Lucas 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs MNT

Sair da comparação
MNT Minaifia NT
1 Ambiri anayesa kufotokoza nkhani ya zimene zinakwaniritsidwa pakati pathu,
1 Are Theophilus, Sabuw maumurih na’in abisa iti biyatamaim mamatar isan hisinaftobon ana tur etei’imak bukamaim hikirumen.
2 monga mmene zinaperekedwera kwa ife ndi iwo amene anaona poyambirira ndi atumiki a mawu.
2 Abisa hikikirum i sabuw iyab iti sawar matar matah yan hi’itin hio hinonowar i hikirum, naatu sabuw iyab iti tur isan hibow hibibinan i hio hinowar hikirum.
3 Popeza inenso ndafufuza mosamalitsa chilichonse kuyambira pachiyambi, zandikomera kukulemberani mwatsatanetsatane inu wolemekezeka Tiofilo,
3 Isan imih Theophilus o i gewas maiyow, ayu iti sawar himamatar isan kiruminamih anot, imih sawar no aneika anutitiy, sabuw ai babatiyih hai an abow gewas, naatu akubaitutur o isa iti a kikirum,
4 kuti mudziwe bwinobwino zoona za zinthu zimene mwaphunzitsidwa.
4 saise o boro inaso’ob sawar iti etei o hibi’obaiyi i turobe.
5 Mʼmasiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali wansembe dzina lake Zakariya wa gulu la ansembe la Abiya; mkazi wake Elizabeti analinso wa fuko la Aaroni.
5 Judea wanawanan Herod bi’aiwob ana maramaim, firis wabin Zechariah i Abaijah ana kou’ay wanawanan ma firis ana bowabow bowabow, naatu aawan Elizabeth ana tufuw an i Aaron ana rara’ane na tufuw.
6 Onse awiri anali olungama pamaso pa Mulungu, ndipo amasunga malamulo ndi malangizo onse a Ambuye osalakwa konse.
6 Iti orot aawan hairi God matanamaim hai yawas i gewasin, God ana ofafar naatu ana tur etei hibosiyasiyar hibi’ufunun.
7 Koma analibe ana chifukwa Elizabeti anali wosabereka; ndipo onse anali okalamba.
7 Baise hairi natunatuh en hima hin hiregah hibabine, anayabin Elizabeth i a’arin.
8 Nthawi yogwira ntchito yotumikira ansembe a gulu la Zekariya, Zekariya ankatumikira ngati wansembe pamaso pa Mulungu,
8 Veya ta Jerusalem Tafaror Bar gagamin wanawanan firis ana bowabow isan matan fufur tebowabow na’atube, Zechariah ibo ana veya na tit Tafaror Bar wanawanan ana bowabow isan run.
9 Zakariyayo anasankhidwa mwa maere, monga mwa mwambo wa unsembe, kupita mʼNyumba ya Ambuye kukafukiza lubani.
9 Firis hai binanakwaramaim eo na’atube, gem kakafiyin tafanamaim fi’ufiu afunin isan hibi’arow Zechariah wabin tit, basit na Regah ana Tafaror Bar wanawanan run.
10 Ndipo nthawi yofukiza lubani itafika, gulu lonse lopembedza linkapemphera kunja.
10 Naatu Tafaror Bar wanawanan fi’ufiu Zechariah ea’afun ana veya’amaim, sabuw etei i bar ufunane hibat hiyoyoyoban.
11 Kenaka mngelo wa Ambuye anaonekera kwa iye, atayimirira ku dzanja lamanja la guwa lofukizira.
11 Regah ana tounamatar, gem kakafiyin tainin asukwafune fi’ufiu ea’afunimaim tit irerereb bat.
12 Zakariya ataona mngeloyo, anadzidzimuka ndipo anagwidwa ndi mantha.
12 Zechariah tounamatar tit batabat itin yan hamu iwa’an ana bir ra’at,
13 Koma mngeloyo anati kwa iye: “Usachite mantha, Zakariya; pemphero lako lamveka. Mkazi wako Elizabeti adzakuberekera iwe mwana wamwamuna ndipo udzamutche dzina loti Yohane.
13 baise tounamatar eo, “Zechariah men inabir! God a yoyoban nowar. O aaw Elizabeth boro yan namatar naatu nataub kek orot nayai o wabin John iniwab.
14 Ndipo adzakhala chimwemwe ndi chisangalalo kwa iwe, ndipo ambiri adzasangalala chifukwa cha kubadwa kwake,
14 Nati kek orot natutufuw ana veya o ya wanawanan boro yasisir kawasa awan nakaratan, na’atube sabuw moumurih maiyow auman boro hiniyasisir,
15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Ambuye. Iye sadzamwa vinyo kapena chakumwa choledzeretsa, ndipo adzazadzidwa ndi Mzimu Woyera kuyambira pa kubadwa.
15 anayabin Regah matanamaim i boro orot gagamin ta. Iti kek wine o harew fokarih men natom, naatu God Anunin Kakafiyin boro niwanasum aumannama’ama natufuw.
16 Iye adzabweretsanso Aisraeli ambiri kwa Ambuye Mulungu wawo.
16 I boro Israel sabuw maumurih na’in nabow hinamatabir maiye Regah hai God isan.
17 Ndipo iye adzabwera Ambuye asanabwere mu mzimu ndi mphamvu ya Eliya. Adzatembenuzira mitima ya abambo kwa ana awo ndi osamvera ku nzeru ya olungama, kuthandiza anthu kuti akonzekere kubwera kwa Ambuye.”
17 Naatu God ana dinab orot Elijah ana fair baib na’atube boro nab Regah aunan ni’iyon nan, kek tamahinah bairi dogoroh nikitabir hinan hinita’imon maiye; sabuw baifanasairayah dogoroh nikitabir hinan mutufor ma ana not gewasin hinab, naatu Regah ana sabuw nabobunabuna’ih.”
18 Zakariya anamufunsa mngeloyo kuti, “Kodi ndingatsimikize bwanji zimenezi? Ine ndine wokalamba ndipo mkazi wanga ali ndi zaka zambiri.”
18 Zechariah tounamatar iu, “Iti i boro mi’itube anitumatum? Anayabin ayu i ai regah, naatu aawau auman ibabine sawar.”
19 Mngeloyo anayankha kuti, “Ine ndine Gabrieli. Ndimayima pamaso pa Mulungu, ndipo ndatumidwa kwa iwe kudzakuwuza uthenga wabwinowu.
19 Tounamatar iya’afut eo, “Ayu i Gabriel God nanamaim abatabat, imih ayu iyafaru o airit oisan tur gewasin abai ana o a tur ao’owen,
20 Ndipo kuyambira tsopano sudzatha kuyankhula kufikira izi zitachitika chifukwa sunakhulupirire mawu awa, amene adzakwaniritsidwe pa nthawi yake yoyenera.”
20 baise ayu au tur men itumitum, imih o boro mena nabit, inama nanan sawar mataramih ao ana veya’amaim namatar, abisa ao’omatan nan niturobe.”
21 Pa nthawiyi, anthu ankadikira Zakariya ndipo anadabwa chifukwa anatenga nthawi yayitali ali mʼNyumba ya Mulungu.
21 Nati ana maramaim sabuw ufunane hima’am hai kasiy ra’at, Zechariah manin maiyow Tafaror Bar wanawanan ma’am isan.
22 Atatuluka sanathe kuyankhulana nawo. Anazindikira kuti anaona masomphenya mʼNyumbamo, chifukwa ankasonyeza zizindikiro kwa iwo koma sankatha kuyankhula.
22 Naatu Zechariah Tafaror Barene titit ana mar, tur oisan menan bit, sabuw nati’imaim hi’itin hiso’ob ina’inan ta isan matar, naatu tur o isan menan bit umanamaim imanuman bairi hio.
23 Nthawi yake yotumikira itatha, anabwerera kwawo.
23 Zechariah ana bowabow Tafaror Bar wanawanan sasawar ufunamaim matabir maiye na ana bar tit.
24 Zitatha izi, mkazi wake Elizabeti anakhala ndi pakati ndipo anadzibisa kwa miyezi isanu.
24 Nati ufunamaim a wan Elizabeth yan matar, sumar etei umatroun na’atube baremaim nutanub ma.
25 Iye anati, “Ambuye wandichitira izi, kuti mʼmasiku ano wandionetsera kukoma mtima kwake ndi kuchotsa manyazi anga pakati pa anthu.”
25 Elizabeth eo, “Regah bounabo ibaisu au biya’ohow, orot babin matahimaim etei’imak bosair.”
26 Mwezi wachisanu ndi chimodzi, Mulungu anatuma mngelo Gabrieli ku Nazareti, mudzi wa ku Galileya,
26 Elizabeth ana sumar umatroun ta’imon ana maramaim God ana tounamatar Gabriel iyafar in Galilee wanawananamaim bar merar ta wabin Nazareth imaim tit.
27 kwa namwali wopalidwa ubwenzi ndi Yosefe, wa fuko la Davide. Dzina la namwaliyo linali Mariya.
27 Nati’imaim babitai ta biyan numin Joseph, aiwob orot David ana agir ta i ana rum hiomatan ma’ama biyan tit, babitai wabin Mary.
28 Mngeloyo anafika kwa iye nati, “Moni, inu amene Ambuye wakukomerani mtima kwambiri! Ambuye ali ndi inu.”
28 Tounamatar na babitai biyan tit eo, “Tufuw isa nama! Regah o isa i yan ebaib kwanekwan, naatu baigegewasin o ebit.”
29 Mariya anavutika kwambiri ndi mawu awa ndipo anadabwa ndi kulonjera kotere.
29 Mary iti tur nonowar ana veya biyababan na’atube bai naatu ana kasiy ra’at iti merarayow ana’an isan.
30 Koma mngeloyo anati kwa iye, “Usachite mantha Mariya, pakuti wapeza chisomo pamaso Mulungu.
30 Baise tounamatar eo “Mary, men inabirumih, anayabin God o isa ebiyasisir gagamin maiyow.
31 Udzakhala woyembekezera ndipo udzabala mwana wamwamuna ndipo udzamupatse dzina loti Yesu.
31 O boro ya namatar inatoub kek orot inayai, naatu wabin Jesu iniwab.
32 Iye adzakhala wamkulu ndipo adzatchedwa Mwana wa Wammwambamwamba. Ambuye Mulungu adzamupatsa Iye mpando waufumu wa abambo ake Davide,
32 I boro orot gagamin naatu God auyomtoro’ot Natun narouw nao, naatu Regah God boro aiwob nitin, marasika ana’agir David bitin na’atube.
33 ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.”
33 Naatu Jacob ana rara’ane i boro ni’aiwob wanatowan, naatu ana aiwob i boro nama wanatowan, wanatowan ana yomanin en.”
34 Mariya anafunsa mngeloyo kuti, “Izi zingatheke bwanji popeza ine sindidziwa mwamuna?”
34 Mary tounamatar isan eo, “Ayu i biyau numin. Iti i boro mi’itube namatar?”
35 Mngelo anayankha kuti, “Mzimu Woyera adzabwera pa iwe ndipo mphamvu ya Wammwambamwamba idzakuphimba, ndipo Woyerayo amene adzabadwe adzatchedwa Mwana wa Mulungu.
35 Tounamatar iya’afut eo, “Anun kakafiyin boro niwani, naatu God ana fair boro natarsumi, imih iti kek Kakafiyin natutufuw i boro God Natun hinarouw hinao.
36 Ngakhale Elizabeti mʼbale wako adzakhala ndi mwana mu ukalamba wake ndipo iye amene amati ndi wosabereka, uno mwezi wake wachisanu ndi chimodzi.
36 Naatu o tura Elizabeth sabuw a’arin hirouw hio baise boun babine tafan yan matar ana sumar umatroun ta’imon sawar.
37 Pakuti palibe chinthu chosatheka ndi Mulungu.”
37 Anayabin God isan sawar etei’imak i men ta fokarinamih.”
38 Mariya anayankha kuti, “Ine ndine mtumiki wa Ambuye. Zikhale kwa ine monga mwanenera.”
38 Mary eo, “Ayu i Regah ana akir wairafin, abis isou kuo na’atube namatar.” Naatu tounamatar Mary itumar tit.
39 Nthawi imeneyo anakonzeka ndipo anapita mofulumira ku mudzi wa ku mapiri a dziko la Yudeya,
39 Nati ana veya’amaim, Mary matan kabiy bobuna ra’iy yen in Judahwanawananamaim oyaw na’atune bar merar gagamin ta imaim tit,
40 kumene anakalowa mʼnyumba ya Zakariya nalonjera Elizabeti.
40 Zechariah ana bar wanawanan run Elizabeth ana merar yi.
41 Elizabeti atamva moni wa Mariya, mwana anatakataka mʼmimba mwake, ndipo Elizabeti anadzazidwa ndi Mzimu Woyera.
41 Elizabeth Mary ana merarayow nonowar ana maramaim, yan wanawanan kek inu’in ia’ayob, nati’imaim Anun Kakafiyin Elizabeth iwan
42 Anafuwula ndi mawu akulu kuti, “Ndiwe wodala pakati pa akazi, ndipo ndi wodala mwana amene udzabereke!
42 fanan aumetawat eo, “God ana baigegewasin o ebit baibin etei tafahimaim, naatu ya wanawanan a ub auman God ebigegewasin!
43 Koma nʼchifukwa chiyani andikomera mtima kuti amayi a Ambuye anga abwere kwa ine?
43 Aisim sawar gagamin na’in iti na’atube isou matar, au Regah hinah na ebinanawanu?
44 Nthawi yomwe ndinamva mawu akulonjera kwanu, mwana anatakataka mʼmimba mwanga chifukwa cha chimwemwe.
44 O a merarayow anonowar ana mar, kek yau wanawanan inu’in yasisir auman ia’ayob.
45 Wodala iye amene wakhulupirira kuti chimene Ambuye wanena kwa iye chidzakwaniritsidwa!”
45 O a baitumatumamaim baigegewasin ibai, God eo’omatani boro nan turobe namatar!”
46 Ndipo Mariya anati:
46 Mary eo,
47 Ndipo mzimu wanga ukondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,
47 — ausente —
48 pakuti wakumbukira
48 — ausente —
49 pakuti Wamkuluyo wandichitira ine zinthu zazikulu,
49 — ausente —
50 Chifundo chake chifikira kwa iwo amene amuopa Iye
50 — ausente —
51 Iye wachita zamphamvu ndi dzanja lake;
51 — ausente —
52 Iye anachotsa olamulira pa mipando yawo yaufumu,
52 — ausente —
53 Iye wakhutitsa a njala ndi zinthu zabwino
53 — ausente —
54 Iye anathandiza mtumiki wake Israeli,
54 — ausente —
55 Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse
55 — ausente —
56 Mariya anakhala ndi Elizabeti pafupifupi miyezi itatu ndipo kenaka anabwerera kwawo.
56 Mary sumar etei tounu na’atube Elizabeth hairi hima, imaibo matabir maiye na ana bar tit.
57 Itakwana nthawi yoti Elizabeti abereke, anabereka mwana wamwamuna.
57 Elizabeth ana toub isan veya na tit, naatu toub ana kek orot yai.
58 Anansi ndi abale ake anamva kuti Ambuye anamuchitira chifundo chachikulu ndipo anakondwera naye pamodzi.
58 Tain tuwan naatu ana ofonah, God ana baigegewasin gagamin na’in Elizabeth bitin ana tur hinowar hina ana merar hiyi bairi hiyasisir.
59 Pa tsiku lachisanu ndi chitatu anabwera ndi mwana kuti adzachitidwe mdulidwe, ndipo anafuna kumupatsa dzina la abambo ake Zakariya,
59 Naatu fur ta’imon ufunamaim, kek ana’ar mo’on afuwin wabin baiwabin isan tain tuwan etei hina. Tain tuwan hikokok kek wabin i boro Zechariah, tamah wabinamaim hitiwabimih hio,
60 koma amayi ake anayankhula nati, “Ayi, atchulidwe kuti Yohane.”
60 baise hinah eo, “En! Kek wabin i boro John taniwab.”
61 Iwo anati kwa iye, “Palibe mmodzi mwa abale ake amene ali ndi dzina limeneli.”
61 Sabuw hio, “O taituwa wabih men ta nati na’atube ema’ama boro kek wabin nati taniwab.”
62 Pamenepo anapanga zizindikiro kwa abambo ake kuti adziwe dzina limene akanakonda kumutcha mwanayo.
62 Basit umahimaim kek tamah isan himan wabin menatan kokok baiwabin isan hibatiy.
63 Iye anapempha poti alembepo, ndipo chodabwitsa kwa aliyense analemba kuti, “Dzina lake ndi Yohane.”
63 Zechariah eo fef hibai hina hitin imaim kirum eo, “Kek wabin i John.” Sabuw etei hifofofor men kafaita.
64 Nthawi yomweyo pakamwa pake panatsekuka ndi lilime lake linamasuka ndipo anayamba kuyankhula, nayamika Mulungu.
64 Nati ana veya’amaim Zechariah menan bit ma’am menan kerer busuruf tur eo, God bora’ara’ah.
65 Anansi onse anachita mantha kwambiri, ndipo ku madera onse a kumapiri a Yudeya, anthu anayankhula zinthu zonsezi.
65 Taintuwan etei awah hae’e hai baifofofor ra’at, baise abisa himamatar ana tur tasasar tit tafaram Judea wanawanan sabuw etei hinowar.
66 Aliyense amene anamva izi anadabwa nazo nafunsa kuti, “Kodi mwana uyu adzakhala wotani?” Pakuti dzanja la Ambuye lili pa iye.
66 Sabuw etei iti sawar matar ana tur hinonowar isan hai kasiy ra’at taiyuwih hibabatiyih hio, “Iti kek narara’at ana itinin i boro mi’itube?” Anayabin Regah uman i iti kek biyanamaim ma’am.
67 Abambo ake, Zakariya, anadzazidwa ndi Mzimu Woyera ndipo ananenera kuti,
67 John tamah Zechariah Anun Kakafiyin targabuw, God ana ewamaim tabor eo.
68 “Alemekezeke Ambuye, Mulungu wa Israeli
68 — ausente —
69 Iye wakweza nyanga yachipulumutso kwa ife
69 — ausente —
70 (Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera),
70 — ausente —
71 chipulumutso kuchoka kwa adani athu
71 — ausente —
72 kuonetsa chifundo kwa makolo athu
72 — ausente —
73 lumbiro limene analumbira kwa kholo lathu Abrahamu:
73 — ausente —
74 kutilanditsa ife mʼdzanja la adani athu,
74 — ausente —
75 mʼchiyero ndi mʼchilungamo masiku athu onse.
75 — ausente —
76 “Ndipo iwe mwana wanga udzatchedwa mneneri wa Wammwambamwamba;
76 — ausente —
77 kupatsa anthu ake chidziwitso cha chipulumutso
77 — ausente —
78 chifukwa cha chifundo chachikulu cha Mulungu wathu,
78 — ausente —
79 kuwalira iwo okhala mu mdima
79 — ausente —
80 Ndipo mwanayo anakula nakhala wamphamvu mu mzimu; ndipo anakhala ku chipululu mpaka pamene anaonekera poyera mu Israeli.
80 — ausente —

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Lucas 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.