Marcos 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Nthawi inanso Yesu atakhala mʼmbali mwa nyanja, anayamba kuphunzitsa. Gulu lalikulu la anthu linasonkhana momuzungulira kotero kuti Iye analowa mʼbwato lomwe linali pa nyanja nakhalamo, anthu onse ali pa mtunda mʼmbali mwa madzi.
1 Iban maiye Jesu harew Galilee sisibinamaim ana bai’ubaiyen bai tit. Sabuw i himour kwanekwan imih i wa afe’en yen mare naatu sabuw harew sisibin dones yan himarir
2 Anawaphunzitsa zinthu zambiri mʼmafanizo, ndipo mʼchiphunzitso chake anati:
2 naatu i oroubonamaim sawar moumurih na’in i’obaiyih eo.
3 “Tamverani! Mlimi anapita kukafesa mbewu zake.
3 “Kwananowar! Masaw bowayan ana masawamaim ub tanumamih in.
4 Akufesa, mbewu zina zinagwera mʼmbali mwa njira, ndipo mbalame zinabwera ndi kuzidya.
4 Naatu ana ub tata’asi’asiy ana maramaim ub afa i ef yan hira’iy, naatu mamu hina hibow hi’aa.
5 Zina zinagwa pa malo a miyala pamene panalibe dothi lambiri. Zinamera mofulumira chifukwa panalibe dothi lambiri.
5 Ub afa i karakarar yan kamar men gagamin yanamaim hira’iy, naatu saisewat hikuboubunih hiyen, anayabin me kikimin baban inu’in.
6 Koma dzuwa litakwera, mbewuzo zinapserera, ndipo zinawuma chifukwa zinalibe mizu.
6 Imih veya yen rararan ana mar ana fora’abinamaim, nati ub hikukubounih i hi’arat himorob, anayabin ah wairoron i men ra’iy me babanika.
7 Mbewu zina zinagwa pa minga, ndipo mingayo inayanga ndi kuzirepheretsa kukula.
7 Ub afa i fotan kokor wanawanan hira’iy, naatu ro’oh men matar, anayabin fotan yen fafa rab isuk.
8 Mbewu zinanso zinagwa pa nthaka yabwino ndipo zinamera, zinakula ndi kubereka zipatso, zina zochuluka makumi atatu, zina makumi asanu ndi limodzi ndi zina 100.”
8 Baise ub afa i me gewasin yan hira’iy, naatu hikubounih hiyen hibiw, afa i magamagar 30 na’atube, afa i rubirubih 60 na’atube, naatu afa i hiwai re 100 na’atube.”
9 Pamenepo Yesu anati, “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”
9 Naatu Jesu iuwih eo, “O yait tain nama’am na’at iti tur nanowar ininotanot.”
10 Ali yekha, ophunzira ndi ena omuzungulira, anamufunsa za mafanizo.
10 Jesu akisin ma’am ana maramaim ana bai’ufununayah nah 12 naatu sabuw afa iyab tur hinonowar hina hibatiy oroubon anayabin so’ob isan.
11 Iye anawawuza kuti, “Chinsinsi cha ufumu wa Mulungu chapatsidwa kwa inu. Koma kwa amene ali kunja zinthu zonse zinenedwa mʼmafanizo:
11 Naatu iuwih, “God ana aiwob ana buriburin i hibai kwa hit. Baise iyab no ufunamaim tema’am sawar etei i boro oroubonamaim hina’uwih.
12 kotero kuti,
12 Saise,
13 Pamenepo Yesu anawawuza kuti, “Kodi simukulimvetsa fanizoli? Kodi nanga mudzazindikira bwanji fanizo lina lililonse?
13 Naatu Jesu i’uwih, “Kwa iti oroubon naniyan men kwanabaib na’at oroubon afa auman naniyah boro mi’itube kwanaso’ob?
14 Wofesa amafesa mawu.
14 Masaw bowayan i God ana tur ub na’atube ta’asiy re.
15 Anthu ena ali ngati mbewu za mʼmbali mwa njira, mʼmene mawu amafesedwamo. Akangowamva, Satana amabwera ndi kuchotsa mawu amene anafesedwa mwa iwo.
15 Sabuw afa i ub ef yan ta’asi’asiyen hire’erebe, God ana tur tenonowar ufunamaim, Satan boro nan abisa re hai yawasamaim tatanum boro nabosair.
16 Ena, monga mbewu zofesedwa pa miyala, amamva mawu ndipo nthawi yomweyo amawalandira ndi chimwemwe.
16 Afa i ub karakarar yanamaim hire’erebe, tur gewasin tenonowar ana veya i boro matah nakabiy ereyasisir auman hinab.
17 Koma popeza alibe mizu, amakhala kwa kanthawi kochepa. Mavuto kapena masautso akafika chifukwa cha mawu, amagwa mofulumira.
17 Baise i an wairoroh en, imih boro men maninaka nawainabih, anayabin tur gewasin hibaib isan ahay waf naatu bai’akir kakafin wanawanan hinarur ana maramaim i boro saisewat hinare.
18 Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;
18 Naatu baise ub afa i fotan kokor wanawanan hire’erebe, i tur gewasin tenonowar,
19 koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso.
19 baise i hai yababan biyah ana yasisir isan, totobuyoy ana baitenbibiren, naatu hai kok sawar ta ta men gewasih erun, tur gewasin hai yawasamaim erabirab, imih men ebiwamih.
20 Ena, ngati mbewu zofesedwa pa nthaka yabwino, amamva mawu, nawalandira, ndi kubereka zipatso zokwanira makumi atatu, makumi asanu ndi limodzi, kapena ngakhale 100 kuwonjezera pa zomwe zinafesedwa.”
20 Naatu sabuw afa i ub me gewasin yanamaim hire’ere’ebe, tur hinowar hibasit hibai naatu hai yawasamaim ro’on matar, afa i 30, afa 60, naatu afa i 100.”
21 Iye anawawuza kuti, “Kodi umatenga nyale ndi kuyiika pansi pa mbiya kapena pansi pa bedi? Mʼmalo mwake, kodi simuyika pa choyikapo chake?
21 Naatu i’uwih, “Kwa ramef kwabito’ab i noukwatamaim kwatatarafut? O gem babanamaim kwaya’iyai? Ai ana sisikofamaim kwasisikof?
22 Pakuti chilichonse chobisika chidzayenera kuwululika, ndi chilichonse chachinsinsi chidzayenera kuonekera poyera.
22 Anayabin sawar abisa baibunuwenamaim ti’inu’in boro hinagatur, naatu sawar abisa wa’iwa’irih ti’inu’in boro hinatit hinibebeyan.
23 Ngati wina ali ndi makutu akumva, amve.”
23 O yait tain nama’am na’at iti tur inanowar inanot!”
24 Anapitiriza nati, “Ganizirani mosamala zimene mukumva, ndi muyeso umene mugwiritsa ntchito, mudzayesedwa nawo, ndipo ngakhale kwambiri.
24 Ibanak iuwih maiye, “Kwananowar gewas! O sabuw kufufufunih na’atube, nati fufun ta’imonamaim boro God o nafufuni, baise boro afe’enamaim naya’abar auman nafufuni.
25 Amene ali nazo adzapatsidwa zochuluka; amene alibe, ngakhale zimene ali nazo zidzachotsedwa kwa iwo.”
25 Yait aurin ema’am boro afe’en hinaya’abar hinitin, yait aurin en, abistanawat biyan ti’inu’in boro hinabosair.”
26 Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka.
26 Ibanak eo maiye, “God ana aiwob i orot ub me yan tatanum na’atube.
27 Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira.
27 Fai mar in emimisir, i men so’ob ub i mi’itube kuboun yen erara’at.
28 Nthaka pa yokha imatulutsa mbewu, umayamba mʼmera, kenaka ngala, kenaka mbewu yokhwima mʼngalayo.
28 Me akisin ub ituw eyey, wantoro’ot i boro nakufufun, naatu naiwan nayai, imaibo boro niw ro’on namatar.
29 Mbewuyo ikangokhwima, amayimweta chifukwa nthawi yokolola yakwana.”
29 Naatu sanabey ibiyamur ana maramaim, masaw bowayan boro ana nikok nab natit nan natar.”
30 Ndipo anatinso, “Kodi tinene kuti ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani, kapena ndi fanizo lotani limene tidzagwiritsa ntchito pakuwufotokozera?
30 Naatu ibanak eo maiye, “God ana aiwob boro abisa’amaim tanayai tanao, o oroubon boro menatanamaim tanakubuna kwananowar?
31 Uli ngati mbewu ya mpiru imene ndi mbewu yayingʼono kwambiri yomwe mumadzala mʼnthaka.
31 I ana itinin i momor ro’on kikimin maiyow na’atube, tafaramamaim iti ro’on i kikimin maiyow o boro me yan inatanum.
32 Koma ikadzalidwa, imakula ndi kukhala yayikulu koposa mbewu zina zonse za mʼmunda ndipo mʼnthambi zake zazikulu mbalame zamlengalenga zimadzapuma pa mthunzi wake.”
32 Baise inatatanun ufunamaim, boro nara’at nayen masaw etei nanatabir, ai gagamin famefamen auman namatar, naatu famenamaim mamu boro hinan hinabatar.”
33 Ndi mafanizo ambiri onga awa Yesu anayankhula mawu kwa iwo, monga mmene akanatha kumvetsa.
33 Oroubon maumurih na’in iti na’atube imaim binan sabuw hima hinowar, saife isah tirerereb naniyan hitab.
34 Iye sananene kanthu kwa iwo osagwiritsa ntchito fanizo. Koma ali yekha ndi ophunzira ake, ankawatanthauzira zonse.
34 Sabuw isah i oroubonamaim eo hinonowar, baise nabinamaim oroubon hai yabih i ana bai’ufununayah eo hinonowar.
35 Tsiku limenelo atafika madzulo, anawuza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina.”
35 Nati veya ta’imon ana rabirab, i ana bai’ufununayah iuwih, “It i boro tanarabon harew rounane.”
36 Atasiya gulu la anthu mʼmbuyo, anamutenga Iye, napita naye monga momwe anali mʼbwatolo. Panalinso mabwato ena pamodzi ndi Iye.
36 Ana bai’ufununayah hire wa i afe’en ma’amamaim hisra’at. Naatu wa afa i nati’imaim auman hibatabat.
37 Mphepo yamkuntho inabuka, ndipo mafunde anawomba bwatolo, kotero kuti linali pafupi kumira.
37 Hirarabon wowog tafair tit, naatu yabat misir, harew wa wanawanan iwan yen awan kakaratan. Wa yabat wanawanan run|alt="boat in storm" src="CN01707B.TIF" size="col" loc="Mrk 4.37" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="4.37"
38 Pa nthawi imeneyi Yesu anali akugona atatsamira pilo kumbuyo kwa bwato. Ophunzira anamudzutsa nati kwa Iye, “Aphunzitsi, kodi simukusamala kuti timira?”
38 Jesu wa uranane ukwarin kunuwar yara’ah matan fot inu’in. Ana bai’ufununayah hibunibun misir hiu, “Bai’obaiyenayan it morob isan men kunotanot?”
39 Yesu anauka nadzudzula mphepo nati kwa mafunde, “Chete! Khala bata!” Pamenepo mphepo inaleka ndipo kunachita bata.
39 Misir wowog naatu yabat kwarar eo, “Kwanutanub! Kwa’inbaibinub!” Naatu wowog morob ra’iy nuwarob eafuw.
40 Iye anati kwa ophunzira ake, “Muli ndi mantha chifukwa chiyani? Kodi mukanalibe chikhulupiriro?”
40 Ana bai’ufununayah iuwih, “Aisim kwabirubir? Kwa men kwabitumatum?”
41 Iwo anachita mantha nafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndani? Ngakhale mphepo ndi nyanja zimumvera Iye!”
41 Ana bai’ufununayah hibir naatu taiyuwih hibabatiyih, “Iti orot i yait? Wowog naatu yabat hairi fanan hibai!”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Marcos 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.