Marcos 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Chiyambi cha Uthenga Wabwino wa Yesu Khristu, Mwana wa Mulungu,
1 Iti i Tur Gewasin ana busurufin i Jesu Keriso God Natun isan.
2 monga zalembedwera mʼbuku la mneneri Yesaya:
2 Ana tur i dinab orot Isaiah kikirum imaim busuruf eo.
3 “Mawu a wofuwula mʼchipululu,
3 Orot ta fanan arar yanamaim eafa’af,
4 Ndipo Yohane anabwera mʼmadera a mʼchipululu nabatiza, ndi kulalikira za ubatizo wa kutembenuka mtima ndi wa chikhululukiro cha machimo.
4 John arar yanane tit na dogor baikitabir bapataito bain, saise God bowabow kakafih notawiyen isan binan.
5 Madera onse a ku Yudeya ndi anthu onse a ku Yerusalemu anatuluka napita kwa iye. Akavomereza machimo awo, amawabatiza mu mtsinje wa Yorodani.
5 Judea bar merar tutufin etei naatu Jerusalem sabuw tutufin etei hitit hin biyan hitit. Hai kakafih hi’e’en naatu Jordan harewamaim bapataito itih.
6 Yohane amavala zovala zopangidwa ndi ubweya wangamira, ndi lamba wachikopa mʼchiwuno mwake, ndipo amadya dzombe ndi uchi wamthengo.
6 John ana faifuw i camel bunibunin sakir iyoun, naatu ana kikir i bobaituw ta kanabin e’afuw naiwan kik, ana bay i sisik naatu kutor tafu.
7 Ndipo uthenga wake unali uwu: “Pambuyo panga pakubwera wina wondiposa ine mphamvu. Ine si woyenera kuwerama ndi kumasula zingwe za nsapato zake.
7 Ana tur i iti binan, “Orot ta ayu ufu’umaim enan ana fair i ra’at ayu natabiru, an ana sumasum ayu men karam boro ana kwafure anarufam. John Baptist ebibinan|alt="John the baptist" src="CN01653b.tif" size="col" loc="Mrk 1.7" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="1.7-8"
8 Ine ndikubatizani ndi madzi, koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.”
8 Ayu i harewamaim bapataito abit, baise i boro Anun Kakafiyinamaim bapataito nit.”
9 Pa nthawi imeneyo Yesu anabwera kuchokera ku Nazareti wa ku Galileya ndipo anabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani.
9 Nati ana veya’amaim tafaram gagamin Galilee wanawanan bar merar Nazarethane Jesu na Jordan harewamaim John bapataito itin.
10 Pamene Yesu ankatuluka mʼmadzi, anaona kumwamba kukutsekuka ndipo Mzimu Woyera akutsikira pa Iye ngati nkhunda.
10 Jesu harewane yey ana maramaim, mar botawiy, Anun Kakafiyin mamu imak na’atube re na tafan yey itin.
11 Ndipo Mawu anamveka kuchokera kumwamba: “Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa; ndipo ndikondwera nawe.”
11 Naatu maramaim orot fanan tit eo, “O i ayu Natu, ayu Natu au yabow, o isa ayu abiyasisir.”
12 Nthawi yomweyo Mzimu Woyera anamutumiza Iye ku chipululu,
12 Mar ta’imonamo Anun Kakafiyin iunawiy arar yan tit.
13 ndipo anali mʼchipululumo masiku makumi anayi, akuyesedwa ndi Satana. Anali pakati pa nyama zakuthengo; ndipo angelo anamutumikira.
13 Veya 40 na’atube imaim ma, Satan routobon itin. Sigarafor yumatah ta ta wanawanahimaim, naatu tounamatar nati’imaim i hina hitatafafar.
14 Yohane atamutsekera mʼndende, Yesu anapita ku Galileya nalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu nati,
14 John dibur hiyayari’iy ufunamaim Jesu na Galilee tit, naatu God ana tur gewasin binan eo,
15 “Nthawi yafika, ufumu wa Mulungu wayandikira. Tembenukani mtima ndi kukhulupirira Uthenga Wabwino!”
15 “Veya anababatun i na tit, God ana aiwob i na iyubin, bowabow kakafin kwasisinaf i kwanihamiyen kwanamatabir tur gewasin kwanitumitum!”
16 Pamene Yesu ankayenda mʼmbali mwa nyanja ya Galileya, anaona Simoni ndi mʼbale wake Andreya akuponya khoka mʼnyanja, popeza anali asodzi.
16 Naatu Jesu harew Galilee kukuf dones yan remor inan, siy bowayah orot rou’ab itih, Simon Peter tain Andrew hairi buwatamaim siy hibowabow.
17 Yesu anati, “Bwerani, tsateni Ine, ndipo ndidzakusandutsani asodzi a anthu.”
17 Jesu iuwih eo, “Kwai’ufnunu bairi tan ayu boro ani’obaiyi sabuw kwanabow.”
18 Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.
18 Mar ta’imonamo hai buwat hihamiyen naatu hi’ufunun bairi hin.
19 Atapita patsogolo pangʼono, anaona Yakobo ndi mʼbale wake Yohane ana a Zebedayo, ali mʼbwato akukonza makoka awo.
19 In kikiminamo orot rou’ab itih, James tain John hairi, orot Zebedee natunatun, hai wa wanawanan hima hai buwat hiyayabuna.
20 Mosataya nthawi anawayitana, ndipo anasiya abambo awo Zebedayo ndi anyamata aganyu ali mʼbwatomo, namutsata Iye.
20 Jesu e’afa’af ana veya hairi matah kabiy himisir tamah Zebedee ana bowabow sabuw bairi wa afe’en hihamiyih hima, i Jesu hi’ufunun bairi hin.
21 Iwo anapita ku Kaperenawo, ndipo tsiku la Sabata litafika, Yesu analowa mʼsunagoge nayamba kuphunzitsa.
21 Jesu ana bai’ufununayah bairi hina tafaram Capernaum hitit, naatu Baiyarir ana veya na Kou’ay Bar run naatu busuruf i’obaiyih eo.
22 Anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake, chifukwa anawaphunzitsa ngati munthu amene anali ndi ulamuliro, osati ngati aphunzitsi amalamulo.
22 Sabuw hinonowar hifofofor men kafaita. Anayabin bai’obaiyen bitih ana itinin i roubabaruwen ana fairamaim bi’obaiyih, men Ofafar bai’obaiyenayah na’atube’emih.
23 Pomwepo munthu wina mʼsunagogemo amene anali wogwidwa ndi mzimu woyipa anafuwula kuti,
23 Men yok afiy kakafin orot iwanasum ma’am na Kou’ay Bar run ikirir eo,
24 “Mukufuna chiyani kwa ife, Yesu wa ku Nazareti? Kodi mwabwera kudzatiwononga? Ndikudziwa kuti ndinu ndani, ndinu Woyerayo wa Mulungu!”
24 “Jesu Nazareth mowan, aki biyai’imaim o abisa sinafumih kukokok? O kukokok aki inagurusi’imih? Ayu aso’ob o i yait, O i God ana Orot Kakafiyin!”
25 Yesu anadzudzula chiwandacho mwamphamvu nati, “Khala chete! Tuluka mwa iye!”
25 Jesu afiy kakafin kwarar iu, “Awa efot orot biyanamaim kutit!”
26 Mzimu woyipawo unamugwedeza mwamphamvu ndipo unatuluka mwa iye ukufuwula.
26 Afiy kakafin orot iyuwiyuw naatu fanan auman bihir tit.
27 Anthu anadabwa kwambiri kotero kuti anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Ichi nʼchiyani? Chiphunzitso chatsopano ndi ulamuliro! Iye akulamula, ngakhale mizimu yoyipa ikumumvera.”
27 Sabuw etei hifofofor men kafaita naatu taiyuwih hibabatiyih hio, “Iti anayabin i abisa? Bai’obaiyen boubun roubabaruwen ana fair auman, anayabin afiy kakafih eo biyunih i fanan tebaib!”
28 Mbiri yake inafalikira kudera lonse la Galileya mofulumira.
28 Naatu Jesu ana tur saisewat tasasar tit tafaram Galilee ana uman men sanet hima’am eretei tur hinowar.
29 Atangochoka mu sunagoge, Yesu pamodzi ndi Yakobo ndi Yohane anakalowa mʼnyumba ya Simoni ndi Andreya.
29 Kou’ay Bar hibihamiy ufunamaim James, John hairi mutufor hin Simon Andrew hairi hai bar hitit.
30 Mpongozi wa Simoni anali chigonere akudwala malungo, ndipo anamuwuza Yesu za iye.
30 Simon rawan babin sawow biyan fora’ab inu’in Jesu na titit ana veya ana tur hi’owen,
31 Ndipo Yesu anapita kwa iye, namugwira dzanja namuthandiza kudzuka. Malungo anachoka ndipo anayamba kuwatumikira.
31 Naatu na biyan tit uman bai ibais misir, nati’imaim sawow ihamiy busuruf bow.
32 Madzulo omwewo dzuwa litalowa anthu anabweretsa kwa Yesu anthu onse odwala ndi ogwidwa ndi ziwanda.
32 Nati rabirab veya re’er auman sabuw sawusawuwih naatu afa demon hitarsumih hima’am hibuwih hina Jesu isan.
33 Anthu onse a mʼmudzimo anasonkhana pa khomo,
33 Sabuw nati bar merar hima’am etei hiru’ay nati bar nanamaim,
34 Yesu anachiritsa ambiri amene anali ndi matenda osiyanasiyana, komanso anatulutsa ziwanda zambiri, ndipo sanalole kuti ziwandazo ziyankhule chifukwa zinkamudziwa Iye.
34 Jesu sawow yumatah ta ta hibow hinan etei iyawasih naatu demon moumurih nunih hitit, men ibasit boro demon tihamiyih tur hitao, anayabin i hiso’ob i yait.
35 Mmamawa, kukanali kamdima, Yesu anadzuka, nachoka pa nyumbapo kupita kumalo kwa yekha, kumene anakapemphera.
35 Mar tomih ana gugumin iu’ufiy auman Jesu misir bar ihamiy tit remor in bar merar gagamin natabir na efan noutanubinamaim tit imaim ma yoyoban.
36 Simoni ndi anzake anapita kokamufunafuna Iye,
36 Baise Simon ana ofonah bairi hitit hinuwih hin.
37 ndipo atamupeza, anamuwuza kuti, “Aliyense akukufunani!”
37 Naatu hititita’urih ana veya hi’u, “Sabuw o tenunuwihi.”
38 Yesu anayakha kuti, “Tiyeni tipite kwina ku midzi ya pafupi kuti ndikalalikirenso kumeneko. Ichi ndi chifukwa chimene ndinabwerera.”
38 Baise Jesu iyafutih eo, “It tanan bar merar afa iti bar merar gagamin sisibinamaim auman isah anabinan, anayabin nati isan ayu ana.”
39 Potero anayendayenda mu Galileya, kulalikira mʼmasunagoge awo ndi kutulutsa ziwanda.
39 Imih Galilee wanawanan etei remor hai Kou’ay Baremaim binan naatu demon kakafih nunih hitit.
40 Munthu wakhate anabwera kwa Iye, nagwada, namupempha kuti, “Ngati mukufuna, mukhoza kundiyeretsa.”
40 Orot biyan kokom ani’anin na Jesu nanamaim tit sun yowen baibaisin isan ifefeyan eo, “Inakokok na’at basit iniwa’an anigewasin.”
41 Yesu pomva naye chifundo, anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo nati, “Ndikufuna, yeretsedwa!”
41 Jesu dogoron wanawanan yababan awan karatan uman ru’atayan naatu biyan butubun eo, “Ayu akokok. Kwigewasin!”
42 Nthawi yomweyo khate linachoka ndipo anachiritsidwa.
42 Mar ta’imonamo orot biyan kokom hihururuwih hire naatu igewasin.
43 Nthawi yomweyo Yesu anamuwuza kuti apite koma anamuchenjeza kuti,
43 Baise Jesu ana baimatnuwen tur fokarinaka orot iu naatu biyafar eo,
44 “Wonetsetsa kuti usawuze aliyense za zimenezi. Koma pita, kadzionetse wekha kwa wansembe ndi kukapereka nsembe zimene Mose analamulira zotsimikizira kuyeretsedwa kwanu, ngati umboni kwa iwo.”
44 “Inanowar men yait ta ana tur ina’owen, baise mutufor inan firis biyan inatit o biya nanutitiy, naatu Moses eo na’atube sibor inayai, saise orot babin matahimaim hinaso’ob o igewasin.”
45 Mʼmalo mwake anapita nayamba kuyankhula momasuka, nafalitsa mbiriyo. Zotsatira zake, Yesu sanathe kulowa mʼmudzi moonekera, koma anakhala kunja kumalo kopanda anthu. Komabe anthu amabwera kwa Iye kuchokera kulikonse.
45 Baise orot tit in busuruf tur bosemor tafaram etei bai. I ana turamaim Jesu men karam boro bebeyan tan bar merar tarun, imih i efan noutanubinamaim ma, baise sabuw efan ta ta i boro’ika hina biyan hititit.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Marcos 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.