João 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs MNT

Sair da comparação
MNT Minaifia NT
1 Patapita nthawi Yesu anakwera kupita ku Yerusalemu ku phwando la Ayuda.
1 Veya bai’ab sawar ufunamaim, Jew hai hiyuw aa isan Jesu yen in Jerusalem.
2 Ndipo ku Yerusalemuko pafupi ndi chipata cha Nkhosa kuli dziwe limene mʼChihebri limatchedwa Betisaida ndipo ndi lozunguliridwa ndi makumbi asanu.
2 Jerusalem wanawanan efan wabin For Hirahirsisibinamaim i harew kukuf, naatu ana seboseb etei umatroun hiwowaben Aramek fanahimaim tisusu’ub Betsaida,
3 Mʼmenemo munkagonamo gulu lalikulu la anthu odwala, osaona, olumala ndi ofa ziwalo.
3 nati sebosebomaim sabuw sawusawuwih moumurin maiyow hiya hi’inu’in, matah fim, ah umah kafikafirih, naatu ah umah ririmih hima hikakaif harew tabi’etaw isan.
4 Pakuti nthawi zina mngelo wa Ambuye ankatsikira mʼdziwemo nʼkuvundula madziwo. Woyamba kulowamo madzi atavundulidwa, ankachira ngakhale akhale ndi nthenda yanji.
4 Anayabin veya ta ta Regah ana tounamatar boro nara’iy harew kukuf nabenei niyabat rarouw nayen. Naatu sabuw sawow ana yumat ta ta hibow hina ti’inu’in, yait wan nara’iy nakifukif i boro nayawas.
5 Mmodzi wa amene anali pamenepo anali atadwala zaka 38.
5 Orot ta sawow bai ma kwamur etei 38 i nati wanawanahimaim.
6 Yesu atamuona ali chigonere, nadziwa kuti anakhala chotero kwa nthawi yayitali, anamufunsa iye kuti, “Kodi ukufuna kuchira?”
6 Jesu nuw orot nati’imaim inu’in itin, naatu so’ob orot sawow nati bai virurumin maiyow, imih orot ibatiy, “O kukokok inayawas?”
7 Wodwalayo anayankha kuti, “Ambuye, ndilibe wina aliyense woti angandithandize kulowa mʼdziwe pamene madzi avundulidwa. Pamene ndikuyesera kuti ndilowemo, wina amalowamo ine ndisanalowemo.”
7 Orot iya’afut eo, “Regah, anamaramaim harew iyabat rarouw eyey, men yait ta boro nibaisu nabuwu anara’iy harew kukuf yan. Ayu misir ra’iyemih abiwa’an, sabuw afa i wan hira’iyeka.”
8 Ndipo Yesu anati kwa iye, “Imirira! Nyamula mphasa yako yamba kuyenda.”
8 Naatu Jesu orot isan eo, “Kumisir! A ir kunu naatu kuremor kwen.”
9 Nthawi yomweyo munthuyo anachiritsidwa. Iye ananyamula mphasa yake nayamba kuyenda.
9 Mar ta’imon orot yawas; misir ana ir nu bat remor. Iti sawar mamatar i Baiyarir Ana Veya.
10 Ndipo Ayuda anati kwa munthu amene anachiritsidwayo, “Lero ndi la Sabata; lamulo silikulola iwe kunyamula mphasa yako.”
10 Naatu Jew sabuw orot yayawas isan hi’o, “Iti boun i Baiyarir ana veya, ata ofafar men ebibasit o a ir ina’abar.”
11 Koma iye anayankha kuti, “Munthu amene wandichiritsa anati kwa ine, ‘Nyamula mphasa yako yamba kuyenda.’ ”
11 Baise iya’afutih eo, “Orot yait ayu biyawasu iuwu, ‘Kumisir a ir kunu naatu kubat kuremor.’”
12 Pamenepo anamufunsa iye kuti, “Kodi munthu ameneyo ndani amene wakuwuza kuti, ‘Nyamula mphasa yako ndipo yenda?’ ”
12 Imih hibatiy, “Nati orot i yait uwi a ir inu i’abar ibat kureremor?”
13 Munthu amene anachiritsidwayo sanadziwe kuti anali ndani, pakuti Yesu anangolowera mʼgulu la anthu ndi kupita.
13 Orot nati yayawas i men kafa’imo so’ob orot i yait, anayabin sabuw moumurin maiyow nati’imaim hibatabat Jesu sorabon in kasiy.
14 Patapita nthawi Yesu anamupeza ku Nyumba ya Mulungu ndipo anati kwa iye, “Taona uli bwino tsopano. Usakachimwenso kuti choyipa choposa ichi chingakugwere.”
14 Nati ufunamaim Jesu Tafaror Bar wanawanan tita’ur naatu iu, “Kwi’itin, o iyawas. Bowabow kakafih inihamiyen o sawar kakafin anababatun boro biyamaim namatar.”
15 Munthu uja anachoka ndi kukawawuza Ayuda kuti anali Yesu amene anamuchiritsa iye.
15 Orot nati’imaim tit in, Jew sabuw hai tur eowen i Jesu iyawas.
16 Ndipo popeza Yesu amachita zinthu izi tsiku la Sabata, Ayuda anayamba kumulondalonda.
16 Imih hibusuruf Jesu isan turamaim hi’u hi’a’a’afiy, anayabin i Baiyarir ana veya sawar iti na’atube sinaf isan.
17 Yesu anawawuza kuti, “Atate anga amagwira ntchito nthawi zonse mpaka lero lino, ndipo Inenso ndili pa ntchito.”
17 Jesu isah eo, “Ayu Tamai i mar etei ebowabow, imih ayu auman boro anabow.”
18 Chifukwa cha ichi Ayuda anawirikiza kufuna kumupha; osati chifukwa chakuswa Sabata kokha komanso chifukwa ankanena kuti Mulungu ndi Atate ake, nadziyesa Iye wofanana ndi Mulungu.
18 Ana’an iti isan Jew hisinaftobon ef hinuwet Jesu asabunin isan; men Baiyarir ana ofafar ea’eastu’ub akisin, baise God isan Tamah rouw eo’omaim, iwa’an taiyuwin bai yen in God hairi anafofonin matar.
19 Yesu anawapatsa yankho ili: “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Mwana sangathe kuchita kanthu pa Iye yekha. Iye amachita zokhazo zimene amaona Atate ake akuchita, chifukwa chilichonse chimene Atate amachita Mwana amachitanso.
19 Jesu iyafutih eo. “Turobe a tur ao’owen, Orot Natun akisin ana kok men karam nasinaf; baise Tamah abistan sinaf i i’itinimaim boro nasinaf, anayabin Tamah abistan isisinaf na’atube Natun isisinaf.
20 Pakuti Atate amakonda Mwana, amamuonetsa zonse zimene Iwo amachita. Inde, Atate adzamuonetsa zinthu zazikulu kuposa zimenezi ndipo mudzadabwa.
20 Anayabin Tamah i Natun iyabuw sawar etei esisinaf na’atube Natun i’obaiy imaim esisinaf. Turobe, kwa a baifofofor isan, i boro sawar gagamihika ni’obaiy nasinaf men boun iti na’atube.
21 Pakuti monga Atate amaukitsa akufa nawapatsa moyo, momwemonso Mwana amapereka moyo kwa amene Iye akufuna.
21 Tamah murumurubih imisiruwih yawas ebitih na’atube, nati ef ta’imon Natun ekok yait yawas baitinamih boro nitin.
22 Komanso, Atate saweruza aliyense koma wapereka kwa Mwana ulamuliro woweruzawo,
22 I na’atube Tamah men yait ta ebibatiy, baise baibabatiyen ana fair tutufin etei Natun itin.
23 kuti aliyense alemekeze Mwanayo monga momwe amalemekezera Atate. Munthu amene salemekeza Mwana salemekezanso Atate amene anamutuma Mwanayo.
23 Saise sabuw etei Tamah tirurusagiy na’atube, Natun boro hinarusagiy. Imih o yait Natun men kururusagiy, Tamah, i ana baiyonenayan auman men kururusagiy.
24 “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo.
24 “Turobe a tur ao’owen, o yait ayu au tur inowar naatu menatan ayu iyafaru anan kubitumitum, o i yawas ma’ama wanatowan ibaika, naatu o boro men baibatebat inab, anayabin morobone irabon yawas wanawanan irun.
25 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano, pamene akufa adzamva mawu a Mwana wa Mulungu ndipo iwo amene amva adzakhala ndi moyo.
25 Turobe a tur ao’owen, veya i enan naatu i na titaka, nati ana veya murumurubih boro God Natun fanan hinanowar naatu iyab fanan hinanonowar boro yawas hinab hinama.
26 Pakuti monga Atate ali gwero la moyo, momwemonso anapereka mphamvu zopereka moyo mwa Mwana.
26 Anayabin Tamah taiyuwin i yawas an, imih nati yawas ta’imon Natun itin yawas an matar.
27 Ndipo wamupatsa Iye ulamuliro woweruza chifukwa ndi Mwana wa Munthu.
27 Naatu i baibabatiyen ana fair Natun itin, anayabin i, i Orot Natun.
28 “Musadabwe ndi zimenezi. Pakuti nthawi ikubwera pamene onse amene ali mʼmanda adzamva mawu ake
28 “Tur iti ao isan men kwana’ororsa’ir; veya i nati namamataramaim enan, murumurubih etei boro fanan hinanowar,
29 ndi kutuluka. Iwo amene anachita zabwino adzauka ndi kupita ku moyo wosatha ndipo amene anachita zoyipa adzauka ndi kupita ku chilango chamuyaya.
29 hai rahane hinatit, naatu iyab gewasin hisisinaf boro hinamisir yawas hinab, iyab kakafih hinasisinaf boro hinakusairih.”
30 Pakuti sindingathe kuchita kena kalikonse pa ndekha. Ine ndimaweruza molingana ndi zomwe Mulungu wandiwuza ndipo kuweruza kwanga ndi kolungama. Ine sindifuna kudzikondweretsa ndekha koma Iye amene anandituma.
30 “Ayu men karam akisu au kok ana sinaf, baise abisa God iu’uwu’umaim sabuw abibabatiyih, imih ayu au baibatiyen i mutufor, anayabin men ayu au kokomaim asisinaf, baise orot yait ayu iyunu anan i anakok asisinaf.
31 “Ngati ndidzichitira umboni ndekha, umboni wanga si woona.
31 Ayu taiyuwu au sinaf isan ana’o’orereb na’at, au tur i men turobe’emih.
32 Alipo wina amene amandichitira umboni wabwino. Ine ndikudziwa kuti umboni wake wonena za Ine ndi woona.
32 Baise orot ta ayu isou eo’orereb, i a tur ao’owen i ana orereb ayu isou i turobe.
33 “Inu munatumiza amithenga kwa Yohane ndipo iye anachitira umboni choona.
33 Kwaso’ob gewasomih kob abarayah John isan kwaiyafarih hinan John i turobe kwa a tur eowen.
34 Sikuti Ine ndikudalira umboni wa munthu; koma ndikunena zimenezi kuti mupulumutsidwe.
34 Iti i men kwa orot maiyow isou kwataorereb, baise iti ao saise mi’itube kwa yawas kwatab isan.
35 Yohane anali ngati nyale imene imayaka ndi kuwala, ndipo inu kwa kanthawi munasankha kusangalala ndi kuwala kwakeko.
35 John i hinow na’atube to’ab marakaw kwa it, naatu mar kikimin kwa ana marakaw isan kwaiyasisir.
36 “Koma Ine ndili ndi umboni woposa uja wa Yohane. Pakuti ntchito imene Atate andipatsa kuti ndiyikwaniritse ndi imene ndikugwira, ndipo ikundichitira umboni kuti Atate andituma Ine.
36 Baise ayu au orererebayan orot i gagamin, men iti John eo’orereb na’atube. Ayu au orererebayan i abisa Tamai iyunu ana asisinaf i eo’orereb, naatu nati ebi’obaiyi ayu i Tamai iyafaru anasinaf isan, orot ta eo’orereb i John eo’orereb natabir, anayabin iti bowabow ayu Tamai bitu i anisawar, naatu iti bowabowamaim eo’orereb Ayu Tamai iyunu ana i ana bowabow anabow.
37 Ndipo Atate amene anandituma Ine, Iye mwini wandichitira umboni. Inu simunamvepo mawu ake kapena kuona maonekedwe ake,
37 Naatu Tamai iyunu anan i taiyuwin ayu isou eo’orereb. Kwa men kafa’imo fanan kwanowar naatu yumatan kwa’itin.
38 kapena mawu ake kukhala mwa inu, pakuti simukhulupirira Iye amene anamutuma.
38 Kwa ana tur men dogor wanawanan run, anayabin menatan ayu iyunu anan i men kwabitumitum.
39 Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni.
39 Kwa Buk Atamaninamaim hikikirum kwaiyab kwabinotanot anayabin boro imaim yawas wanatowan kwanab. Nati tur i ayu isou eo,
40 Koma inu mukukana kubwera kwa Ine kuti mukhale ndi moyo.
40 baise men kwakokok kwanan ayu biyau yawas kwanab.
41 “Ine sindilandira ulemu kuchokera kwa anthu
41 “Ayu men orot babin bora’ara’ahu isan ao’omih.
42 koma Ine ndikukudziwani. Ndikudziwa kuti mʼmitima mwanu mulibe chikondi cha Mulungu.
42 baise kwa orot babin a yawas ayu aso’ob, kwa a yabow God isan dogoromaim i men ema’am.
43 Ine ndabwera mʼdzina la Atate anga, ndipo inu simukundirandira Ine; koma wina wake akabwera mʼdzina la iye mwini, inu mudzamulandira.
43 Ayu Tamai wabinamaim anan kwa men kwabuwu au merar kwayi, baise orot babin ta i taiyuwin wabinamaim nanan boro kwanab ana merar kwanay.
44 Kodi inu mudzakhulupirira bwanji ngati mumapatsana ulemu wina ndi mnzake, ndipo simufuna kulandira ulemu kuchokera kwa Mulungu yekhayo?
44 Kwa taiyuw baifa’i isan a kok gagamin, baise God ta’imonamo ana baifa’en i men kwakokok, imih ayu abisa ao boro kwanitutumu?
45 “Koma inu musaganize kuti Ine ndidzakunenezani kwa Atate. Wokunenezani ndi Mose, amene inu mwayikapo chiyembekezo chanu.
45 Men kwananot ayu boro Tamai nanamaim ubar kwa bait kwanarouw en, baise Moses kwa a not tutufin imaim kwayai kwama’am boro ubar nabit kwana’itin.
46 Ngati mukanakhulupirira Mose, mukanakhulupiriranso Ine, pakuti iye analemba za Ine.
46 Moses kwatabitumitum na’at, ayu boro kwatitutumu, anayabin i ayu isou kirum.
47 Koma ngati simukhulupirira zimene iye analemba, mudzakhulupirira bwanji zimene Ine ndikunena?”
47 Baise Moses abistan kikirum kwa men kwanabitumatum na’at, boro mi’itube ayu ao kwanitumatum?”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.