Mateus 24
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Yesu anatuluka mʼNyumba ya Mulungu ndipo akuchoka ophunzira ake anadza kwa Iye ndi kumuonetsa mamangidwe a Nyumbayo.
1 Jesu Tafaror Bar gagamin ihamiy tit inan auman, ana bai’ufununayah hina hiu, “Tafaror bar kwi’itin gewasin maiyow.”
2 Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukuona zinthu zonsezi? Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti palibe mwala pano umene udzasiyidwe pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.”
2 Jesu iyafutih eo, “Sawar iti kwa’i’itan, a tur ao’owen, kabay etei boro natafofor nare naatu kabay ta boro men ana efanamaim na’inu’in kwana’itinimih.”
3 Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?”
3 Jesu yen Olive Oyaw tafan mare, ana bai’ufununayah wa’iwa’iramaim hina biyan hitit hibatiy hio, “Kuo anowar mar i boro biy iti sawar hinamatar? Naatu o inanan ina’inanen boro abisa ana’itin anaso’ob. Naatu mar yomanin nakakabon boro mi’itube ana so’ob?”
4 Yesu anayankha kuti, “Onetsetsani kuti wina asakunyengeni.
4 Jesu iyafutih eo, “Matato niwa’an, men sabuw hinan hinifufuwimih.
5 Pakuti ambiri adzabwera mʼdzina langa nadzati, ‘Ndine Khristu,’ ndipo adzanyenga ambiri.
5 Sabuw moumurih na’in boro ayu wabu’umaim hinan hinao, ‘Ayu i Keriso’ naatu sabuw moumurih na’in boro hinifufuwih.
6 Mudzamva za nkhondo ndi mbiri za nkhondo, koma onetsetsani kuti musadzidzimuke nazo. Zotere ziyenera kuchitika, koma chimaliziro sichinafike.
6 Baiyow ana tur boro kwananowar, naatu baiyow isan ana tur boro kwananowar, baise men kwanabir. Sawar yumatah ta ta boro hinamatar, baise nati i men mar yomanin.
7 Mtundu ndi mtundu udzawukirana, ndipo ufumu ndi ufumu udzawukirana. Kudzakhala njala ndi zivomerezi mʼmalo osiyanasiyana.
7 Tafaram ta boro tafaram ta hairi hiniyow, na’atube bar merar ta boro bar merar ta ana aiwob hairi hiniyow. Baimar kakafin, iriyoy boro tafaram awan nakaratan.
8 Zonsezi ndi chiyambi chabe cha zowawa.
8 Sawar iti etei hinamatar i kek tufuwamih ebobotukwar na’atube.
9 “Pamenepo adzakuperekani kuti mukazunzidwe ndi kuphedwa, ndipo mitundu yonse idzakudani chifukwa cha Ine.
9 “Sabuw boro hinafatumi hinabuw kwanan hini’a’akir, hina’asbuni kwanamorob, ayu wabu’umaim kwabowabow isan.
10 Pa nthawi imeneyo ambiri adzasiya chikhulupiriro ndipo adzadana ndi kuperekana wina ndi mnzake,
10 Nati ana veya’amaim baitumatumayah boro hai baitumatum hinihamiy, naatu turahinah babah hinao, taiyuwih turahinah hinifa’ifa’ih,
11 ndipo aneneri onama ambiri adzaoneka ndi kunyenga anthu ambiri.
11 dinab baifufuwenayah moumurih na’in boro hinatit sabuw moumurih na’in hinifufuwih.
12 Chifukwa cha kuchuluka kwa zoyipa, chikondi cha ambiri chidzazirala,
12 Tafa’asar boro nara’at natasasar sabuw momurih na’in hai yabow boro wan natutum.
13 koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka.
13 Baise yait nabukikin nan yomanin natitit i boro yawas nab.
14 Ndipo uthenga wa ufumu udzalalikidwa ku dziko lonse lapansi ngati umboni kwa mitundu yonse, ndipo pomwepo chimaliziro chidzafika.”
14 Tur Gewasin, mar ana aiwob isan, i boro tafaram wanawanan etei hinabinan sabuw etei hinanowar, imaibo mar yomanin boro nan natit.
15 “Tsono mukadzaona chinthu chonyansa chosakaza chitayima pamalo oyera chimene anayankhula mneneri Danieli, owerengayo azindikire.
15 “Biya’ohow Ana Sawar Kakafin boro efan kakafiyinamaim nabatabat kwana’itin, dinab orot Daniel eo na’atube. Baiyabayan orot iti tur nabiyab naniyan nab gewas.
16 Pamenepo amene ali ku Yudeya athawire ku mapiri.
16 Sabuw iyab Judea wanawananamaim tema’ama boro hinabihir hinan oyaw wan hinayen.
17 Yemwe ali pa denga la nyumba yake asatsike kukatulutsa chinthu chilichonse mʼnyumba.
17 Orot yait ana bar faifiy wan ema’am boro men nare ana sawar bar wanawanan nabowamih, veya en.
18 Yemwe ali ku munda asapite kukatenga mkanjo wake.
18 Orot yait masaw ebowabow boro men namatabir ana biya baibiyon bar nabaimih.
19 Kudzakhala koopsa kwambiri masiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi kwa oyamwitsa!
19 Nati ana veya’amaim baibin iyab siasiar tema’ama naatu baibin iyab kek tibitotoman boro hini’akir yababan hinab.
20 Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzachitike nthawi yozizira kapena pa Sabata.
20 God isan kwanayoyoban, saise men rarab kokou ana veya’amaim o Sabbath ana veya’amaim namataramih.
21 Popeza kudzakhala masautso aakulu, omwe safanana ndi ena ali onse chiyambireni cha dziko lapansi mpaka lero lino ndipo sadzafanananso ndi ena.
21 Nati ana veya’amaim boro yababan kakafin men marasika anamaim o boro namamatar na’atube namataramih.
22 Ngati masiku amenewo sakanafupikitsidwa, palibe mmodzi akanapulumuka, koma chifukwa cha osankhidwawo masiku amenewo adzafupikitsidwa.
22 God nati veya narurukabum na’at sabuw boro yawas men hinab. Baise ana sabuw rurubiniyih isah enotanot, imih veya boro narukabum.
23 Pa nthawi imeneyo ngati wina adzati kwa inu, ‘Onani, Khristu ali pano!’ Kapena, ‘Uyo ali ukoyo!’ Musakhulupirire.
23 “Nati ana veya sabuw afa hinan hina’uwi, ‘Keriso’oban iti!’ o ‘Iban ni’i!’ men kwanitumatum.
24 Chifukwa akhristu onama ndi aneneri onama adzaoneka ndipo adzachita zizindikiro zazikulu ndi zodabwitsa kuti akanyenge ngakhale osankhidwawo ngati kukanakhala kotheka kutero.
24 Anayabin Keriso na’atube naatu dinab baifufuwenayah boro hinan ina’inan fokarih hinasinaf God ana rourubinen sabuw moumurih na’in boro hinabow.
25 Onani, ndakuwuzani izi nthawi isanafike.
25 Imih abimatuwibo sawar hinamatar.
26 “Ndiye ngati wina akuwuzani inu kuti, ‘Uyo ali ku chipululu,’ inu musapiteko; kapena akati, ‘Uyu ali kuno mʼchipinda chamʼkati,’ musakhulupirire.
26 “Sabuw a tur hinaowen hinao, ‘Iban nati arar yan ema’am,’ men imaim kwanan kwananuwih. O hinao, ‘Nati nanawan bar wanawanan wa’ir ema’am,’ men kwanitumatum.
27 Monga momwe mphenzi ingʼanima kuchokera kummawa kupita kumadzulo, momwemonso kudzakhala kubwera kwa Mwana wa Munthu.
27 Veya yeninane namanamar ebowabow veya ra’iyinane uman emamarakaw, Orot Natun nanan ana marakaw boro nati na’atube.
28 Kulikonse kuli chinthu cha kufa, makwangwala adzasonkhanako.
28 Menamaim orot babin biyan murubin inu’in mamu ikou boro etei imaim hinaru’ay.
29 “Akadzangotha mavuto a masiku amenewo,
29 “Yababan iti hinamamatar ufunamaim
30 “Pa nthawi imeneyo chizindikiro cha Mwana wa Munthu chidzaoneka mlengalenga, ndipo mitundu yonse ya pa dziko lapansi idzalira. Idzaona Mwana wa Munthu akubwera ndi mitambo, mphamvu ndi ulemerero waukulu.
30 “Imaibo Orot Natun maramaim boro natit, tafaram wanawanan sabuw etei orot Natun ana fair ana marakaw bonamanamarin auman natit sakuk wanawanan nanan hina’itin hinama hinarerey.
31 Ndipo adzatuma angelo ake, ndi kulira kwa lipenga kwakukulu, nadzasonkhanitsa osankhidwa ake kuchokera ku mphepo zinayi, ndi kuchokera kumathero a thambo kufika mbali ina.
31 Ana tounamatar boro taur douduf auman hinatit tafaram tutufin wanawanan umasusun kwafe’en etei God ana sabuw rurubinih hinabow hinita’ay.
32 “Tsopano kuchokera ku mtengo wamkuyu phunzirani ichi: Pamene uyamba kuphukira, masamba ake akatuluka, mumadziwa kuti dzinja layandikira.
32 “Ai fofou raurihimaim ebi’obaiyih kwanaso’ob, ai raurih boubuh tititit kwa kwaso’ob, ai hai buwayan ana veya i natit.
33 Momwemonso, pamene mudzaona zinthu zonsezi mudzadziwe kuti ali pafupi pa khomo penipeni.
33 Bai’obaiyen i ta’imon, sawar iti na’atube hinamamatar kwa boro kwanaso’ob, veya i nakabom etawan awanamaim ebatabat.
34 Zoonadi, ndikuwuzani kuti mʼbado uwu sudzatha mpaka zinthu zonse zitachitika.
34 Anababatun a tur ao’owen, sabuw iti boun yawas kwama’am boro iti sawar namatar kwana’itinibo kwanamorob.
35 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
35 Mar tafaram i boro nasawar, baise ayu au tur boro men nasawar.
36 “Palibe amene adziwa za tsikulo kapena nthawi, angakhale angelo akumwamba, angakhale Mwana, koma Atate okha.
36 “Orot men yait ta Jesu ana na isan veya o sumar so’obamih. tounamatar maramaim men hiso’ob na’atube i Natun auman men so’ob, baise Tamah akisinamo so’ob.
37 Monga momwe zinalili nthawi ya Nowa, momwemonso zidzatero pobwera kwa Mwana wa Munthu.
37 Noah ana veya’amaim abisa mamatar na’atube Orot Natun nanan boro na’atube namatar.
38 Pakuti masiku amenewo chisanafike chigumula, anthu amadya ndi kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa, mpaka tsiku limene Nowa analowa mʼchombo;
38 Nati ana veya tuw yena’e ana veya orot babin hiyuw hibow, hiaa hitom, hitabin hibiyasisir ufut Noah ark wanawanan run;
39 ndipo sanadziwe za chimene chikanachitika mpaka pamene chigumula chinafika ndi kuwamiza onse. Umu ndi mmene zidzakhalira pobwera kwa Mwana wa Munthu.
39 naatu so’oba’e hima’am kwanekwan tuw yen etei e’aruwih hin himorob. Imih orot Natun nanan ana itinin i boro nati na’atube.
40 Amuna awiri adzakhala mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
40 Orot rou’ab boro hai masaw hinama hinabob, Orot ta boro tounamatar hinabora’ah ta boro hinihamiy nama.
41 Amayi awiri adzakhala akusinja pa mtondo; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
41 Baibin rou’ab boro hinama maiwok hinakakair, babin ta boro hinabora’ah, babin ta boro hinihamiy nama.
42 “Chifukwa chake yangʼanirani, popeza simudziwa tsiku lanji limene Ambuye anu adzabwera.
42 “Isan imih mata to niwa’an, anayabin men kwaso’ob mar biy boro a Regah nan.
43 Koma zindikirani ichi: Ngati mwini nyumba akanadziwa nthawi yanji ya usiku imene mbala imabwera, sakanagona ndipo sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
43 Baise tur iti ao i naniyan kwanab. Orot bar matuwan bainowan hai veya nasoso’ob, boro matan nanuw nama’am nanunih hinabihir, ana bar boro men hinakwib hinabainuwimih.
44 Inunso tsono muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa nthawi imene inu simukumuyembekezera.
44 Imih mar etei mata to niwa’an kwanabobuna kwanama, anayabin Orot Natun boro men o veya kunotanotamaim natitamih.
45 “Kodi wantchito wokhulupirika ndi wanzeru amene ambuye ake anamuyika kukhala woyangʼanira antchito a mʼnyumba kuti awapatse chakudya chawo pa nthawi yake ndani?
45 “Akir wairafin bosunusunubayan naatu not wairafin ana orot ukwarin boro nayara’ah akir wairafih afa nakaifih hai bay ana veya’amaim nitih.
46 Chidzakhala chabwino kwa wantchitoyo ngati mbuye wake pofika adzamupeza akuchita zimenezi.
46 Naatu ana orot ukwarin namatabir nanan bowabow gewasin nabowabow na’itin boro niyasisir.
47 Zoonadi, ndikuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
47 A tur ao’owen nati akir wairafin boro nayara’ah sawar etei nakaifen.
48 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo ndi woyipa, nati kwa iye yekha, ‘Mbuye wanga akuchedwa kubwera,’
48 Baise akir wairafin nitafasar nao, ‘Au orot ukwarin men saise matabir enanamih.’
49 nayamba kumenya antchito anzake, nadya ndi kumwa ndi zidakwa.
49 Naatu natatabir akir wairafih afa narauw ni’a’afiyih bay naa, harew tomayah bairi hinaa hinatom hinabikoko’aw wanawanan
50 Mbuye wa wantchitoyo adzabwera pa tsiku limene iye samamuyembekezera ndi pa nthawi imene iye sakuyidziwa.
50 veya naatu sumar so’oba’e nama’am kwanekwan ana orot ukwarin namatabir nan natit.
51 Adzamulanga koopsa ndipo adzamuyika kokhala anthu achiphamaso, kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.”
51 Naatu orot ukwarin nati ana akir wairafin boro nab narab ufun narauwatait, sabuw afa wanawanah rerekabih bairi baimakiy kakafin hinab hinama hinarerey wah takitak niwa’an.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Mateus 24, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.