nyale zawo koma sanatenge mafuta;
3 Baibitar men not wairafih hai ramef hibow, baise karisin men ta hirirabar hibaimih.
4 koma ochenjerawo anatenga mafuta awo mʼmabotolo pamodzi ndi nyale zawo.
4 Baibitar five not wairafih hai ramef hibow naatu kibubumaim karisin hirirbaren hibow auman hin.
5 Mkwati anachedwa ndipo onse anayamba kusinza nagona.
5 Tabin boubun ana orot men saise na, baibitar isan hima hikakaif matah fot hi’inurir hi’in.”
6 “Pakati pa usiku kunamveka kufuwula kuti, ‘Onani Mkwati! Tulukani kuti mukakumane naye!’
6 “Fainaiwan sabuw fanah sibisib hinowar, ‘Tabin boubun ana orot enan kwana kwa’itin.’”
7 “Pamenepo anamwali onse anadzuka nayatsa nyale zawo.
7 “Imaibo baibitar ten hi’inu’in himisir, hai ramef matah hibobaituturen naatu hito’aben.
8 Opusawo anati kwa ochenjerawo, ‘Tipatseniko mafuta anu; nyale zathu zikuzima.’
8 Baibitar men not wairafih turahinah not wairafih isah hio, ‘A karisin turin kwaibaisi, aki ai ramef temomorob.’”
9 “Ochenjerawo anayankha, nati, ‘Ayi sangakwanire inu ndi ife. Pitani kwa ogulitsa mafuta ndi kukadzigulira nokha.’
9 “Baise baibitar five not wairafih hiyafutih hio, ‘Men karam boro kwa turin anit naatu aki turin anab. Gewasin boro kwanan sabuw biyahimaim kwabo isa kwanatobon.’”
10 “Koma pamene ankapita kukagula mafutawo, mkwati anafika. Anamwali amene anali okonzeka aja analowa naye pamodzi mʼnyumba ya phwando la ukwati. Ndipo khomo linatsekedwa.
10 “Basit baibitar karisin tobonamih hinan ufut, tabin boubun ana orot natit, baibitar five hibobuna hima’am bairi hin tabin ana yasisir wanawanan hirun etawan hitufabon.”
11 “Pambuyo pake enawo anabwera nati, ‘Ambuye! Ambuye! Titsekulireni!’
11 “Men manin baibitar five hina hitit hi’afririy ‘Regah, Regah, etawan kubotawiy arun!’”
12 “Koma iye anayankha kuti, ‘Zoonadi, ine ndikuwuzani kuti sindikukudziwani.’
12 “Baise orot efatait eo, ‘Anababatun a tur ao’owen, ayu men aso’ob kwa iyab.’”
13 “Choncho khalani odikira, popeza simudziwa tsiku kapena nthawi.”
13 “Isan imih mata to niwa’an kwanama, anayabin veya o sumar men kwa so’ob, mar biy boro iti sawar hinamatar.”
14 “Komanso udzafanizidwa ndi munthu amene ankapita pa ulendo, ndipo anayitana antchito ake nawasiyira chuma chake.
14 “Maramaim mar ana aiwob itinin ta i iti na’atube. Orot ef yok bainanawan isan bobobunabuna ana veya; ana akir wairafih e’afih hina ana sawar kaifen isan faramih.
15 Wina anamupatsa ndalama 5,000, kwa wina 2,000 ndi kwa wina 1,000. Aliyense monga mwa nzeru zake. Pamenepo anapita pa ulendo wake.
15 Hai so’ob ana fofoninamaim orot ta ana kabay 5,000 itin, orot ta 2,000, orot ta 1,000. Imaibo i ana nanawan busuruf in.
16 Munthu amene analandira ndalama 5,000 uja, anapita nthawi yomweyo nachita nazo malonda napindula 5,000 zina.
16 Akir wairafin 5,000 baib in banikamaim yari’iy in bowabow, 5,000 tafan hiya’abar bai.
17 Chimodzimodzinso amene analandira 2,000 uja anapindula 2,000 zina.
17 Akir wairafin bairou’abin i na’atube sinaf. Kabay 2,000 bai in imaim ma bikukumiyaw 2,000 tafan hiya’abar bai.
18 Koma munthu amene analandira 1,000 uja, anapita nakumba dzenje nabisapo ndalama ya mbuye wake.
18 Baise akir wairafin ta ana kabay 1,000 baib i mutufor in hub bai regah ana kabay hub iwan taunafut in.
19 “Patapita nthawi yayitali, mbuye wa antchitowo anabwera nawayitana kuti afotokoze chimene anachita ndi ndalama zija.
19 “Hima manin maiyow, imaibo akir wairafih hai orot ukwarin matabir na tit, naatu hai bowabow nuteteyan itah.
20 Munthu amene analandira ndalama 5,000 uja anabweretsa 5,000 zina nati, ‘Ambuye munandisungitsa 5,000, taonani ndapindula 5,000 zinanso.’
20 Naatu akir wairafin kabay 5,000 baib na run ana regah nanamaim eo, ‘Regah o 5,000 itu, baise ayu abowabow tafanamaim 5,000 abaib i iti kubai.’”
21 “Ambuye ake anayankha nati, ‘Wachita bwino, wantchito wabwino ndi wokhulupirika iwe! Wakhala wokhulupirika pa zinthu zochepa; ndidzakuyika iwe kukhala woyangʼanira zinthu zambiri. Bwera, udzakondwere pamodzi ndi mbuye wako!’
21 “Regah iya’afut eo, ‘A merar ayiy, o i bowayan orot gewas naatu bosunusunubayan, bowabow gidigidih ibosunusunub kukakaifen gewas, imih boro anayara’ahi inayen sawar gagamih inakaifen. Kuna kurun au yasisir turin kubai!’
22 “Munthu amene anali ndi ndalama 2,000 uja anabweranso nati, ‘Ambuye munandisungitsa 2,000, onani, ndapindula 2,000 zinanso.’
22 “Naatu akir wairafin bairou’abin kabay 2,000 baib na run eo, ‘Regah o a kabay 2,000 ibitu i iti, naatu abowabow tafanamaim 2,000 abaib i iti kubai.’
23 “Mbuye wake anayankha nati, ‘Wachita bwino, wantchito wabwino ndi wokhulupirika! Wakhala wokhulupirika pa zinthu zochepa; ndidzakuyika kukhala woyangʼanira zinthu zambiri. Bwera, udzakondwere pamodzi ndi mbuye wako!’
23 “Regah eo, ‘A merar ayiyi, o i bowayan orot gewas naatu bosunusunubayan, sawar matan ta ibosunusunub kukakaifen gewas. Imih boro anayara’ahi inayen sawar moumurihika inakaifen. Kuna kurun au yasisir turin kubai.’
24 “Kenaka munthu amene analandira ndalama 1,000 uja anabwera nati, ‘Ambuye ndinadziwa kuti ndinu munthu wowuma mtima, amene mumakolola pamene simunadzale ndi kututa kumene simunafese.
24 “Imaibo akir wairafin baitonin kabay 1,000 baib na run eo, ‘Regah ayu aso’ob, o i a tur fokarin, turanah hai masaw o aribe kufafaur naatu turanah nowah o kutatanumabe kutaratar.
25 Choncho ndinachita mantha ndipo ndinapita ndi kukabisa ndalama yanuyo pa dzenje. Onani, si iyi ndalama yanu ija.’
25 Imih ayu o isa abir. A kabay abai an hub agais aibun inu’in, iti abai ana abit maiye kwitin.’
26 “Mbuye wake anayankha nati, ‘Iwe wantchito woyipa ndi waulesi! Iwe umadziwa kuti ndimakolola pamene sindinadzale, ndi kututa kumene sindinafese.
26 “Ana Regah iya’afut eo, ‘O i orot kakaf nokonokow anababatun! O iso’ob, ayu i tebob nonowatih afafour naatu tetatanum nonowatih ataratar.
27 Bwanji sunayike ndalama yanga kwa osunga ndalama kuti ine pobwera ndidzalandire ndalama yangayo pamodzi ndi chiwongoladzanja?
27 Gewasin au kabay banikamaim itayi ta’in tabowabow, ayu atanan, saise tafan hitaya’abar auman hitutu atab.’
28 “ ‘Mulandeni ndalamayo, ndipo patsani iye amene ali ndi ndalama 10,000.
28 “Naatu orot ukwarin eo, ‘Kabay iti orot umanamaim kwabosair kwabai kwan akir wairafin kabay 10,000 baib i kwaitin.
29 Pakuti aliyense amene ali nazo adzapatsidwa zambiri, ndipo adzakhala nazo zochuluka. Aliyense amene alibe adzalandidwa ngakhale chimene ali nacho.
29 Anayabin orot yait uman ebi’e’etaw boro sawar tafan hinaya’abar moumurihika nabow isan nakaram. Baise orot yait uman nutanub ema’am biyanamaim sawar etei’imak boro hinabosairen.
30 Ndipo muponyeni wantchito wopanda phinduyu kunja, ku mdima kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.’ ”
30 Imih iti akir wairafin nukunukuwin kwabai kwan kwarauw ufun gugumin wanawanan ere, nati imaim nama narerey wan nayob nitafofofor.’
31 “Pamene Mwana wa Munthu adzabwera mu ulemerero wake, pamodzi ndi angelo ake onse, adzakhala pa mpando waufumu mu ulemerero wakumwamba.
31 “Orot Natun ni’aiwob nanan ana maramaim ana tounamatar kakafiyih boro bairi hinan ana urama’am bonamanamarin tafan namare.
32 Mitundu yonse ya anthu idzasonkhanitsidwa pamaso pake, ndipo adzawalekanitsa iwo wina ndi mnzake monga mʼbusa amalekanitsa nkhosa ndi mbuzi.
32 Naatu tafaram wanawanan sabuw tutufin etei boro hinaru’ay Jesu nanamaim hinabat. Imaibo i boro sabuw nakusib rou’ab hinamatar, nabatanenayan sheep naatu goat bairi ekukusibih na’atube.
33 Adzayika nkhosa ku dzanja lake lamanja ndi mbuzi ku lamanzere.
33 Sheep i boro uman ana asukwafune hinabat naatu goat boro uman ana beyawane hinabat.”
34 “Pamenepo mfumu idzati kwa a ku dzanja lamanja, ‘Bwerani inu odalitsika ndi Atate anga; landirani ufumu umene unakonzedwa chifukwa cha inu kuyambira pachiyambi cha dziko.
34 “Imaibo aiwob orot boro sabuw uman ana asukwafune isah nao, ‘Kwa i Tamai ebigegewasini, kwana mar ana aiwob nowamih kwabai. Anayabin tafaram matara’e ana veya God kwa isa yabuna.
35 Pakuti ndinali ndi njala ndipo munandipatsa chakudya, ndinali ndi ludzu ndipo munandipatsa madzi akumwa, ndinali mlendo ndipo munandilandira,
35 Ayu bayumih amomorob bay kwaitu, sikau mamamah harew kwaitu atom, abinanawan au merar kwayi a baremaim ama ra’at ama.
36 ndinali wausiwa ndipo munandiveka, ndinali wodwala ndipo munandisamalira, ndinali ku ndende ndipo inu munandiyendera.’
36 Segar ama’am faifuw kwaitu aus, asawow ainu’in, kwakaifu naatu dibur bar ama’am kwana kwainanawanu.’”
37 “Ndipo olungamawo adzamuyankha kuti, ‘Ambuye ndi liti tinakuonani muli ndi njala ndipo tinakudyetsani, kapena ludzu ndipo tinakupatsani madzi akumwa?
37 “Sabuw gewasih boro hiniya’afut hinao, ‘Regah mar biyika bayumih imomorob ai’it bay ait, o sika mamamah harew ait itom?
38 Ndi liti tinakuonani muli mlendo ndipo tinakulandirani, kapena wa usiwa ndipo tinakuvekani?
38 Naatu biyika inanawan inan ai’it a merar ayiy abuwi ai sebomaim imara’at? O segar ima’am faifuw ait ius?
39 Ndi liti tinakuonani mutadwala kapena ku ndende ndipo tinakuyenderani?’
39 Naatu mar biyika isawow inu’in akaifi, o dibur bar ima’ama ainanawani?’”
40 “Mfumu idzayankha kuti, ‘Zoonadi, ndikuwuzani kuti chilichonse chimene munachitira mmodzi wa abale anga onyozekawa munandichitira Ine.’
40 “Aiwob orot boro niyafutih nao, ‘Anababatun au’uwi, nati ana veya’amaim ayu taitu gidigidih isah kwasisinaf, i ayu isau kwasinaf.’”
41 “Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake.
41 “Imaibo sabuw ana beyawane hinabatabat isah boro nao, ‘Biyau’umaim kwatit sa’ab kwan. Kwa i orarafen wanawanan kwarun, Demon Mowan ana tounamatar bairi isah wairaf wanatowan hibobogaigiwas kwan imaim kwarun bairi e’arahi.
42 Pakuti ndinali ndi njala ndipo simunandipatse chakudya, ndinali ndi ludzu ndipo simunandipatse madzi akumwa,
42 Ayu aa amomorob, men abisa ta kwaitu aan, sikau mamamah harew men kwaitu atom.
43 ndinali mlendo koma inu simunandilandire, ndinali wa usiwa koma simunandiveke, ndinali wodwala komanso ku ndende simunandisamalire.’
43 Ai nanawan anan men au merar kwayi a sebomaim amara’at. Segar ama’am faifuw men kwaitu ausimih, a sawow ainu’in, o dibur baremaim ama’am men kwana kwainanawanu.’”
44 “Iwo adzayankha kuti, ‘Ambuye ndi liti tinakuonani muli ndi njala kapena ludzu kapena mlendo kapena wausiwa kapena wodwala kapena mʼndende, ndipo kuti sitinakuthandizeni?’
44 “Naatu i boro hiniya’afut hinao, ‘Regah, mar biyika o aa imomorob, o harewamih sika mamamah, o ibinanawan, o segar ima’am, o isawow inu’in, o dibur bar ima’am men aibaisimih?’”
45 “Iye adzayankha kuti, ‘Zoonadi, ndikuwuzani kuti chilichonse chimene simunachitire mmodzi wa abale anga onyozekawa simunandichitire Ine.’
45 “Imaibo i boro niyafutih nao, ‘Anababatun a tur ao’owen, ayu taitu gidigidih men kwabibaisih, nati i men kwakok ayu kwatibaisu.’”
46 “Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.”
46 “Naatu nati sabuw i boro hinan ma’ama wanatowan ana baimakiy hinab. Baise sabuw gewasih boro hinan yawas ma’ama wanatowan hinab hinama hiniyasisir.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Mateus 25, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.