Marcos 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ndipo anawoloka nyanja napita ku dera la Gerasa.
1 Jesu ana bai’ufununayah bairi harew Galilee hirabon hina tafaram Gerasa imaim hitit.
2 Yesu atatuluka mʼbwato, munthu amene anali ndi mzimu woyipa anachoka ku manda ndi kukumana naye.
2 Jesu wa wanawanan tit bisure auman, mar ta’imonamo orot ta afiy kakafih hitounbubur ma’am rahane tit na biyan tit.
3 Munthuyu amakhala ku manda, ndipo panalibe amene akanatha kumumanganso ngakhale ndi unyolo.
3 Iti orot i rahamaim in ma reremor, naatu sabuw murab fokarih anababatun hifafatum men karam.
4 Pakuti nthawi zambiri akamumanga manja ndi miyendo amadula maunyolo ndi kudula zitsulo zimene zinali mʼmapazi ake. Panalibe amene anali ndi mphamvu yoti ndi kumugonjetsa.
4 Anayabin mar etei an uman murab fokarihimaim tefafatumen, baise eyi erab an uman murab tetoro’oro’omen naatu aur tetatafofor, fair kwanekwan men karam boro hitarouh.
5 Usana ndi usiku ankakhala ku manda ndi kumapiri, akulira ndi kudzicheka ndi miyala.
5 Fai mar rahamaim naatu oyawemaim in ma itar koukuw taiyuwin biyan agimamaim bobeyabeyaten reremor.
6 Ataona Yesu ali patali, anathamanga nagwa pa mawondo ake pamaso pake.
6 Jesu no ef yokaika nan itin, nunuw in nanamaim ra’iy sun yowen. Demon mowan Jesu nanamaim sun eyoyowen|alt="demoniac kneel b4 Jesus" src="CN01710B.TIF" size="col" loc="Mrk 5.6" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="5.6"
7 Iye anafuwula kwambiri nati, “Mukufuna muchite nane chiyani, Yesu Mwana wa Mulungu Wammwambamwamba? Lumbirani kwa Mulungu kuti simundizunza!”
7 Naatu fanan aumetawat na’in iwow eo, “O ayu biyau’umaim abisa kukokok, Jesu God auyom ma’ama’anin Natun? God wabinamaim abifefeyan men biyababan initu’umih!”
8 Pakuti Yesu anati kwa iye, “Tuluka mwa munthuyu, iwe mzimu woyipa!”
8 Anayabin Jesu iu, “O afiy kakafin orot biyanane kutit!”
9 Ndipo Yesu anamufunsa iye, “Dzina lako ndani?”
9 Naatu Jesu ibatiy, “O
10 Ndipo anamupempha Yesu mobwerezabwereza kuti asazitulutse mʼderalo.
10 Naatu Jesu fefeyan kikin men hikok boro tiyafarih hitatit tafaram nati hitihamiy.
11 Gulu lalikulu la nkhumba limadya mʼmbali mwa phiri limene linali pafupi.
11 For burut kakafin nati yubin heher ta sisibinamaim hima hi’u’ufar.
12 Ziwandazo zinapempha Yesu kuti, “Titumizeni pakati pa nkhumbazo; ndipo mutilole tilowe mwa izo.”
12 Afiy kakafih Jesu hifefeyan hio, “Karam boro iti yafari atan for wanawanah atarun?”
13 Iye anazipatsa chilolezo, ndipo mizimu yoyipayo inatuluka ndi kukalowa mu nkhumbazo. Gulu la nkhumba, zokwana pafupifupi 2,000 zinathamanga kutsetserekera ku nyanja ndipo zinamira.
13 Jesu afiy kakafih baibasit itih, orot biyanane hitit hin for wanawanah hirun, for 2,000 na’atube heher sisibin hinunuw hira’iy harew yan hire hi’ar tomatom himorob.
14 Omwe amaweta nkhumbazo anathawa ndi kukawuza anthu za izi mu mzinda ndi ku madera a ku midzi, ndipo anthu anapita kukaona zomwe zinachitika.
14 Orot iyab hima for hibituw hinunuw hin bar merar gagamin naatu bar merar afa hai tur hi’owen. Naatu sabuw abisa mamatar itininamih hitit hina.
15 Atafika kwa Yesu, anaona munthu amene anagwidwa ndi ziwanda zambiri uja atakhala pansi pomwepo, atavala, ndipo ali bwinobwino. Iwo anachita mantha.
15 Hina Jesu biyan hitit hinuwanuw orot afiy kakafih hitounbububur ma’am, i boun ana not rumutufur faifuw gewasin iyoun mare ma’am hi’i’itin ana maramaim hibir.
16 Amene anaona zimenezi anawuza anthu zomwe zinachitika kwa munthu wogwidwa ndi ziwandayo ndipo anawawuzanso za nkhumbazo.
16 Sabuw iyab matah yan orot afiy hitounbububur ma’am isan mi’itube mamatar, naatu for isah abisa mamatar hi’i’itan sabuw hai tur hi’owen.
17 Ndipo anthu anayamba kumupempha Yesu kuti achoke mʼdera lawo.
17 Naatu sabuw Jesu hifefeyan hai tafaram baihamiyinamih hiu.
18 Yesu akulowa mʼbwato, munthu amene anagwidwa ndi ziwanda uja anamupempha kuti apite nawo.
18 Jesu wa afe’en yenamih orot afiy hitounbububur ma’am na Jesu ifefeyan hairi namih.
19 Yesu sanamulole, koma anati, “Pita kwanu ku banja lako ndipo ukawawuze zimene Ambuye wakuchitira, ndi chifundo chimene wakuchitira.”
19 Baise Jesu men ibasit, naatu orot iu, “O kwen a bar hinat tamat naatu taituwa, Regah ana gewasin o isa sisinaf naatu ana kabeber bit i hai tur ku’owen.”
20 Pomwepo munthuyo anapita nayamba kuwuza anthu a ku Dekapoli zinthu zimene Yesu anamuchitira. Ndipo anthu onse anadabwa.
20 Basit orot nati’imaim ihamiyih Bar Merar Etei Umat Roron imaim remor Jesu mi’itube biyawas sabuw hai tur eowen, naatu sabuw hinonowar i hifofofor men kafaita.
21 Yesu atawolokeranso pa bwato kupita mbali ina ya nyanja, gulu lalikulu la anthu linasonkhana momuzungulira. Ali mʼmbali mwa nyanja,
21 Jesu ibanak maiye wa isra’at rabon harew rounane hitit, naatu re riy sisibin bat, imaibo sabuw moumurih na’in hina hi’arbebera’uh.
22 mmodzi wa akulu a mʼsunagoge, dzina lake Yairo anafika pamenepo. Ataona Yesu, anagwa pa mapazi ake,
22 Naatu Kou’ay bar ana ukwarin orot wabin Jairus na tit, nuw Jesu i’itin ana maramaim na anamaim ra’iy.
23 ndi kumudandaulira kwambiri nati, “Mwana wanga wamkazi wamngʼono ali pafupi kufa. Chonde tiyeni kuti mukamusanjike manja kuti akachiritsidwe nakhala ndi moyo.”
23 Naatu fefeyan kikin eo, “Ayu natu babitai i emomorob, akokok inan umamaim au kek biyan inabutun saise nayawas!”
24 Ndipo Yesu anapita naye.
24 Naatu Jesu orot Jairus hairi hin, sabuw himour kwanekwan hibi’ufunun naatu yaten hiyey.
25 Pomwepo panali mayi amene amadwala nthenda yotaya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri.
25 Wanawanahimaim i babin ta, baibin hai sawow bai ma kwamur etei 12 sawar.
26 Iye anavutika kwambiri pamene asingʼanga ambiri ankamusamalira ndipo anagwiritsa ntchito zonse anali nazo, koma mʼmalo mochira, nthenda yake inkakulakulabe.
26 I’akir manin na’in, adanafur bowayah ta ta isah run tit kabay gagamin na’in ibaiyanih, baise men yawas ta tita’ur ana sawowone i rara’at sasa.
27 Atamva za Yesu, anabwera kumbuyo kwake mʼgulu la anthu ndipo anakhudza mkanjo wake,
27 Jesu ana tur nowar, naatu sabuw wanawanahimaim inan babin Jesu ufunane tit ana faifuw butubun.
28 chifukwa anaganiza kuti, “Ngati nditangokhudza mkanjo wake, ndidzachiritsidwa.”
28 Anayabin i na’at not, “Ayu ana faifuw ana butubun boro ana yawas.”
29 Nthawi yomweyo magazi ake analeka kutuluka ndipo anamva mʼthupi mwake kuti wamasulidwa ku vuto lake.
29 Naatu bubutubun mar ta’imonamo rara nununuw nutanub naatu biyan wanawanan naniyan tatatam nati bai’akirane yawas.
30 Pomwepo Yesu anazindikira kuti mphamvu inachoka mʼthupi mwake. Anatembenuka mʼgulu la anthu ndipo anafunsa kuti, “Ndani wakhudza zovala zanga?”
30 Jesu fair biyanane titit i naniyan tatam, sabuw wanawanahimaim tatabir ibatiyih, “Yait ayu au faifuw butubun?”
31 Ophunzira ake anayankha kuti, “Mukuona kuti anthu akukupanikizani, ndipo Inu mukufunsa kuti, ‘Ndani wandikhudza?’ ”
31 Ana bai’ufununayah hiu, “O sabuw moumurih na’in yate teyey, naatu baise o kubibat, yait ayu butubuni?”
32 Koma Yesu anapitirizabe kuyangʼana kuti aone amene anachita zimenezi.
32 Baise Jesu bat inuwanuw menatan sisinaf itininamih.
33 Kenaka mayi uja pozindikira chimene chinamuchitikira, anabwera ndi kugwa pa mapazi ake, ndipo akunjenjemera ndi mantha, anamuwuza zoona zokhazokha.
33 Naatu babin biyanamaim abisa mamatar i so’ob, imih tit Jesu nanamaim ra’iy an uman hi’oror mi’itube isan mamatar etei eorerereb.
34 Anati kwa iye, “Mwana wamkazi, chikhulupiriro chako chakuchiritsa. Pita mu mtendere ndipo khala womasulidwa ku mavuto ako.”
34 Naatu babin iu, “Natu, o abaitumatumamaim iyawasi, tufuwamaim kwen, a bai’akirane o arufami kutitit.”
35 Pamene Yesu ankayankhulabe, amuna ena anafika kuchokera ku nyumba ya Yairo, mkulu wa sunagoge. Iwo anati, “Mwana wanu wamkazi wamwalira, muvutitsiranjinso aphunzitsiwa?”
35 Jesu bat eo’o auman, sabuw afa Kou’ay Bar orot ukwarin ana barene hina Jairus hiu, “O natu babitai i morob, Bai’obaiyenayan men inarowenbibibir.”
36 Posasamala zomwe ananena, Yesu anamuwuza mkulu wa sunagoge uja kuti, “Usachite mantha; ingokhulupirira.”
36 Abisa hio Jesu nowar, natu Jairus iu “Men inabir o initumatum.”
37 Iye sanalole munthu wina aliyense kuti amutsatire koma Petro, Yakobo ndi Yohane mʼbale wa Yakobo.
37 Sabuw etei eotanih hima, i Peter, James naatu John akisihimo iuwih bairi hin.
38 Atafika ku nyumba ya mkulu wa sunagoge, Yesu anaona chipiringu cha anthu akulira ndi kufuwula kwambiri.
38 Hina Jairus ana bar hititit ana veya sabuw yababan gagamin na’in buwih fanah aumetawat na’in hima hirererey Jesu nowar.
39 Analowa nati kwa iwo, “Mukuchita phokoso ndi kulira chifukwa chiyani? Mwanayu sanamwalire koma ali mtulo.”
39 Naatu bar wanawanan run sabuw iuwih, “Kwa aisim kwarererey? Iti kek i men morobomih, i matan fot inu’in.”
40 Koma anamuseka Iye.
40 Baise sabuw Jesu eo isan himarib. Naatu Jesu sabuw iuwih ufun hitit, kek hinah tamah naatu ana bai’ufununayah akisihimo hirun hin kek inu’inumaim hitit.
41 Anagwira dzanja lake nanena kwa iye, “Talita Kumi!” (Kutanthauza kuti, “Mtsikana, ndikunena ndi iwe, imirira!”)
41 Kek babitai umanamaim bai naatu iu, “Talitha koum!” Nati anayabin i iti na’atube, “Babitai kafai o au’uwi kumisir!”
42 Nthawi yomweyo anayimirira nayenda mozungulira (anali wa zaka khumi ndi ziwiri). Pa ichi onse anadabwa kwambiri.
42 Mar ta’imonamo babitai misir an yan bat remor, babitai ana kwamur 12 iti mamatar i hi’oror sa’ir hai kasiy ra’at hifofofor men kafaita.
43 Anawalamulira kwambiri kuti asawuze wina aliyense za ichi, ndipo anawawuza kuti amupatse kanthu koti adye.
43 Jesu ofafarih uwih eo, “Men sabuw hai tur kwana’owenamih, bay kwabai babitai kwaitin eaan.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Marcos 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.