João 4
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Yesu atazindikira kuti Afarisi amva zoti Iye ankapeza ndi kubatiza ophunzira ambiri kupambana Yohane,
1 Pharisee hinowar Jesu i bigegesairih naatu John natabir ana bai’ufununayah moumurih na’in bapataito ebitih,
2 (ngakhale kuti Yesuyo sankabatiza, koma ophunzira ake).
2 turobe iti i men Jesu bapataito ebitih, baise i ana bai’ufununayah.
3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.
3 Anamaramaim Jesu, i Judea ihamiy naatu matabir maiye in Galilee.
4 Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.
4 Boun ana remoramaim i boro Samaria wanawanan narun nan.
5 Iye anafika mʼmudzi wa Asamariya wotchedwa Sukari, pafupi ndi malo amene Yakobo anapatsa mwana wake Yosefe.
5 Imih i Samaria bar merar wabin Sychar tit, Jacob ana me kamar i natun Joseph bitin i sisibinamaim.
6 Chitsime cha Yakobo chinali pamenepo ndipo Yesu atatopa ndi ulendo anakhala pansi pambali pa chitsimecho. Nthawi inali pafupifupi ora lachisanu ndi chimodzi masana.
6 Jacob ana harew karakar i nati’imaim, naatu Jesu ef nan hahar, karakar sisibin mara’at ma. Nati i ouyit.
7 Mayi wa Chisamariya atabwera kudzatunga madzi, Yesu anati kwa iye, “Kodi ungandipatse madzi akumwa.”
7 Samaria babin harew huninamih nan anamaramaim, Jesu babin isan eo, “Karam harew ititu atatom?Jesus Samaritan babin hairi tibidudur|alt="Jesus talking to Samaritan woman" src="CN01674B.TIF" size="col" loc="Jhn 4.7" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="4.7"
8 (Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya).
8 I ana bai’ufununayah hin bar merar bay tobonamih.
9 Mayiyo anati kwa Iye, “Inu ndinu Myuda ndipo ine ndine Msamariya. Bwanji mukundipempha madzi akumwa?” (Popeza Ayuda ndi Asamariya sankayanjana).
9 Samaria babin Jesu isan eo, “O i Jew naatu ayu i Samaria babin. Mi’itube ayu isou harewamih kufefefeyan?” (Jew hai naukwat, o hai kerowas boro men Samaria bairi hinafaram hinaa hinatom.)
10 Yesu anamuyankha kuti, “Koma iwe ukanadziwa mphatso ya Mulungu ndi Iye amene akukupempha madzi akumwa, ukanamupempha ndipo akanakupatsa madzi amoyo.”
10 Jesu, babin isan iya’afut eo, “O God ana siwar itasoso’ob na’at yait o isa harew tomamih efefeyan, o boro itibatiy i boro yawas ana harew tit itatom”.
11 Mayiyo anati, “Ambuye, Inu mulibe kanthu kotungira madzi ndipo chitsime ndi chakuya. Kodi madzi amoyowo mungawatenge kuti?
11 Babin eo, “Aro, o taratarfuruwen men ibai ina naatu karakar ana sou i manin na’in ra’iy in. Karakar menatanamaim boro iti yawas ana harew inab?
12 Kodi Inu ndinu wamkulu kuposa kholo lathu Yakobo, amene anatipatsa chitsimechi ndipo iye ankamwanso monga anachita ana ake ndi ziweto zake?”
12 Iti karakar i aki agir Jacob kair imaim ma tomatom, naatu ana haru ana for ouman. Iti karakar aki iti. O taiyuw ku’o’o, o Jacob inatabir?
13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,
13 Jesu iya’afut eo, “Orot babin etei iti harew natomatom boro sikan namamah maiye,
14 koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.”
14 baise yait ayu harew anitin natomatom boro men sikan namamah. Naatu harew nati ayu anabitin boro wanawananamaim harew buruburur namatar. Naatu yawas’anaharew imaim na’in nitin, naatu yawas wanatowan nab.
15 Mayiyo anati kwa Iye, “Ambuye, patseni madzi amenewo kuti ndisadzamvenso ludzu ndi kumabwerabe kuno kudzatunga madzi.”
15 Babin Jesu isan eo,” Aro, harew nati ayu kwiti saise ayu men sikou namamaa nan naatu men mar etei iti’imaim harew huninamih anan.”
16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”
16 Jesu babin iu, “Kwen ku’af aaw isan naatu kumatabir kuna.”
17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.”
17 Babin iya’afut eo, “Ayu aawu en.” Jesu eo,” O aaw en ku’o’o i turobe.”
18 Zoona nʼzakuti iwe wakhala pa banja ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene uli naye tsopano si wako. Zimene wanenazi ndi zoona.”
18 Anababatun, o oro’orot etei five, i aa’awanen naatu orot iti boun airi kwama’am i men o aawamih. Abistan iti boun i’o’o i turobe.”
19 Mayiyo anati, “Ambuye, ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri.
19 Babin eo, “Aro, ayu ai’iti, o i dinab orot.”
20 Makolo athu ankapembedza mʼphiri ili koma inu Ayuda mumati malo amene tiyenera kupembedzera ali ku Yerusalemu.”
20 “Aki ai a’agir iti oyawemaim hikwakwafir, baise kwa Jew kwa’o’o kwafiren efan i Jerusalemamaim tanakwafir.”
21 Yesu anati, “Mayi inu khulupirira Ine. Nthawi ikubwera pamene inu simudzapembedza Atate mʼphiri ili kapena mu Yerusalemu.
21 Jesu eorereb eo, “Babin ayu initutumu, veya i enan anamaramaim kwa boro men Tamat no oyawemaim o Jerusalemamaim kwanakwafir.
22 Inu Asamariya mumapembedza chimene simukuchidziwa. Ife timapembedza chimene tikuchidziwa, pakuti chipulumutso nʼchochokera kwa Ayuda.
22 Kwa Samaria men kwaso’ob abistan kwakwakwafir, aki aso’ob abistan a kwakwafir, anayabin yawas i Jew sabuw biyahine na.
23 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano pamene opembedza woona adzapembedza Atate mu mzimu ndi mʼchoonadi, pakuti opembedza otere ndiwo amene Atate akuwafuna.
23 Veya i enan naatu natitaka anamaramaim anababatun kwafirenayah boro Regah turobe naatu Anuninamaim hinakwafir, naatu kwafirinayah iti na’atube i boun Regah enunuwet.
24 Mulungu ndi Mzimu, ndipo omupembedza Iye ayenera kumupembedza mu mzimu ndi mʼchoonadi.”
24 God i Anunin, naatu i ana kwafirenayah i turobe naatu Anuninamaim hinakwafir.”
25 Mayiyo anati, “Ine ndikudziwa kuti Mesiya (wotchedwa Khristu) akubwera. Akabwera, Iye adzafotokoza zonse kwa ife.”
25 Babin eo, “Ayu nati Roubininenayan i aso’ob (Keriso terarouw) i enan. I nanan ana veya i boro sawar etei it isat nakubuna.”
26 Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”
26 Imaibo Jesu eorereb eo, “Ayu i yait? Ayu yait airit ta’o’o.”
27 Pa nthawi yomweyo ophunzira ake anabwerera ndipo anadabwa kupeza Iye akuyankhula ndi mayi. Koma palibe amene anamufunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” kapena, “Nʼchifukwa chiyani mukuyankhula naye?”
27 Jesu eo oumatan, ana bai’ufununayah himatabir hina hitit naatu Jesu babin hairi hibidudur hi’itih hi’ororsa’ir. Baise men yait ta kok babin tibatiy, o Jesu hitibatiy, “Anayabin aisimamih babin airi kwabidudur?”
28 Kenaka mayiyo anasiya mtsuko wamadzi, nabwerera ku mzinda ndipo anati kwa anthu,
28 Naatu babin ana harew hunihun ihamiy, i matabir in bar merar tit naatu sabuw nati’imaim hima’am hai tur eo’wen,
29 “Tiyeni mukaone munthu amene wandiwuza ine zilizonse zimene ndinazichita. Kodi ameneyu sangakhale Khristu?”
29 Kwana tan orot kwa’itin, sawar abistanawat asisinaf etei’imak au tur eowen. Ta’itin i Roubinineyan wariten?”
30 Iwo anatuluka mʼmudziwo ndi kupita kumene kunali Iye.
30 Naatu bar merar hihamiy naatu sabuw etei ef hinuwet hin Jesu biyan hitit.
31 Pa nthawi imeneyi ndi kuti ophunzira ake akumukakamiza kuti, “Rabi idyani.”
31 Nati ana veya’amaim ana bai’ufununayah hi’o, “Bai’obaiyenayan bay ta ku’aan ya kurutan!”
32 Koma Iye anawawuza kuti, “Ine ndili ndi chakudya choti ndidye chimene inu simukuchidziwa.”
32 Baise i isah eo, “Ayu au bay menamaim ana’ani’aan kwa men kafa’imo kwaso’ob.”
33 Ndipo ophunzira ake anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi alipo wina amene anamubweretsera Iye chakudya?”
33 Imih bai’ufununayah taiyuwih hima hi’o, “Ta’itin sabuw afa bay hibow hina hitin eaa wariten?”
34 Yesu anati, “Chakudya changa ndikuchita chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi kumaliza ntchito yake.
34 Jesu eo, “Ayu au bay, i yait ayu biyafaru i anakok anabosiyasiyar anasinaf naatu bowabow ayu bitu i anabow anisawar.
35 Kodi inu simunena kuti, ‘Kwatsala miyezi inayi ndipo kenaka kukolola?’ Ine ndikukuwuzani kuti, tsekulani maso anu ndipo muyangʼane mʼminda! Mbewu zacha kale kuti zikololedwe.
35 Kwa iti na’atube kwa’o’o, ’Sumar kwafe’en o tafanamaim aki boro anafour’. Baise a tur ao’owen, Kwa matatoniwa’an me kwana’itin gewas naatu bay iyamur sawar fourin isan ana veya tit.
36 Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi.
36 Boun auman fourayan boro hibaiyan ana kabay nab, naatu bay four eya’ay ma’ama wanatowan isan, imih ta’itin tanumayan naatu fourayan i hairi auta’imon hiniyasisir.
37 Nʼchifukwa chake mawu akuti, ‘Wina amafesa ndipo wina amakolola’ ndi woona.
37 Abistan hi’o’o i turobe, “Orot ta’imon etatanum naatu orot ta’imon efafour”.
38 Ine ndinakutumani kukakolola zimene simunagwirire ntchito. Ena anagwira ntchito yolemetsa ndipo inu mwatuta phindu la ntchito yawo.”
38 “Efan men imaim ima ibowabow, ayu aiyafari kwenan inafouramih naatu i hai fairamaim hibowabow o nonowatin inafour inaa’amih”.
39 Asamariya ambiri ochokera mʼmudziwo anakhulupirira Iye chifukwa cha umboni wa mayiyo wakuti, “Iye anandiwuza ine zonse ndinazichita.”
39 Samaria moumurih maiyow nati bar merar Jesu hitumitum anayabin babin ana turamaim, “I ayu au sinaf etei eo anowar”.
40 Choncho Asamariya atabwera kwa Iye, anamuwumiriza Iye kuti akhale nawo, ndipo Iye anakhala nawo masiku awiri.
40 Imih anamaramaim Samaria sabuw hina Jesu biyan hititit, hifefeyan bairi ma isan, imih veya rou’ab bairi hima.
41 Ndipo chifukwa cha mawu ake, ena ambiri anakhulupirira.
41 Sabuw moumurin maiyow hitumatum anayabin i ana turamaim,
42 Iwo anati kwa mayiyo, “Ife sitikukhulupirira chifukwa cha mawu ako okha, koma tsopano ife tadzimvera tokha, ndipo tikudziwa kuti munthu uyu ndithu ndi Mpulumutsi wa dziko lapansi.”
42 naatu babin isan hi’o, “Aki bounabo abitumatum, men babin i’o isan, baise abistan tur eo’o aki taiyuwika taini anowar”.
43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya.
43 Veya rou’ab sasawar ufunamaim Jesu efan nati ihamiy, naatu au Galilee na’at misir in.
44 (Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).
44 Anayabin i taiyuwin isan eorereb eo, “Dinab orot taiyuwin ana tafaram sabuw isan men tekakakaf”.
45 Iye atafika ku Galileya, Agalileya anamulandira. Iwo anali ataona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pa phwando la Paska, pakuti iwonso anali komweko.
45 Imih anamaramaim na Galilee titit, sabuw ana merar hiyi hibai. Anayabin hin Jerusalem Tar Nowaten Hiyuw aa isan hiruru’ay, nati’imaim sawar abistanawat sinaf hi’i’itin isan.
46 Iye anakafikanso ku Kana wa ku Galileya, kumene anasanduliza madzi kukhala vinyo. Ndipo kumeneko kunali nduna ina ya mfumu imene mwana wake wamwamuna anali chigonere akudwala ku Kaperenawo.
46 Naatu matabir maiye in Canna tit, nati Canna i Galilee wanawanan, imaim harew botabir wine mamatar. Naatu nati’imaim gawan ana orot ukwarin natun sawow Capernaumamaim inu’in.
47 Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.
47 Jesu Judea’ane na Galilee tit ma’am ana tur na nowar. Misir in biyan tit ana tur eowen naatu ifefeyan i tare tan natun sawow inu’in tiyawas i kafa’imo namorob.
48 Yesu anawawuza iwo kuti, “Anthu inu pokhapokha mutaona zizindikiro zodabwitsa, simudzakhulupirira.”
48 Jesu sabuw iuwih, “Kwa sabuw ina’inan naatu baifofofor kwana’itah, baise boro men kwanitumatum.”
49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”
49 Gawan ana orot ukwarin Jesu isan eo, “Aro, inare tananabo au kek namorob.”
50 Yesu anayankha kuti, “Pita. Mwana wako adzakhala ndi moyo.”
50 Jesu orot isan eo, “Kwen! O a kek yawas ema’am!” Orot itumatum abistan Jesu tur isan eo naatu ana ef rura’ah in.
51 Iye ali pa njira, antchito ake anakumana naye, namuwuza kuti mwana wanu uja wachira.
51 I ra’iy inan efamaim ana akir orot bairi hitar naatu ana tur hi’owen, “O a kek i yawas ema’am
52 Iye atafunsa kuti ndi nthawi yanji imene mwana wake anapeza bwino, iwo anati kwa iye, “Malungo anamusiya iye dzulo pa ora lachisanu ndi chiwiri.”
52 Naatu ibatiyih, Veya abistanamaim au kek yawas?” Naatu i hiya’afut hi’o, “Fai ouyit one korok na’atube imaim sawow ihamiy”.
53 Ndipo bamboyo anazindikira kuti iyi inali nthawi yomweyo imene Yesu anati kwa iye, “Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Choncho iye ndi onse a pa banja lake anakhulupirira.
53 Naatu imaibo tamah not nati ana veya Jesu eo, “O a kek i boro nayawas.” Imih nati ana baremaim hima’am etei hitumatum.
54 Ichi ndiye chinali chizindikiro chodabwitsa chachiwiri chimene Yesu anachita atafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya.
54 Iti ina’inan bairu’abin men tesinaf emamatar Jesu sinaf matar, no Judea’ane na au Galilee inan ufunamaim.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.